It's 2024 let's gather here and listen to this and like this
@victoriazomba16746 ай бұрын
pephelo bale uyu wapita kumene ndi week sinathe tionetseni apanga za school za agriculture tionetseni alimi anapita kalekalerewo kuti akukhala motani mutionetse atha miyeziyo ali kudimba tione kuti agwilako bwanji agwila nthawi yaitali bwanji komaso palizabwino pamankhala zovuta tione kuti muwafuse kuti akumana ndi mavuto aji tifuna tione komaso muyankhulane ndi anapita kalekalewo
@IsaacMwale-hu9kgАй бұрын
I wish i could go there Israel
@atholechiwala99976 ай бұрын
Phawafu. .. work hard and represent us...
@wangachindeya85776 ай бұрын
For what? Zachisoni
@JasonNdaba-zs7rm6 ай бұрын
Zikomo guys ndikubwera next trip tidzakupedzan proud ov u guys
@mphatsochitimbe22056 ай бұрын
This is amazing,,,,May God Guide and protect you, inuyu ndima millionaire basi olo ena afune asafune inuyo mwaiphula basi
@petersekani98086 ай бұрын
Awesome guys..tasilila oneday hope will meet there
@user-eg8wx8oi5z6 ай бұрын
i personally know this guy is my nebour
@daisykay6886 ай бұрын
Can't wait for my turn,all the best koma anzathu
@user-gs7wc3nx3q2 ай бұрын
Atumidwa.kumene awa ninaonapo nyuzi ina anawaonesa amalawi akuvutika.anathawa kumunda kumakagwira chito kumashop anawamanga.aporice zanuizo mukuvutika inu guyz uko
@enockdickson41826 ай бұрын
God bless you guys, and protect as well
@MichaelChisambi5 ай бұрын
God first ;party less and invest more at home!we are proud of you!
@user-rg4du4vu9r6 ай бұрын
Munthu ngovuta moyo uno kumapanga chomwe wachiwona kt kwaiwe miriphindu ukayendera zot akut chani utuwa vuto ndirot enewo akungoziwa kunyoza km kuthandiza munthu sangathe god bress you guys
@EditahLaundan4 ай бұрын
My dream 😊
@user-mv8mc6tz1s6 ай бұрын
Muauzeso kt katundu amupezayo amusamale kt azawoso azagwiritseko ntchito vuto la Malawi uve,kuononga careless, chonde let's take care tisamachite kudzionetsera kt tazionera kukulu 🤩
@Tabie80215 ай бұрын
Koma Ka clean kakufunika pang' Ono coz eeeh.i can see the house is beautiful but kaumve kalipo ndithu.
@edfrenkampala73425 ай бұрын
100%true take care and be smart
@user-qw4pk7wj8i6 ай бұрын
Zonamaz guys uyu asakunamize uyuuu watotumidwa zaboza ask me
@CollessTambala6 ай бұрын
No akunena zowona Israel is well advanced in everything
@user-gs7wc3nx3q2 ай бұрын
Kkkkkķk koma braz mumarandira zingati ku joz kuno 100.000 😂😂😂 ine nimarandira 200 000 kuno ku joz.
@user-tu7sh3ss2f6 ай бұрын
Nice stay.. missing guys
@nicksonjohnjumbe83826 ай бұрын
Nafenso ku jonz tikunjoyanso tinabwelanso tokha sizotengedwa ngati ukapolo. Big thanks to you guys I wish you well
@alickkachepa38016 ай бұрын
Kuypatsa moto paja 🤣🤣
@JeremiahPaulNgalawah6 ай бұрын
Kamtima aka sakangakupindulisen
@JusticeBornNdhlamini-fp7ic5 ай бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@user-kw7wr4kq9w5 ай бұрын
Stop undermining Malawi my buitiful land ❤
@user-wp2yp3vh6b6 ай бұрын
Good news
@user-oe5kj6rb5b5 ай бұрын
Nice
@preciousdiyere92846 ай бұрын
Nice one lsee
@AmosMarkko-fp6pg6 ай бұрын
Chipe voice eeeee ! Loud en clear koma Boyz
@godfreylungu6 ай бұрын
Ndikuona kuchedwa ambuye nditsogoleleni visa yanga ituluke
@estoniamoffat86336 ай бұрын
Zitheka osadandaula..we all want to go koma ndikuona kuti government likuchedwesa ngini
@masterchitabwino8984 ай бұрын
Mwayamba kunyozatu mmm khalani ndi khalidwe
@amabhohlela.34926 ай бұрын
5yrs..azikazanu akukudikilani
@Fortu_neDrSabba6 ай бұрын
Kodi a Manzy muliso ku Israel?
