Km Chakwera ndi anthu ako mukubweretsa mfundo zopanda Pake, iwe mmene umalowa m'boma ndalama unatenga kut?
@RedeemaKachali16 күн бұрын
Ndipo inu
@GrantYohane-zd4qy16 күн бұрын
Koma boma kagulidwe kake ka chimanga aaa ku admark amafunatu chotsuka. Koma mbewu sabweletsa ya chimanga chimene amafunachi.
@JimmyIsaac-xd4ef16 күн бұрын
😊😊😊😊😊
@FaressPatel16 күн бұрын
Zoopsa kwabasi
@user-ii2sh1mz3r16 күн бұрын
Kodi uni ukuti tili pa ufulu wozilamulira , Koma bwanji nthawi zonse tikudalira chuma kuchokera Ku maiko akunja, economically we are still colonised, politically we are dependent, but full of witchcraft , instead of serving people political leaders are busy shouting at their fellow leaders , akuti ,ine mungandifanizire ndi a Kuti , ine ndi kumtunda , muona uja ndithana naye mmmmm
@mishecksipolo715316 күн бұрын
Iyyeyo chakwerayo ankazitenga kuti?
@Mahamudu-q6b16 күн бұрын
😮😮😮😂😂😂
@Homeofpeace32116 күн бұрын
Chakwela Uchenjele Ndi Nzimu wachilima ndi Ena 8 unawapha aja ndicholinga uimenso 2025, Ndalamazo Zakoma Chotani Zochita Kuphela Nanzo Anzako. Amalawi Munapusa Kwambili Izi zinachita poyela simunapangepo kanthu Only Born Kalindo Amene Amaona Zinthu Ndikuyankhulapo Ena Nonse Zitsilu
@DavidMtambo-zm8ne16 күн бұрын
Ayambe kaye kuulura chakwera panthawwi ya campaign yake ya 2019, stupiet thinking
@EfeloYovita16 күн бұрын
ndalama zomwe amaitanitsaila asilikali aku isalael ndi Rwanda akumazitenga kuti zomwe akumatumiza anyamata kokasaka atolankhani alimpopo fm ndi bakili muluzi tv akuzitenga kuti
@user-nw6ie3xx8b16 күн бұрын
Leave us alone as mcp ask dpp how norman chisale got rich