Tikutuluka aise zichani wayikazi kungotithela ma bundle basi
@christophermatemba22412 ай бұрын
please hanif tv tazipangani post zinthu za serious osati masanje mwayambawa
@collingskasanga42572 ай бұрын
Akusowa zochita
@user-zl9vj6hc6y2 ай бұрын
Simungamupeze bakili muluzi t v... apolisi asanduka young pioneer
@usumanidaudi2 ай бұрын
Akozeke kt akubwera ku south Africa chifukwa kuno a marawi arikuno ndi okwiya ndi chakwera sikumarawi kuno akusakani anyamata kuno maro mosaka wa bakiri tv anyamata akusakani si ku Lilongwe kuno musamare🎉
@user-ll7fy1gz9m2 ай бұрын
Good one❤🔥
@HenryLaidon-pl9ly2 ай бұрын
Kugwa mmanja mwa MULUNGU NDI NGOZI YAYIKULU. Apa ndizomwe Amalawi Anzanga tazionazi. Agule azipita
@SamKaposa-i5c2 ай бұрын
Exactly
@bokaalfan91462 ай бұрын
Inu mwaika zichani izi police amakhala chochi.
@user-cp7hu6xu8h2 ай бұрын
Zimene tikufuna ku malawi ndi zimeneso osamangogona one loom house Chakwera ndi ana Ake there billionare
@FrankKambwani2 ай бұрын
Phokoso lake limenero munthuyo ndiye sathawa😅😅😅Bakili Muluzi TV is for ever simungamugwire mukhalira kumangoyimba nyimbo dzolawuladzo chomcho kuleka kudzigwira mbava dzenidzeni Chakwera ndi nduna dzake wa😅😅😅😅
@adamusaidih85702 ай бұрын
Malawi ndiziko lotembeleledwa chifukwa cha chakwela
😂😂😂😂😂😂Agalu achakwera Inu nyimbo zake .Palibe chomwe mungapange apa kadyeni chinangwacho chifukwa banziso simungakwanitse ndikasalary kanuko.zaziiii
@princedetbozsmallboy17492 ай бұрын
Koma mbulizi akachoka pamenepa akagula sugar pa 5 000 mbuzi izi
@PatieKates2 ай бұрын
Kkkkkk
@mtumikiJuda2 ай бұрын
Poyamba ndinkakusatira nkayesa umakamba zoona koma ndiwe waboza.... Olo munthu opanda ubongoyo angakanike kudziwa kuti this was just a route match😂😂😂😂 Kamba ina ase.... Kwa amene amadziwa apolisi akumalawi, every Wednesday amakhala ndi afternoon run. Ndi sports day.