No video

Zaululika Zomwe Zikuchitika Ku Israel - Chilungamo Chenicheni Cha zomwe AMALAWI apezaa ku Israel

  Рет қаралды 56,192

Adzukulu

Adzukulu

Күн бұрын

#adzukulu #malawi #trending #viral

Пікірлер: 136
@Sunnygw260
@Sunnygw260 6 ай бұрын
It's 2024 let's gather here and listen to this and like this
@victoriazomba1674
@victoriazomba1674 6 ай бұрын
pephelo bale uyu wapita kumene ndi week sinathe tionetseni apanga za school za agriculture tionetseni alimi anapita kalekalerewo kuti akukhala motani mutionetse atha miyeziyo ali kudimba tione kuti agwilako bwanji agwila nthawi yaitali bwanji komaso palizabwino pamankhala zovuta tione kuti muwafuse kuti akumana ndi mavuto aji tifuna tione komaso muyankhulane ndi anapita kalekalewo
@IsaacMwale-hu9kg
@IsaacMwale-hu9kg Ай бұрын
I wish i could go there Israel
@atholechiwala9997
@atholechiwala9997 6 ай бұрын
Phawafu. .. work hard and represent us...
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 6 ай бұрын
For what? Zachisoni
@JasonNdaba-zs7rm
@JasonNdaba-zs7rm 6 ай бұрын
Zikomo guys ndikubwera next trip tidzakupedzan proud ov u guys
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
This is amazing,,,,May God Guide and protect you, inuyu ndima millionaire basi olo ena afune asafune inuyo mwaiphula basi
@petersekani9808
@petersekani9808 6 ай бұрын
Awesome guys..tasilila oneday hope will meet there
@user-eg8wx8oi5z
@user-eg8wx8oi5z 6 ай бұрын
i personally know this guy is my nebour
@daisykay688
@daisykay688 6 ай бұрын
Can't wait for my turn,all the best koma anzathu
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q 2 ай бұрын
Atumidwa.kumene awa ninaonapo nyuzi ina anawaonesa amalawi akuvutika.anathawa kumunda kumakagwira chito kumashop anawamanga.aporice zanuizo mukuvutika inu guyz uko
@enockdickson4182
@enockdickson4182 6 ай бұрын
God bless you guys, and protect as well
@MichaelChisambi
@MichaelChisambi 5 ай бұрын
God first ;party less and invest more at home!we are proud of you!
@user-rg4du4vu9r
@user-rg4du4vu9r 6 ай бұрын
Munthu ngovuta moyo uno kumapanga chomwe wachiwona kt kwaiwe miriphindu ukayendera zot akut chani utuwa vuto ndirot enewo akungoziwa kunyoza km kuthandiza munthu sangathe god bress you guys
@EditahLaundan
@EditahLaundan 4 ай бұрын
My dream 😊
@user-mv8mc6tz1s
@user-mv8mc6tz1s 6 ай бұрын
Muauzeso kt katundu amupezayo amusamale kt azawoso azagwiritseko ntchito vuto la Malawi uve,kuononga careless, chonde let's take care tisamachite kudzionetsera kt tazionera kukulu 🤩
@Tabie8021
@Tabie8021 5 ай бұрын
Koma Ka clean kakufunika pang' Ono coz eeeh.i can see the house is beautiful but kaumve kalipo ndithu.
@edfrenkampala7342
@edfrenkampala7342 5 ай бұрын
100%true take care and be smart
@user-qw4pk7wj8i
@user-qw4pk7wj8i 6 ай бұрын
Zonamaz guys uyu asakunamize uyuuu watotumidwa zaboza ask me
@CollessTambala
@CollessTambala 6 ай бұрын
No akunena zowona Israel is well advanced in everything
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q 2 ай бұрын
Kkkkkķk koma braz mumarandira zingati ku joz kuno 100.000 😂😂😂 ine nimarandira 200 000 kuno ku joz.
