I prefer UTM to take the charge of the country.enawo analamulirapo komanso anatiphera abale athu.kodi mukufunanso kuti azakutheni?wina adanena kale kuti amalawi samachedwa kuyiwala
@ishakatimbe73412 ай бұрын
Utm ili ngt Eff or patavuta bwanji singawine.... Adad my vote❤❤❤
@stanleykaludzu-bm4pm2 ай бұрын
UTM bomaaaaaaa
@user-qp8kh2hj9o2 ай бұрын
Utm 2025 BOMA ❤❤❤❤
@user-qp8kh2hj9o2 ай бұрын
SKC my vote 2025 BOMA ❤❤❤
@user-uc1pd1tc2x2 ай бұрын
Zopusa zanuzo ifee ai nkhani ndi DPP
@user-uk3bz1hr5t9 күн бұрын
Kunyoza UTM is same as kunyoza DPP aise,,nd amoz awa,,,muona kusogoloku akudyera mbale imozi,,,Inu muzakhumudwa,,UTM ndi mwana wa DPP
@user-uc1pd1tc2x2 ай бұрын
APM for ever ❤❤❤❤❤
@user-uc1pd1tc2x2 ай бұрын
APM Bomaaaaaa iloooo
@Zamwano2 ай бұрын
Inu ngoimba basi zinazi mmmmm
@user-oq5rg5mz7q2 ай бұрын
MCP mukhaula sizinaoneke ndalama zanuzo tidya mwaulele, UDF my vote
@SHEREEFKanthochi-ft3dm2 ай бұрын
Komatu kuwina kulibe kaya mukudziwa?
@FrancoKaunga-rq2ki2 ай бұрын
Unless you end chewa language in schools
@jamesgama54892 ай бұрын
Chipani chopanda strong hold
@marryphili54192 ай бұрын
Za ziiiii kumasapotaso mbamva imeneyi odi apo DPP tiduse iya mavuto wosewa mwayiwara
@user-is5dl7np9g2 ай бұрын
APM my vote 2025
@EdwardRichman-zs5pl2 ай бұрын
Munalamulako kd ku utm chipani ichi chinthela malangizo bas
@Aisha-db6ds21 күн бұрын
Atsogoleli ake opanda mfundo
@user-jk8sh7fh2d2 ай бұрын
And tonse alliance ya pangisa kuti lero tiziganiza kuti Dpp iwoneke ngati anali ma dolo pamene nawonso pa level yawo anafikaposo posakhala bwino kuwatenga amalawi for granted that's bad koma to me zinakhala bwino kuchosedwa mwina ngati angapasidweso mpata aphunzilepo kuti osauka akakwiya si zienda bwino.
@user-jk8sh7fh2d2 ай бұрын
Iiiii koma guys moti utm simunaiphunzilebe ? Moti mukuembekezela kuti kuipasa mpata itha kuthandiza zikoli ndikuiphula pa moto? Aaah kwa ineyo ndi kukaika kwambili anakakhala kuti azisogoleri akewa ndi okhuzika ndi kuvutikwa kwa amalawi payamba pompaja amaenela kuonesa chidwi pa kuvutika kwa amalawi osati pano achedwa . Ndi amozi utm mcp aford ndi sangathandizeso zikoli believe me guys let's wait and see.
@user-tb6yh1kx3o2 ай бұрын
Zowanamiza anthu zisiyike wamva ulendo uno zikuvutani
@kondwanimunthali74012 ай бұрын
A DPP kuzikonda too much.Boma simuzatengaso
@SanudiMcDonald8 күн бұрын
DPP singawine payokha popanda chipani china chothandizira 🤞
@user-uc1pd1tc2x2 ай бұрын
DPP pachiongolero ❤❤❤❤❤
@cosmasnkanda81932 ай бұрын
APM my voti basi
@chrisschikozera72712 ай бұрын
😂😂😂😂😂........osazivuta chilima ll never be president in this country
@user-lf6qf2tw5o2 ай бұрын
Mbava zachabe
@jamesgama54892 ай бұрын
Mcp ulendo waku kenani kupita okha. Anzanu a UTM kuwasiya kwa pilato zaka zonsezi kumakamvera milandu, DPP tilinayo limodzi ku bagamoyo kuno.
@user-jk8sh7fh2d2 ай бұрын
Ngati Dpp ingapasidwe mwai akuenela kukonza mavuto amene anapangisa kukhala kunja kwa boma ndithu , koma ine all tonse alliance pano olo zitatani bwanji si ndingaikhulupilireso why zaonesesa kuti onse zawo ndi zimozi kuzunza ovutika basi olo kupeleka mpata kwa chilima sangasinthe chilichose azingoikilana ku mbuyo zo pusa zimene akupanga chakwela.