The real son of mother Malawi silvester namiwa keep it up brother plz don't give up
@yusufbanda4980Ай бұрын
Lets support him wth anythng
@user-nn9mx5tt6dАй бұрын
Namiwa your the best freedom fighter continue my brother my Allah protecte u
@user-co3wr3rn4hАй бұрын
Namiwa uyu munthu wankulu kwambili kufotokoza mwambemve ndithu keep it up brother tiyamike uli moyo bomali chonde a Malawi tiyeni tichose
@user-nf3ik3ff6yАй бұрын
Good Message 2025 Chakwela you go
@KelvinGutaАй бұрын
A Namiwa,ndakuthokozani zedi.Keep it up,popeza Malswi idakalibe ndi mzika zophunzira koma zoyimbira mmanja zinthu zachabe,mu dzina lokonda chipani ndi.........
Namiwa uku nde kuyakhula kosanyengerera muthu keep it up😊😊😊
@rashidadan2533Ай бұрын
Inshort , In Malawi we don't have ACB , we have LCB , which means love corruption beurou , under tonse alliance corruption is worse than before . Chakwela him self is a leader of corruption and all the carbinet , We made a mistake to allow 9 parties to rulling Malawi , this time let's change ,
@user-pv9uk6sc3wАй бұрын
Timakunyadilani mr.Namiwa, keep it up ❤
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
Thanks Mr Namwiwa for talking the truth for the Malawi national keep it up
@lameckmphande-yt4ouАй бұрын
Thanks namiwa gwilani nichito anthu alitolazikoli ngatilawo kuli mlungu kumwambaku azayankha pazomwe akutichila Ife a Malawi siku ndiimozi pitilizani kutimenyela nkhondo anamiwa washing in port Elizabeth South Africa
@mikekhamusi1807Ай бұрын
Koma ikazawinaso MCP ine ndizachokamo dziko mwanu muno
@KestonNGUBOАй бұрын
Galu chokerathu iwe
@sylvesteralfred8355Ай бұрын
I would love see if CDEDI works together ndi MALAWI FIRST
@lallanayahyakasakuadam8378Ай бұрын
ine ndinachoka koma kungopitilira akapunyanyawa sindizabweranso
@user-mn3ev8rr6fАй бұрын
Keep it up my best friend 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
@HusseinMoffatt-mi1flАй бұрын
Zoonadiitu aise bomali ndi manjiokhaokha kumkuyu pwalalake asatitenfengatiife ana chakwelaiwe pamako wamva
@user-qg4it7my9n28 күн бұрын
keep it up i uyo ndi igwee cakwera acoke watikwana watching from cape town
@rashidsaid2232Ай бұрын
Mr Namiwa always standing for the truth keep it up
@user-lf6qf2tw5oАй бұрын
Kod ndalama ija mmat chakwera abweze zilipat😮
@user-lw9su5om5zАй бұрын
Katundu wina mu group ya ma president aanthu osauka keep it up
@JimmyIsaac-xd4efАй бұрын
Anamiwa , Mulungu azikudalitsani mumatiimilila a Malawi
@user-pv9uk6sc3wАй бұрын
Mr. Namiwa, mtundu wa a Malawi ukudalila bungwe lanu. Bungwe la mphavu.
@mayesojameskateteАй бұрын
You good guys
@moyo77777Ай бұрын
Koma ndiye chakwera ndimbava Mmmmm osapanga mayazi😂
@BlessingsChitekweАй бұрын
Kuyakhula kwapamwamba kwambiri ❤❤❤❤❤❤
@user-gu8fx5gl3gАй бұрын
There is no funding in many government institutions not only ACB.
@patsonmtalika1971Ай бұрын
Ndalama zathu amalawi akuwapa anthu akukasiya mwezi uliwonse akumalandila ndalama zosachepela 800 thousand kwacha ngakhale mwana akumalandila kumeneko k
@marryphili5419Ай бұрын
Keep it up we're tired of this government 🙏🙏
@DannielOnions-fy3dcАй бұрын
Thanks so much keep GOING
@user-qq1uj7ct6nАй бұрын
dziko lathu likufunika zimenezi mwina pang'ono pokha zingasinthe. mwangochedwerapo pang'ono cos zinthu zambili zawonongedwa. keep it up aziakulu akulu athu. next time tifufuzilenso kumapasipotiku kut zikuti bwanji . dziko lathu lasakazika
@YasinMusa-ym8lpАй бұрын
Mkukuyu ndimbuzi yamundu
@BhekiMavundla-po2bqАй бұрын
Big up Namiwa,izi ndizomwe timafuna kut tiziziwa mmene boma likupanga mu mphamva yaulamulo wake pothana ndikatangale.I'm fatigue with Chakwela and Tonse alliance regime, stupid!
@HalisonSolomonАй бұрын
Apapa ndipamene mukufunika kuuonesa mtundu wa a malawi kuti inu mumaimirira , chomwe chinafunika anamiwa ndi kuyenda pamseu chakwera ndi nduna zake azipita uyu ngati sachoka ife tiuma mtima tikaphulitsa statehouse akafere momo ndi banja lake ndipo afa mozunzika koopsa ngati sasamala basopu chakwera
makamaka Moses kumkuyu nde Mmmmmm he is the one amene dziko lathu walisakaza mopanda chisoni. mmene mwanenera kut amalankhula ngat zanzeru Koma ali munthu wopsa kwambili. Amose dziwani kut anthu amaziwa zomwe inu muli. Yahweh wakumwamba ndiyemweso akuziwa kuposa ife anthu Za inu. you don't even fear God maka pakutenga Mbali yakuwononga dziko. Mene Mene tekeli ovasin
@JongwenyirendaАй бұрын
Chakwera must go (.....
@BerthaBerharАй бұрын
Following
@MastaraMedisoniАй бұрын
❤❤❤❤❤
@shealtielmajawa8234Ай бұрын
Athu ambiri mdziko lino alibe nzeru
@user-lk8kj9zv6xАй бұрын
Mr Nawiwa son of the soil
@user-qp5mu7ui2cАй бұрын
Umakwan kwambiri hot 265
@AffickChaonaАй бұрын
Namiwa katundu
@NgomaRaheemАй бұрын
Mkukuyu ndimbuz
@user-nx6dk4bj8vАй бұрын
Iweyo ndikape wanva
@user-qv8sp5cz5xАй бұрын
Iwenso ndi chislu ngt uyo ali kape
@user-uc1pd1tc2xАй бұрын
Ndipo ndigaru weniweni kunkuyu
@user-uc1pd1tc2xАй бұрын
@@user-nx6dk4bj8vIwe nditombolombo zedi ndithu
@royGovender-vl9onАй бұрын
Kuwina a chakwela 2025.sindidzabweranso Ku malawiko
@Sophisticate230Ай бұрын
Kawawa Namiwa❤
@NEBERTMVULAАй бұрын
If Malawians are democratically empowered why NOT dethrone now the poor leadership they voted into power when incompetent? STOP MCP STOP MCP STOP MCP!! this is not a go area in life of Malawians
@LyfordCydseorgАй бұрын
Hope we are still having challenges to fight corruption in this country. Let's just leave this work in the hands of Namiwa but let's all join hands to fight corruption. Malawi will remain poor as it is for ever and it will also very difficult to achieve our 2063 Vision.
@MrChinikoАй бұрын
9. Sw
@GabrielGasiyoАй бұрын
Chakwela 2030 woo!!! Anamiwa aba kwambiri pa msamba parish
@user-on5qq9tg1yАй бұрын
Bola namiwayo amaba pa parish koma mbuzi chakwera akutibera misokho yathu