@user-tu7sh3ss2f
@user-tu7sh3ss2f 6 ай бұрын
Nice stay.. missing guys
@nicksonjohnjumbe8382
@nicksonjohnjumbe8382 6 ай бұрын
Nafenso ku jonz tikunjoyanso tinabwelanso tokha sizotengedwa ngati ukapolo. Big thanks to you guys I wish you well
@alickkachepa3801
@alickkachepa3801 6 ай бұрын
Kuypatsa moto paja 🤣🤣
@JeremiahPaulNgalawah
@JeremiahPaulNgalawah 6 ай бұрын
Kamtima aka sakangakupindulisen
@JusticeBornNdhlamini-fp7ic
@JusticeBornNdhlamini-fp7ic 5 ай бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@user-kw7wr4kq9w
@user-kw7wr4kq9w 5 ай бұрын
Stop undermining Malawi my buitiful land ❤
@user-wp2yp3vh6b
@user-wp2yp3vh6b 6 ай бұрын
Good news
@user-oe5kj6rb5b
@user-oe5kj6rb5b 5 ай бұрын
Nice
@preciousdiyere9284
@preciousdiyere9284 6 ай бұрын
Nice one lsee
@AmosMarkko-fp6pg
@AmosMarkko-fp6pg 6 ай бұрын
Chipe voice eeeee ! Loud en clear koma Boyz
@godfreylungu
@godfreylungu 6 ай бұрын
Ndikuona kuchedwa ambuye nditsogoleleni visa yanga ituluke
@estoniamoffat8633
@estoniamoffat8633 6 ай бұрын
Zitheka osadandaula..we all want to go koma ndikuona kuti government likuchedwesa ngini
@masterchitabwino898
@masterchitabwino898 4 ай бұрын
Mwayamba kunyozatu mmm khalani ndi khalidwe
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 ай бұрын
5yrs..azikazanu akukudikilani
@Fortu_neDrSabba
@Fortu_neDrSabba 6 ай бұрын
Kodi a Manzy muliso ku Israel?
@josephchitsulo5882
@josephchitsulo5882 6 ай бұрын
Akapolo inu, munagwidwa ukapolo ku Malawi kuja kunkananu kumeneko, malipilo anu simukuwaziwa, izingolilani ndi mtima
@macdonaldchimodzi2791
@macdonaldchimodzi2791 6 ай бұрын
Ukapolo wawo nde ma million nde akulowatu inu muli busy kuwanena apa🤣🤣
@josephchitsulo5882
@josephchitsulo5882 6 ай бұрын
@@macdonaldchimodzi2791 life is very tough kumeneko Sir about expenses, kwa anthu osaziwa amangoti nza boh boh, i've been in Dubai very rich country but eee! Bolanso konkuno ku zinafibia kuno
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo 5 ай бұрын
Ndye akubitsa dzina why??? 😂😂😂
@user-xm4pz5hu5r
@user-xm4pz5hu5r 6 ай бұрын
Powerful 🎉🎉
@faithkamlongera5128
@faithkamlongera5128 6 ай бұрын
Great
@RhudesMaliro
@RhudesMaliro 2 ай бұрын
Process yake ikumayenda motani?
@user-rc2wo9bm9w
@user-rc2wo9bm9w 6 ай бұрын
Power of chimidzi
@grantgphiri7085
@grantgphiri7085 6 ай бұрын
Ndiye kukungo woneka ngati kuyudeyatu 🤸🤸🤸
@PhilliphofenKuwanje-fs5wy
@PhilliphofenKuwanje-fs5wy 6 ай бұрын
Nice ,,,,
@RuthNyemba-kc3pz
@RuthNyemba-kc3pz Ай бұрын
kuli chaniso uku chimene ndaona ine
@elizabethsokoe2635
@elizabethsokoe2635 6 ай бұрын
Muzilyala ma bed oyaa!!! Inu ife tili ndima iconso kuno ku jozi and with remote control
@user-rn9cd3be6k
@user-rn9cd3be6k 6 ай бұрын
Nanga mowa simumwako ma weekend 😂😂😂
@GodInks
@GodInks 5 ай бұрын
Bafrep my guy..!
@user-um6dy1kr8t
@user-um6dy1kr8t 6 ай бұрын
What about the laptops, anawagulilaso ?