@josephchitsulo58826 ай бұрын
Akapolo inu, munagwidwa ukapolo ku Malawi kuja kunkananu kumeneko, malipilo anu simukuwaziwa, izingolilani ndi mtima
@macdonaldchimodzi27916 ай бұрын
Ukapolo wawo nde ma million nde akulowatu inu muli busy kuwanena apa🤣🤣
@josephchitsulo58826 ай бұрын
@@macdonaldchimodzi2791 life is very tough kumeneko Sir about expenses, kwa anthu osaziwa amangoti nza boh boh, i've been in Dubai very rich country but eee! Bolanso konkuno ku zinafibia kuno
@KunyengaMoyo5 ай бұрын
Ndye akubitsa dzina why??? 😂😂😂
@user-xm4pz5hu5r6 ай бұрын
Powerful 🎉🎉
@faithkamlongera51286 ай бұрын
Great
@RhudesMaliro2 ай бұрын
Process yake ikumayenda motani?
@user-rc2wo9bm9w6 ай бұрын
Power of chimidzi
@grantgphiri70856 ай бұрын
Ndiye kukungo woneka ngati kuyudeyatu 🤸🤸🤸
@PhilliphofenKuwanje-fs5wy6 ай бұрын
Nice ,,,,
@RuthNyemba-kc3pzАй бұрын
kuli chaniso uku chimene ndaona ine
@elizabethsokoe26356 ай бұрын
Muzilyala ma bed oyaa!!! Inu ife tili ndima iconso kuno ku jozi and with remote control
@user-rn9cd3be6k6 ай бұрын
Nanga mowa simumwako ma weekend 😂😂😂
@GodInks5 ай бұрын
Bafrep my guy..!
@user-um6dy1kr8t6 ай бұрын
What about the laptops, anawagulilaso ?
@DungaNya6 ай бұрын
Makape inu ntchito yosafuna kujombayo
@victoriazomba16746 ай бұрын
wish u well my pipo
@user-cb2cv9fz7m6 ай бұрын
3'2 million Koma rent ,kudya zaziii,mukumakhala ndi ka change , things there very expensive there mabobo abwino guys
@josephychikaonda67016 ай бұрын
Not bad...
@BLESSINGSPEARSON6 ай бұрын
Ok
@ConfusedAtv-bs4gc6 ай бұрын
Ndimufunseko ameneyu ndinzanga Koma Moyo wake Mene amakhalila ndimene amazifilila zoti angakagwile ntchito kumunda munthu sungamvese kwanu Kuno iwe umati sungakalime chifukwa kwanu kuli antchito lelo ukuti ukunyoya nditchito yomwe umati kwanukuno sungagwile waliwona dZiko line limakhalila
@Fortu_neDrSabba6 ай бұрын
We hustle were there is Money bro. Fvxk
@BlessingsGoma-zc4rl6 ай бұрын
Boys are enjoying
@nego50056 ай бұрын
Si onse akukhala kumalo abho
@zabulirani6 ай бұрын
This is fake
@mphatsochitimbe22056 ай бұрын
Mukunama ankolo you don't know israel
@ChamalizikaJoseph-ph1sr6 ай бұрын
aliyese akujoya sayiz yake ndi Malo ake
@rashidadan25336 ай бұрын
Madolowo alibo
@user-tb6yh1kx3o6 ай бұрын
In S A Malawians are living good life more than that😂😂😂😂
@mphatsochitimbe22056 ай бұрын
Bro israel osamaiphweketsa
@mussabizymaunde19956 ай бұрын
Osatchula dzina for his own safety koma munthu nkhope ikuoneka??? What kind of drama is that
@grantgphiri70856 ай бұрын
If possible tango ndi jambulirako nyumba ya uja adakwatila akazi 700 and 300 hundred girlfriend 😅
@user-nu1dj3jh7b6 ай бұрын
Inu muli ku paladaizo sizakuno ku south africa aaa nkhanza zokhazokha
@grantgphiri70856 ай бұрын
Ku Israel ndi mpesa okha okha Kulibe okudya nkhumba uko 🤣🤣
@JustinLPhiri6 ай бұрын
Nafeso tikunjoya kuno Ku joz ndalama zilikuno ndikulandila R10,000 per month
@user-xy4hq6sx7v6 ай бұрын
Vuto lomwe ndinalipeza kwa ifeyo a malawi timangotchulako zabwino zokha zokha mwachitsanzo kunokonso ku joni kuli zokhoma komanso kuli zabwino kuli ena akuvutika ukuku moti awawa angowatukwanapo
@simphiwechakana63375 ай бұрын
Mwatilimbikitsa
@chiccochimwaza47916 ай бұрын
