Рет қаралды 4,467
On 10 July 2024, Concerned Citizens of Malawi are calling for nationwide demonstrations, and renowned Governance and Human Rights Activist Undule Mwakasungula has disapproved of the plans, instead calling for contact and dialogue. However, Steven Simsokwe believes that Mwakasungula is in no position to tell Malawians when they can protest.
Pa 10 July 2024, a Concerned Citizens of Malawi akufuna ziwonetsero m’dziko lonselo, ndipo katswiri wodziwika bwino omenyela ma ufulu a Undule Mwakasungula wakana ndondomekoyi, m’malo mwake wapempha kuti anthu akambirane ndi boma. Komabe a Steven Simsokwe akukhulupirira kuti Mwakasungula sangawuze Amalawi nthawi yomwe angapange ziwonetsero.
#malawi