@DungaNya
@DungaNya 6 ай бұрын
Makape inu ntchito yosafuna kujombayo
@victoriazomba1674
@victoriazomba1674 6 ай бұрын
wish u well my pipo
@user-cb2cv9fz7m
@user-cb2cv9fz7m 6 ай бұрын
3'2 million Koma rent ,kudya zaziii,mukumakhala ndi ka change , things there very expensive there mabobo abwino guys
@josephychikaonda6701
@josephychikaonda6701 6 ай бұрын
Not bad...
@BLESSINGSPEARSON
@BLESSINGSPEARSON 6 ай бұрын
Ok
@ConfusedAtv-bs4gc
@ConfusedAtv-bs4gc 6 ай бұрын
Ndimufunseko ameneyu ndinzanga Koma Moyo wake Mene amakhalila ndimene amazifilila zoti angakagwile ntchito kumunda munthu sungamvese kwanu Kuno iwe umati sungakalime chifukwa kwanu kuli antchito lelo ukuti ukunyoya nditchito yomwe umati kwanukuno sungagwile waliwona dZiko line limakhalila
@Fortu_neDrSabba
@Fortu_neDrSabba 6 ай бұрын
We hustle were there is Money bro. Fvxk
@BlessingsGoma-zc4rl
@BlessingsGoma-zc4rl 6 ай бұрын
Boys are enjoying
@nego5005
@nego5005 6 ай бұрын
Si onse akukhala kumalo abho
@zabulirani
@zabulirani 6 ай бұрын
This is fake
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
Mukunama ankolo you don't know israel
@ChamalizikaJoseph-ph1sr
@ChamalizikaJoseph-ph1sr 6 ай бұрын
aliyese akujoya sayiz yake ndi Malo ake
@rashidadan2533
@rashidadan2533 6 ай бұрын
Madolowo alibo
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o 6 ай бұрын
In S A Malawians are living good life more than that😂😂😂😂
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
Bro israel osamaiphweketsa
@mussabizymaunde1995
@mussabizymaunde1995 6 ай бұрын
Osatchula dzina for his own safety koma munthu nkhope ikuoneka??? What kind of drama is that
@grantgphiri7085
@grantgphiri7085 6 ай бұрын
If possible tango ndi jambulirako nyumba ya uja adakwatila akazi 700 and 300 hundred girlfriend 😅
@user-nu1dj3jh7b
@user-nu1dj3jh7b 6 ай бұрын
Inu muli ku paladaizo sizakuno ku south africa aaa nkhanza zokhazokha
@grantgphiri7085
@grantgphiri7085 6 ай бұрын
Ku Israel ndi mpesa okha okha Kulibe okudya nkhumba uko 🤣🤣
@JustinLPhiri
@JustinLPhiri 6 ай бұрын
Nafeso tikunjoya kuno Ku joz ndalama zilikuno ndikulandila R10,000 per month
@user-xy4hq6sx7v
@user-xy4hq6sx7v 6 ай бұрын
Vuto lomwe ndinalipeza kwa ifeyo a malawi timangotchulako zabwino zokha zokha mwachitsanzo kunokonso ku joni kuli zokhoma komanso kuli zabwino kuli ena akuvutika ukuku moti awawa angowatukwanapo
@simphiwechakana6337
@simphiwechakana6337 5 ай бұрын
Mwatilimbikitsa
@chiccochimwaza4791
@chiccochimwaza4791 6 ай бұрын
Thanks for the video, I think anthu okamba mbwelera awonere this video , anthu amayankhulisa zosakhala bwino
@JeremiahPaulNgalawah
@JeremiahPaulNgalawah 6 ай бұрын
Sangayankhule or kupanga forward kut tionere ambiri amazilowesa ndale
@zabulirani
@zabulirani 6 ай бұрын
This is fake and akufuna kupusitsa anthu Let me tell you anthuwa akukhala bwino but kuli mavuto Let me send you text ya one of my friend mpaka pano foni yake sipezekaso