Thanks for the video, I think anthu okamba mbwelera awonere this video , anthu amayankhulisa zosakhala bwino
@JeremiahPaulNgalawah6 ай бұрын
Sangayankhule or kupanga forward kut tionere ambiri amazilowesa ndale
@zabulirani6 ай бұрын
This is fake and akufuna kupusitsa anthu Let me tell you anthuwa akukhala bwino but kuli mavuto Let me send you text ya one of my friend mpaka pano foni yake sipezekaso
@johnsonminandi14106 ай бұрын
Ena zachilendo mix furij kuziwira ku izilayero zodabwino kwa inu
@user-sp8ql2st5u6 ай бұрын
Kunotso ku joni tikunjoya dzimangotingela ndi kt ndiwe otan
@wabitha97696 ай бұрын
Auze zoonad 🎉
@RabsonPhiri-og5je6 ай бұрын
. Zabwino kwambiri ambuye Jesus alemekezeke
@user-nb8wg3fh4u6 ай бұрын
Munagwidwa ukapolo ndi chakwela pa jozi anthu akuwufila
@NoelKaferawanthu6 ай бұрын
Uku nane ndipiteko ndithu
@PeterGabriel-uh2lh5 ай бұрын
how can be there be safety pomwe nkhope tikuiwona direct
@Isaactembo11116 ай бұрын
See you there
@mafukenimasangwi54876 ай бұрын
Azisilila amene sanayende osati ine nafenso tikunjoya pa RSA pompano
@mphatsochitimbe22056 ай бұрын
Sizampikisano ankolo tonse ndizongosaka ndalama basi
@mafukenimasangwi54876 ай бұрын
@@mphatsochitimbe2205 kumva ndi kumvetsesa ndi zosiyana
@PempheroTomasi5 ай бұрын
Zonsangatsakwambiro
@user-dn5sf3md5t5 ай бұрын
This is politics, awa achita kutumidwa palibe akunjoyako uku guys ineyo mzanga akukhalira kidandaula komweko kuti ndikanaziwa sindikanabwerayi , bodza ili awa atumidwa
@linneausmsiska11845 ай бұрын
You find maybe the signed NDA not to say what really happens
@LesterChiwayula6 ай бұрын
Achina Bally aku 24 muli yudeya kodi
@amabhohlela.34926 ай бұрын
ALIMI,,osamatiputsisapo apa!!kuti musangalara hahahahahahaha!!!munama inu..timadobadoba mufuna kuti mtima udzitiwawa!!!akulandani ma Passport inu,,,show us ur Passport.
@samiljames57196 ай бұрын
Tipatseni link yobwera kumeneko
@lusungubanda82806 ай бұрын
Ati sinditchula dzina koma nkhope taiona aaaaahhh
@HopesonJailosi-vd6ou6 ай бұрын
Nkhani ndi ndalama akumalandira anthuwo asiya mabanja Kuno mabanjawo akuthandizidwa?
@petermagwira55836 ай бұрын
Am single 🥴
@mcfersonmasingi14186 ай бұрын
Zabodza
@garrynsikula45726 ай бұрын
Show us kumunda
@Adzukulu6 ай бұрын
Wul arrange
@victorbanda90396 ай бұрын
Chakwera mpaka 2030
@user-cr3yw3pe1e6 ай бұрын
Zabwino zonse maguyeee. The only thing malawias are full of jealous & envy . Tizifunirana zabwino osati kunyozana
@danielproro27796 ай бұрын
Fred barley
@JaneMoyo-ws2di6 ай бұрын
Akupanga za chani actually?
@user-nb8wg3fh4u6 ай бұрын
Go tu interview those they are working in the farm not this fake information
@user-iy7oh7hf4s6 ай бұрын
tsiku lopuma limodzi pa week, mbola.
@connexchifundo80266 ай бұрын
Midzingolankhula chichewa
@patrickkphiri42376 ай бұрын
Zamphamvu
@user-gk5ok6xp7w5 ай бұрын
KOD mwana wa aballe
@user-lr5bz7qk2d6 ай бұрын
Kapolo Inu
@KhadidyaRichard-jq5td6 ай бұрын
Hybo
@user-bi8vn7lb4b6 ай бұрын
Zaboza basi azanu akutika zoona
@user-ty1vq9lq6w6 ай бұрын
Tionetseni komwe kukukhala alimi
@user-ij9jg7cm7x6 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂God have mercy on you guys where is the ather people who went there for the first time and why you don't even show us where they are working why this is absolutely wrong and abomination