Tikanakhala ogwilizana amalawife tikanasakha chipani chimodz chomwe chizawine,vuto tikuvutika koma aliyense akukavotera yemwe akumufuna zosatila zake timavote to tinyemedwanyemedwa koma aaaa
@user-le9su3mt7r2 ай бұрын
Chakwela mbava
@DONNEXKhama-bk1gy2 ай бұрын
Akut ine ndi chakwera kut tipikisane ndingawine ndine😂😂😂😂😂😂iiiii kma chakwera Ai ndithu
@NditajiMaxwell-cz8ir2 ай бұрын
Km kunena zoona anthu akuvutika kwambiri zomvesa chisoni kwambiri
@Pangolinimw2 ай бұрын
chakwera mapwala ake alipwisi
@user-ub1vt2kq4s2 ай бұрын
Chakwera must go,chifukwa akuba kwambiri wasaukitsa dziko la Malawi kwambiri
@user-xd1cm7tm7t2 ай бұрын
Chakwera must go no matter what next year
@dontreybanda2782 ай бұрын
Chakwera achoke basi
@YohanePatrick-lc2lq2 ай бұрын
Dpp woyeeeee boma
@samsonhavenoyayshonga26092 ай бұрын
A Malawi tikuvutika chifukwa azitsogoleri ndi akuba.
@YohanePatrick-lc2lq2 ай бұрын
Komasotu dzinadzi ndidzofuna munya muwona
@NgomaRaheem2 ай бұрын
Mapwala ako
@APOSTLEBJ-tc5fp2 ай бұрын
WE NEED REFERENDUM IN MALAWI PLEASE
@UseniMailosi2 ай бұрын
Chakwera ndiorepera
@GeorgeLungu-bt6hf2 ай бұрын
Achoke Palowe ena
@DavidCazembe2 ай бұрын
Kkk 😂😂😂😂
@samdiverson97332 ай бұрын
chatsika koma APM only hope for malawians chakwera out and must go 2025
@YusufuKaifa-fr4wt2 ай бұрын
Nziko la malawi akusangalala anthu Ali ku boma basi koma ntosefe tili kunja kwa anthu a boma .. tikusphya moto ndithu 😭😭😭😭😭😭🥶🥶🥶
@JesterChakalamba2 ай бұрын
Anthu Inu palibe olamulira yemwe azapanga zifuna zanu palibe only Jehovah basi izi or mutalankhula bwanji or mutasintha bwanji muzalira mpaka kale mpaka ufumu wake ubwele basi mwana obadwa Kwa mkazi sangakoze zinthu kulibe
@user-gx5ht9gm3z2 ай бұрын
NO PAIN NO GAIN GO BACK 2 SCHOOL BOY
@ThokohKalonga-je9rx2 ай бұрын
Nanunso simukutha kuwona Zoti Zinthu zidadokonekera? Nthawi ya ulamulilo winauja anthu amapanga blame? president like Mesa kutathaudza Nthawi imeneija zidali bwino than now. Ndi president waumbuliyo
@JesterChakalamba2 ай бұрын
@@ThokohKalonga-je9rx whether you like or not trust me zinthu sisizasinthapo mpaka kale may be your young you don't know where we were ndipo tikupita kuti just do your part kuti udye munthu sangathe mavuto Ako gwilantchito
@AleksaWilliams-qc6cn2 ай бұрын
Kod akuyakhulira kut awawa
@dondamissonchdziwe39582 ай бұрын
Komatu wanthu wenawa NKU tembereredwa, ngati akuvutika Wanthu abwino bwino kuli bwanji wopunduka koma sibwino choncho popeza munamu sankha nokha muzaona chochita ife tatchona kunja kuno kumeneko tina choka Kale Kale
@JesterChakalamba2 ай бұрын
Ndinabadwa mama 70 from 1994 up to now palibe Chaka katundu atsikapo momwe zinthu zinayambila kubwela nthawi ya Bakili sizinasinthepo tamawawuzani zolimbikitsa azigwila ntchito molimbikila osati kudalira munthu n0