@johnsonminandi1410
@johnsonminandi1410 6 ай бұрын
Ena zachilendo mix furij kuziwira ku izilayero zodabwino kwa inu
@user-sp8ql2st5u
@user-sp8ql2st5u 6 ай бұрын
Kunotso ku joni tikunjoya dzimangotingela ndi kt ndiwe otan
@wabitha9769
@wabitha9769 6 ай бұрын
Auze zoonad 🎉
@RabsonPhiri-og5je
@RabsonPhiri-og5je 6 ай бұрын
. Zabwino kwambiri ambuye Jesus alemekezeke
@user-nb8wg3fh4u
@user-nb8wg3fh4u 6 ай бұрын
Munagwidwa ukapolo ndi chakwela pa jozi anthu akuwufila
@NoelKaferawanthu
@NoelKaferawanthu 6 ай бұрын
Uku nane ndipiteko ndithu
@PeterGabriel-uh2lh
@PeterGabriel-uh2lh 5 ай бұрын
how can be there be safety pomwe nkhope tikuiwona direct
@Isaactembo1111
@Isaactembo1111 6 ай бұрын
See you there
@mafukenimasangwi5487
@mafukenimasangwi5487 6 ай бұрын
Azisilila amene sanayende osati ine nafenso tikunjoya pa RSA pompano
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
Sizampikisano ankolo tonse ndizongosaka ndalama basi
@mafukenimasangwi5487
@mafukenimasangwi5487 6 ай бұрын
@@mphatsochitimbe2205 kumva ndi kumvetsesa ndi zosiyana
@PempheroTomasi
@PempheroTomasi 5 ай бұрын
Zonsangatsakwambiro
@user-dn5sf3md5t
@user-dn5sf3md5t 5 ай бұрын
This is politics, awa achita kutumidwa palibe akunjoyako uku guys ineyo mzanga akukhalira kidandaula komweko kuti ndikanaziwa sindikanabwerayi , bodza ili awa atumidwa
@linneausmsiska1184
@linneausmsiska1184 5 ай бұрын
You find maybe the signed NDA not to say what really happens
@LesterChiwayula
@LesterChiwayula 6 ай бұрын
Achina Bally aku 24 muli yudeya kodi
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 ай бұрын
ALIMI,,osamatiputsisapo apa!!kuti musangalara hahahahahahaha!!!munama inu..timadobadoba mufuna kuti mtima udzitiwawa!!!akulandani ma Passport inu,,,show us ur Passport.
@samiljames5719
@samiljames5719 6 ай бұрын
Tipatseni link yobwera kumeneko
@lusungubanda8280
@lusungubanda8280 6 ай бұрын
Ati sinditchula dzina koma nkhope taiona aaaaahhh
@HopesonJailosi-vd6ou
@HopesonJailosi-vd6ou 6 ай бұрын
Nkhani ndi ndalama akumalandira anthuwo asiya mabanja Kuno mabanjawo akuthandizidwa?
@petermagwira5583
@petermagwira5583 6 ай бұрын
Am single 🥴
@mcfersonmasingi1418
@mcfersonmasingi1418 6 ай бұрын
Zabodza
@garrynsikula4572
@garrynsikula4572 6 ай бұрын
Show us kumunda
@Adzukulu
@Adzukulu 6 ай бұрын
Wul arrange
@victorbanda9039
@victorbanda9039 6 ай бұрын
Chakwera mpaka 2030
@user-cr3yw3pe1e
@user-cr3yw3pe1e 6 ай бұрын
Zabwino zonse maguyeee. The only thing malawias are full of jealous & envy . Tizifunirana zabwino osati kunyozana
@danielproro2779
@danielproro2779 6 ай бұрын
Fred barley
@JaneMoyo-ws2di
@JaneMoyo-ws2di 6 ай бұрын
Akupanga za chani actually?
@user-nb8wg3fh4u
@user-nb8wg3fh4u 6 ай бұрын
Go tu interview those they are working in the farm not this fake information
@user-iy7oh7hf4s
@user-iy7oh7hf4s 6 ай бұрын
tsiku lopuma limodzi pa week, mbola.
