My gracious God have mercy on Malawians to transform their nation from rut to prosperity or vision 2063 will remain a political requiem to satiate the destitutes.Let callous religious and political leaders change their minds.
@KaisiAbdullah16 күн бұрын
We olways behind u mr bon
@SirNanjalaMw15 күн бұрын
Umakwana koma kalindo suyangana nkhope ukafuna kungalura chilungamo
@DONNEXKhama-bk1gy16 күн бұрын
Ndipo inu opposition yangoziii kumangomvera ma audio a achina horn kalindo,,ntanyiwa,, bakili muluzi TV kma osapanga support zobowa Bwanjiso
Koma chilungamo Malawi anachagamuka mcp ngat simukuziwa munalowa chifukwa kunali ma demo ndiye mukuona nga anatha? Mukufunika kumangolapilatu apa no chance
@twavysibale475115 күн бұрын
Intro yokhayo...mwalamwalatu 🔥🔥🔥
@user-wu8kp7ui5j16 күн бұрын
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
@Uncle_B26515 күн бұрын
Koma zikoli mmmmm zafikapoo
@chrisneySwanepoel-yu5vd15 күн бұрын
Bwana kalindo ingoyambisan chipani chanu tizakuvoteran coz a opposition sali serious kumene
@GRACIOUSKENAN15 күн бұрын
My boss booon kalindo,our freedom savior and fighter.
@fjtkusamba594816 күн бұрын
It is true that opposition leaders are dormant whether they like or not but they are. We Malawians are tired and worried about them. May be they're receiving some money which makes them silent, please work up!!!!!!!
@user-qq3ip1od6i16 күн бұрын
Am not really happy with the way opposition is handling the public affairs,,
@Vascomw15 күн бұрын
Powerful 💪💪💪 Ife sitikuwopa tili pa buyo pako
@OsmanChiwaula15 күн бұрын
opposition yakedi yaziiii atupele ndia DPP angokhala ziiii akungoyang'anira basi koma akufuna kuvoteredwa
@EmmanuelHussein-k8n15 күн бұрын
Mkulu uyu tidzamulira one day,he got love for his country
@KelvinMangwengwe15 күн бұрын
God bless 🙏 you kalindo😅
@user-rz9rm4cb8x15 күн бұрын
Ichi nde ndichi booooni kalindo🎉
@AchinaKellz16 күн бұрын
Ine ndi nchewa koma mcp ndi agaru nyasi zisatiipitsire mbiri uchitsiru umenewu udayamba ndi kamuzu, kuno pakati mcp yaluza ndale mpaka kupha azawo
@tasmania52715 күн бұрын
Si Mchewa iwe, DPP inkazunza aChewa omwewo.
@augustMag16 күн бұрын
Mmatilimbikisa ndi kutipanga lerise up Amalawi ife ❤🔥🔥
@EliasDzoole-js8vx15 күн бұрын
Ma bodza sangawine olo atatani ine ndineso mchewa awawa kapume
@user-oz4xv9rb6h15 күн бұрын
Mulungu azikudalisani a president athu anthu osauka ife
@ClementChilunje-k2c15 күн бұрын
Achewa yo siwose ena anyasidwa nayoso utsogoleri umeneu.
@Dysonkhofi16 күн бұрын
Let kalindo to run for Presidency
@SaidiMbawa-st6bj16 күн бұрын
Zikuchita kuonesekatu kuti ngakhaleso a tawina a opposition palibe chomwe chingasithe
Ndiposo ndizoona kumene kuti achewa ndi ambili kuposa mitundu yose ku Malawiko
@GiftSimubali15 күн бұрын
Ipatseni moto🔥🔥🔥
@IshuBillalli15 күн бұрын
Mwina akufuna muchite kwagwira Malo obisika kuti azuke inu zoona ife achinyamata tikuchita mantha kubwelera kwathu kuti tizikapanga ma business kuopa ulamuliro wa khaza omwe uli dziko lathu lomwe tabadwira zoona koma kumati kuli inu omwe mumazitcha kuti ndinu Andale mumathaso kukalowa nyumba ya malamuro zukani zukani atsogoleri athu kwakwana tsopano Atupele ,, Peter muthalika,, Chihana,, Joyce banda,, Inu bambo asikono,, Ndikunena ndinuyo Timothy mtambo ,, ndi ansanu onse ,, tachangamukani please chotsani nyazi zimenesi
@DaudiHAllie-kk1en16 күн бұрын
MCP is now bringing tribalism but just to remind them that Yao ndintundu waukulu kwambiri Malawi yonse
@agnesgwaza916516 күн бұрын
Raster kumbuyoko amakhala ali cheucheu😂
@user-zs1ec5kx2j16 күн бұрын
Opp0dition yadyetsedwa dekhani ndi mcp
@clintonhodda983016 күн бұрын
Opposition achuluka dyera sangagwilizane
@DavidMtambo-zm8ne16 күн бұрын
Aford UTM alliance tidusa popanda opikisana nawo.
@JunaKananji15 күн бұрын
Karido ❤❤❤🎉🎉
@mphatsobonongwe813115 күн бұрын
😊
@Musa1828-l5d16 күн бұрын
Chakwera anapha Chilima
@andrewmtendere316716 күн бұрын
Chi born kalindo❤
@MosesChinzuze16 күн бұрын
Ulem wan boss man tiri pambuy pano
@ChristopherJames-fm8zc16 күн бұрын
The DC
@RosemaryKhungwa16 күн бұрын
You are talking sense bro
@LatifBeni-e6z16 күн бұрын
Mbambande madala mumakwanila
@PrinceBlessings-bv5bs16 күн бұрын
Kodi Mr Kalindo, simungakoze ulendo osawadziwitsa ma president a opposition kuti akadzuke...?. Chifukwa Boma la tonse mmm likuning'inatu heavy as tsabora., Chakwera must resign ndithu 💔💔💔💔
@agnesgwaza916516 күн бұрын
😢😢ndip Eeeee atiphweteka
@PrinceBlessings-bv5bs15 күн бұрын
@@agnesgwaza9165 Ine daily mtima kuwawa ndikamava ma challenge awo kuti mpaka 30 years
@user-wb3us4pg4b16 күн бұрын
The DC❤❤❤❤❤❤❤
@kaungabondera89216 күн бұрын
When are we protesting
@oskidooscar746816 күн бұрын
Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp
@davedavie621116 күн бұрын
Osusawa sakutithandiza
@Extratremendouszeus16 күн бұрын
Welcome the dangerous child
@Extratremendouszeus16 күн бұрын
Peter nayenso akugona kwambiri.....Chikangawa mmene amasokonezera 2020, Nde mukudikira a Malawi kut aonde kaye kenako akuikeni pa mpando inu muzidzanjoya.kodi a Peter ,kufatsa kumeneko kwamtundu wanji ....check out
@MustafaMachika16 күн бұрын
❤❤❤
@user-nf3ik3ff6y16 күн бұрын
Good Messnge Chakwela you mast go
@SyilesChebomba16 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@mipeacemakermw950116 күн бұрын
Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣kzfaq.info/get/bejne/jbh0nrRp2MWXZJ8.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p
@JayVidrah-mo5xr16 күн бұрын
ThE dC😂
@TopoTopo-bm4vw16 күн бұрын
Inu puppies wa MCP sichipani cha fiti
@Martha-m6e15 күн бұрын
Zowonadi anthudi agona.ifa ya anthu onse aja sangawa vote ataa.