Ma followers a UTM tilipo?? Ngat tilipo manja mmwamba 🙋♂️
@sarahmphande610824 күн бұрын
Thumb up
@clementmahoka628724 күн бұрын
Tilipo ife
@chimeraJonathan24 күн бұрын
Pop L OLo Ok Oi
@chimeraJonathan24 күн бұрын
@@sarahmphande6108 😅ll
@masulasanudi728624 күн бұрын
❤ here
@kettiemkweu452824 күн бұрын
My UTM fellow let’s gather here. Ndikuti 2025 I will be in Malawi all the way from America just to vote for my UTM UTM you got my Vote ❤
@Littlefair725 күн бұрын
Great move UTM family. Koma going forward tiyeni tidzipanga ma decision mofulumira, kunjaku nkwa mvula.
@PeterDandaula-ci5un25 күн бұрын
Ndipo live
@MariamJohn-dg4em25 күн бұрын
Tiri pa mbuyo panu mama osaopa osatopa osafooka, ine sindinavoteko koma next year ndikavota, viva UTM viva mai kaliyati viva SKC
@user-rx1dj7kg8k25 күн бұрын
Inenso ndukavota🎉
@RachelDongolosi25 күн бұрын
Amen 🙏
@user-uf4hp6lu8t24 күн бұрын
Am following you ❤❤
@paulmgombebanda-mr19sate24 күн бұрын
Well done
@user-tk6qh9zs7h23 күн бұрын
@@MariamJohn-dg4em palitu kusiyana pakati pa UTM ndi Malemu SKC. CHILIMA anapeza mavote okwana 1 million pomwe UTM ngati Chipani inapeza Aphungu Anayi okha basi.Ngakhale Kaliati anakanidwa kwawo pa Udindo wa u MP kamba koimira utm ndiye kumachangamuka pochita zinthu. Fame ya Malemu SKC si fame ya UTM as a political party.
@petermark659124 күн бұрын
Ifeyo monga a UTM tasangalala kwambiri coz chotuluka mu tonse Kuti mzimu wa president athu achilima ukhale osangalala, glory to Jesus.
@LeganNyirenda25 күн бұрын
Applause ❤mama for standing film against this alliance.
@fahadwalipeya865625 күн бұрын
Well done ife ndale zanu zopusazo zophanazo ayi UTM in our hearts forever 💕💕💯💪
@user-ri8em6my2e25 күн бұрын
Boom !🔥🔥inuyo mwabwera ngati coming 💃💃
@ReferendumsWaya-y4q24 күн бұрын
5
@user-si7po9sd5i25 күн бұрын
Great news,I am so happy you have made an excellent decision
Well done akweni may the almighty God continue to protect you❤❤❤❤❤❤❤❤
@constancemkandawire737825 күн бұрын
Very good akweni mmakwana, will be waiting from you.May God go before us (UTM)
@louismagongwa25 күн бұрын
mwaitha akwenei mukakamila za tonse allince mutha nose psiti
@InnocentEdasi25 күн бұрын
Yehova alemekezake.., Mzimu wa Chilima use mumtendele❤❤❤
@alomuddin880124 күн бұрын
A utm mwaganinza bwino 👍👍👍👍 osadya pamodzi ndi fiti ayi
@user-dm2fs6hf1b25 күн бұрын
Well done my sister they is no way to keep on going with these monsters, we the followers shall never give up. UTM wozaaaa munya achule a mcp zombalangondo inu.
@isaacchagwa291725 күн бұрын
Hono. kaliat you lead this political party,for its survival
@augustMag25 күн бұрын
Mau amphamvu Mai Kaliati UTM meayitha🔥🔥🔥🔥💪💪♥️♥️
@TressLuka25 күн бұрын
Khaaaa UTM kuti buuuu. Wafwaaaa Chakweraaaa !
@user-be5fc3ed1i24 күн бұрын
Kkkkk wafwa chakwera mbuzi ya mnthu
@MirriamKambale25 күн бұрын
ULemu wanu akweni osabwelera mbuyo pa tsogolo ndi Utm keep keeping the SKC manefesto and try hard kukwanilitsa mzimu wa SKC uzausa mumtendere.
@marryphili541925 күн бұрын
Well done my people wina apenga misara Chaka chake chino
@HarryYottam-ft1bo25 күн бұрын
Keep it up ndazikonda koma ndipemphe nawo Kwa akulu akulu a utm kuti mukamayamba convention, don't forget miyambi mizu yathu inamera pamenepo please
@user-ks3uw8gj8h25 күн бұрын
2025 am going home only to vote for UTM well done guys hope our President Is smiling for the great decision which has been made🎉🎉🎉🎉🎉
@John-to8gl24 күн бұрын
That is what i was waiting to hear from you guys I wish the team all the best and keep going forward 🙏
Mwachita bwino well done UTM Members Akweni umunthu mulinawo ❤timakukondani
@SamsonChafulumira-mv7og24 күн бұрын
Chikangawa watsala ekha well done mama
@peternashyo985025 күн бұрын
Great and wise decision, Viva UTM.