@connexchifundo8026
@connexchifundo8026 6 ай бұрын
Midzingolankhula chichewa
@patrickkphiri4237
@patrickkphiri4237 6 ай бұрын
Zamphamvu
@user-gk5ok6xp7w
@user-gk5ok6xp7w 5 ай бұрын
KOD mwana wa aballe
@user-lr5bz7qk2d
@user-lr5bz7qk2d 6 ай бұрын
Kapolo Inu
@KhadidyaRichard-jq5td
@KhadidyaRichard-jq5td 6 ай бұрын
Hybo
@user-bi8vn7lb4b
@user-bi8vn7lb4b 6 ай бұрын
Zaboza basi azanu akutika zoona
@user-ty1vq9lq6w
@user-ty1vq9lq6w 6 ай бұрын
Tionetseni komwe kukukhala alimi
@user-ij9jg7cm7x
@user-ij9jg7cm7x 6 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂God have mercy on you guys where is the ather people who went there for the first time and why you don't even show us where they are working why this is absolutely wrong and abomination
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
Bro akiyankhulatu chichewa anthuwo tiziti simukunva zomwe akunena
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 6 ай бұрын
Mutichititsa manyazituuu guys muchita kuonekatu kut mukuzionera komwekotu vuto lakeso mukumayankhula chizungusotu mmalo momagoyankhula zanuzo
@Fortu_neDrSabba
@Fortu_neDrSabba 6 ай бұрын
Ikani DP yanzeru then munyoze
@collennyadile8179
@collennyadile8179 6 ай бұрын
zoziwonela ku ukulu zovuta
@user-md5uv2cg6i
@user-md5uv2cg6i 6 ай бұрын
Chokani machende anu mwalembedwa ntchito ndi a mcp mwapwala anu
@user-mq1mb4lk3m
@user-mq1mb4lk3m 6 ай бұрын
Zamphavu
@user-om4jo7cx8c
@user-om4jo7cx8c 6 ай бұрын
😢
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 6 ай бұрын
Simunangonemo metse mwambamo mubwele ku south Africa muza Simba zambili I'm from Cape Town
@angelamkandawire7612
@angelamkandawire7612 6 ай бұрын
Zagwilizanaso bwanji South Africa abale ,asiyeni azanu
@atholechiwala9997
@atholechiwala9997 6 ай бұрын
Olo bakha atavina i cant go to KHUVUKILAND 😂😂😂😂 ... South Africa = the slaughter house of Africa
@emmanuelchapwetekabanda1508
@emmanuelchapwetekabanda1508 6 ай бұрын
Sitikupikisana nanu boss. We are all looking for greener pastures. Let's let love to lead!!!
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
The goal is financial freedom not competition,,,,,
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 ай бұрын
Is not citizen..is a foreigner National
@DanielJuly-dj2ji
@DanielJuly-dj2ji 6 ай бұрын
Mindset yomagomera azungu sitingatukuke aMalawi. How special is azungu. Dangote akulemba ntchito azungu 🚮
@mphatsochitimbe2205
@mphatsochitimbe2205 6 ай бұрын
Nsanje yake iyiyi dziko lathu lija kuti litukuke zitivutilapo kwambili
The Giant sleep in the town 👹🛏️🏡
00:24
Construction Site
Рет қаралды 21 МЛН
When you discover a family secret
00:59
im_siowei
Рет қаралды 25 МЛН
Чёрная ДЫРА 🕳️ | WICSUR #shorts
00:49
Бискас
Рет қаралды 6 МЛН
Rev. Alexander Kambiri preaching at the funeral service - Chiwosha- Mchinji
22:06
Rev. Alexander Kambiri
Рет қаралды 306 М.
CRUISE 5 WITH GEORGE KALICHELO - Inventor
52:33
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 20 М.
Tikuferanji 09 March 2024
14:59
Edson Gunsalu
Рет қаралды 61 М.
CRUISE 5 MAFUMU MATIKI
1:14:37
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 145 М.
The Giant sleep in the town 👹🛏️🏡
00:24
Construction Site
Рет қаралды 21 МЛН