M busawake wodyesa mbuzi all ng'ombe nangaumbavaumenewu bwanji😊
@PaulDaka-dc3re2 ай бұрын
Chakwera kuzunza mmmmm😢😢
@sharifujoe76332 ай бұрын
Malawi wathu akuthera pa a e i o u basi Komatsu just know then masiku amata ndugona ifeyo tikumalemba big zonse
@KayifaSkeffa1232 ай бұрын
Akuba awa eeeeeee mavuto
@AjeliMw2 ай бұрын
Best TV 4ever
@michealchaomba97612 ай бұрын
Dzikoli ena akuliona bwino koma litasala pang,ono kutha Mulungu akukathani posachedwa
@user-be3is8rc4r2 ай бұрын
Muthu wamkulu keep it up
@Shaibmpondan2 ай бұрын
Best TV 🎉
@user-oq5rg5mz7q2 ай бұрын
Chakwala ndi 0, afe nde tilibe choyakhula njala iyi
@user-id8rr8or6d2 ай бұрын
Komano tingatani kut nyasi zimenezi zizathe kuno ku Malawi katangare ndi number one tingatani umboni anthu akupereka""
@kubengovender69962 ай бұрын
Keep on coming brother!!
@user-nf3ik3ff6y2 ай бұрын
Bakili Tv good message
@StevenFombe2 ай бұрын
Mukaona president akuyenda yenda mdziko muno amakhala akumba ndalama zaboma
@user-uc1pd1tc2x2 ай бұрын
Ndipo koopsa zed boss
@YamikaniChataika-ib6dd2 ай бұрын
Nice tv ever
@user-zt7hy5lh4r2 ай бұрын
I respect you Sir, u are my hero ❤️ ♥️ even if u decide to leave what u are doing today u will be legend forever
@user-lc3sw8iz2g2 ай бұрын
Abusa osowa Yesu amaba kuposa mbava zoswa nyumba kuposa odikilira anthu ndi kuwapha. Amakhala oipitsitsa kuposa mfiti kuposa satanic
@wisdommalunda20492 ай бұрын
Keep up the good work
@davidkadyakapita88362 ай бұрын
Respect leadership
@HopefulCoralReef-tx4vx2 ай бұрын
Thanks ulemu wanu big man
@user-dj5hd4ys3n2 ай бұрын
The best tv in malawi timakunyadilan
@HanishaissahKagansa2 ай бұрын
God bless you brother ❤❤❤❤❤❤
@sthoramexjrsa9022 ай бұрын
Amayo mmmm😢😢😢
@user-ky4ce9gb6j2 ай бұрын
Mavuto inu
@hakimbaiton2 ай бұрын
Iiiiiii chakwela koma atimupisa liti abere kukharira Kuba bac
@JannatuyaseenmwangaMwanga2 ай бұрын
Ulemu wanu brother ❤
@emmax91012 ай бұрын
One day is one day....God fights for the poor
@johnmiselo22302 ай бұрын
We are following you from Zambia lusaka capital
@ApocheC.2 ай бұрын
Zikomo bwana, tadziwa
@wilsonsawasawa37942 ай бұрын
They have completely rooted the country
@manzyhetekele86972 ай бұрын
U are the best big man I feel so happy whn I hear your voice ❤️ Keep it up and good protect you, you are doing good job How far this war Russia 🇷🇺 and Ukraine 🇺🇦 🤔
@user-ub1vt2kq4s2 ай бұрын
We respect you Sir good job gift bonomali from south Africa in Johannesburg
@Chikondi-sg1qj2 ай бұрын
Your surname is my grand's name ❤
@user-yi4oc4xz4v2 ай бұрын
Ur best bro
@Razarusmbavachakwera2 ай бұрын
Am tired with this nonsense useless government.please may you give us new update Ukraine war n Israel as well
@lastonmasoatenganji-bs5gf2 ай бұрын
We value you work very high because you try hard to look for justice truth. Justice that would have made us a blessed nation. A place of at least a little joy not grief and bitterness always. Stay blessed 🙏
@abisalomchunga66952 ай бұрын
Chakwela mmm ai simuthu wa bwino
@ChristopherKabanga2 ай бұрын
tiuzeni munthu wabwino
@user-jn9tz3li3v2 ай бұрын
@@ChristopherKabangaAPM
@user-hm9nc7lz6e2 ай бұрын
Zoona ladzalo munthu oipa
@patrickjaenda82882 ай бұрын
Your hill brother
@user-jn9tz3li3v2 ай бұрын
Chakwela is cursed that is why ana ake amangopanga uhule
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw2 ай бұрын
Thanks bro, no any bad words!
@user-xk4zi4cj3d2 ай бұрын
Bravo bk muluzi tv
@user-bh4zb7ji3o2 ай бұрын
Nice kma za ku Israel zili pat or za lasha
@lusolawo732 ай бұрын
Best 📺
@user-md2nf8gl9r2 ай бұрын
Ndi fire fire basi💥🔥🤜🤛
@user-uc1pd1tc2x2 ай бұрын
APM my vote❤❤❤
@JonesChingaya-yf4gg2 ай бұрын
Ife timati tavotera m'busa osaziwa kut ndi mwana wa satana weniwen koma anangobisala Ku church. Ndie wina ndi Nankhumwa akumabwera ndi mavesi, chonde musapusisike naye ndi mwana weniweni wa Chakwera mbeu yodzunza.
@WiseJordan-ds6km2 ай бұрын
God will save us.
@DONNEXKhama-bk1gy2 ай бұрын
My Malawi
@allanmakwiti51452 ай бұрын
1st to like and comment
@user-rk4ch1ly3z2 ай бұрын
Change is coming!!
@user-cd4df3vg4y2 ай бұрын
Ulemu wanu broo Lazaro ndi anzake a mcp analowa m'boma kudzalemera osati kutumikira ife mzika ayi. Ndipo watikwana kwambiri mbava yoyipa mtima iyi
@MaliGomani2 ай бұрын
😂😂More life bakili muluzi tv
@user-do2cs8nf4b2 ай бұрын
Koma Mulungu awalange anthu awa mwapadera dera ndithu yohhh