@nafejonga97224 күн бұрын
UTM FOR REAL😂😂❤❤❤ VAZE VAZE WOYEEE😅😅😅
@dicksonndire185725 күн бұрын
God should be with the family of UTM,
@BlessingsGondwe-v9u25 күн бұрын
Koma kumeneko,,, 🥳🥳🥳🥳🥳 mwat wina satsegula mmimba kuseli,, go UTM go my vote 🔥🔥🔥🔥🔥
@VungaQueen24 күн бұрын
🔥🔥🔥tili pa mbuyo Panu a utm 🔥🔥
@Mwizaso24 күн бұрын
I've been waiting for this speech yooo🥳🥳🥳 the best decision ever 🥳🥳🥳🔥UTM Boma🥳🥳
@MariaNkhata-i9q25 күн бұрын
Weldone mama that's a very good movie ❤
@wizyrastah25 күн бұрын
Tatuluka tatuluka anena anena basi
@RobertLuka-wy9cl25 күн бұрын
Mwachita bwino akweni mwasiye agalu wokuphawo mbuzi za anthu
@OscarMkandawire-g1z25 күн бұрын
Watching live from Mkwapasi Mbizi- St Augustine Mzuzu
@OsmanBakali-s5x25 күн бұрын
Kuzangoti khaaa🔥🔥 akasake ena oti awapatse .... Time over rise up Malawi
@faustascjfronha3425 күн бұрын
Zikomo kwambiri UTM mupitireze ntchito za SKC
@PatrickSomanje24 күн бұрын
U ar strong woman keep up mah don't afraid God will be with u akufuna moyo wanu ayamba ndiyeyo poti anazolowela kupha koma pano pokha tikumuwona ife aa
@GeorgeLipengaphiri25 күн бұрын
Akweni timakunyadilani keep it up vote yanu ilipo basi
@ErnestChansa24 күн бұрын
Big point may kaliati ife ma sapota a UTM tizasangalala mugwilizano uthe basi ndi MCP plz ife tizava kukoma
@MercyChimaliro-fi6mv24 күн бұрын
We are here for UTM. Let's gather here
@BrianJoe-z7u25 күн бұрын
Ndakondwa kwabasi
@FatimanickisJaffer25 күн бұрын
Mulungu akutsogolereni a utm akumenyeren nkhondo pamaganiz anu abwin✅❤️❤️❤️❤️❤️❤️🎉🎉🎉🎉
@ViserKabango-jt1hs24 күн бұрын
Moreeee fireeee,go forward akweni, together we stand
Migwirizano ikumapha tizipani ting'ono ting'ono.Mukaona kuti simungapambane imani mwanokha ndi cholinga chakuti mupeze ma MP. Chipani chimalimba ndi ma MP ku parliament. Ndi 50+1 adzakufunani nthawi imeneyo
@Lemankais24 күн бұрын
Osaonetsa kufooka... keep going! Gud ting take time
@dalitson355824 күн бұрын
Akweni must be tsogoleri wa utm because she’s very clever
@margretsandey25 күн бұрын
Nkhaaaaa akwene mwabweratu mwa coming, my vote
@WilliamKude-oj4mi25 күн бұрын
Tilinanu lomodzi mama more fire 🔥 🔥 🔥 🔥 🔥 🔥 you open gate please
@OmexAkim-ww9nd25 күн бұрын
Mumakwana inuyo Mesa
@Shelifibraheem22 күн бұрын
Apo ndiye mwapitadadi ngati going muli boh
@SaidyKamala-jj7lo25 күн бұрын
Yaaaaaaa bola pamenepo mama uvota kulipo guys shuwaka never give up
@peterchikwakwa847625 күн бұрын
Amen 🙏, mwazunzika enough
@JoshuaMkandawile24 күн бұрын
Very good news a Malawi 😊
@JeanBanda-zy6wu25 күн бұрын
Well done uku ndiye kubwela
@rashidadan253325 күн бұрын
Mmmh mau amai kaliyati sakundipatsa chilimbikiso , pali china chake chikubisidwa , but it's ok let's look the way forward . But remember l'am not politician .
Mwachita bwino kutuluka, koma ndikuuzeni kut musamachite kudikira kut pafe munthu kaye then nkumapanga chiganizo. Koma mukanatuluka nthawi yomwe Chilima anali moyo chikanavuta ndichani??? Padakafunda padadyiwitsa galu. I hope a lesson has been drawn.
@user-pv9uk6sc3w25 күн бұрын
100% !, ndiye apa mupabge alliance ndi DPP, AFORD ndi UDF, basi mwamutha Chakwera ndi boma lake la MCP. Watizunza mokwana.