Ndege yagwera kutali ndi midzi ya anthu yeti it's not far from villegers ndiye iyeyu sanadziwe kuti amanama zosezi ngati alibe choyankhula akhale chete komanso zonsezo zikanati ndi zabwino zokhuza za zosatira za kuchipatala ko bwedzi abanja sanabwere poyera why delay yeti aziti angonenapo izi zokha zinazo azanenabe, presdent wanuyi has something to do ndi imfa ya chilima period
@AlfredNazombe-me2ly26 күн бұрын
Ndipo ine uyuu wandebvuyi amandiyelamo kobs amazimva nzeru kom ndimbuli yothelatu
Nose ndinu zinsiru kwambiri amene mukufotokoza maboza anu Chakwera wamupha muzake 😢😢
@user-zo3bf3ec3g26 күн бұрын
Times chichitikileni malilo achilima chinachake pakatipani chachitika ma program anu sakukoma mukuyeneya muzikonze mukuonesa mbali muzochitika zanu Kanakonda ndalamazo mulandile ndipo mudye koma muzima pachilungamo ndipo muzitiuza zoona😔😔
Koma osayiwala Kuti mphekesera ili pawiri; Kukhala yoona Kapena... Kukhala bodza😢😢
@user-hq8yn8tl1h25 күн бұрын
Azanena akazakhumudwisana 😢😢zitapanga xpire😢😢😢😢
@languitoneelias997226 күн бұрын
And mukazilowetsa ndale mukulakwisa because muona ngati lamulo ndi loyipa
@GeorgePhiri-ub2of26 күн бұрын
Anthu kumalawi kuno amasangalala ndimabodza gwelo LA zonsezi ndiumbuli basi
@augustMag23 күн бұрын
I am waiting 2025 all Malawian tikazavota amene azawineyo ndikukhala president boma limenero ndi lomwe lizachete kafukufuku wa ifa ya anthu amenewa amene anamwalira pa ngozi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere osatha 😭😭😭😭
@Doreen-yl3qm25 күн бұрын
Mboni yayikulu ndi Mulungu amene anali ku chikangawa amene amawona zonse,la 40 likadzakwana zizaulirika
@AyandaPhungula-bg9ql26 күн бұрын
Zawusilutu zoti tidzinamizana 😮😮
@MosesSolomoni25 күн бұрын
Tidzingo koment zachina JB zachina ntanyiwa bakili muluzi TV ndi ena akunjawo bas ife sitidzilemba km ma koment kwaolemba akunjawo bas
@mathewsmakina784524 күн бұрын
Andevu zamwayi zanu munadya kale simunganene zoipa za Mcp ayi
@MosesSolomoni25 күн бұрын
Awanda amzanu munalinawo pa program wa sanati waze asadzabwereso mwamva?
Nde akubitsa chifukwa chani! Or asaneneso zilibe tchito so abitsa bwanji kunena uthenga wenweni 😡😡😡
@VeronicaChirwa-ct4os25 күн бұрын
Etii angotipwetekatsa mtima
@user-ec4jo9cu4d25 күн бұрын
Mukundisokosera mukanena zotsatira za kuchipatala mmalo monena zakugwa kwa ndege?!!
@DalitsoPhiri-sq5nl24 күн бұрын
Kodi amene akupanga defend chakwelayi amupasa zingati akuona ngati akunamizatu mwana wakwaotu cz zokhuza ngozi zija msagwilise njira yowaseka pakamwa anthu kuti alankhule, komanso funso ndiloti kodi zomwe amapanga a silikali wo zoti tiyeni tikasake ndege uku osati kwinako amawalangiza ndi ndani komanso potumidza anthu nine akasake ndege zimenedzo ukudziona kuti ndi zazeru komanso kusiisidwa kwa kufufuza ndege basi nkhani zonsezo iweyo ndi ukadaulo wakowo sungaone kuti something was off here, let malawian explain there views malingana ndi momwe a presdent anuwo anapelekera uthenga wao unali osagwira.
@stevezulu210826 күн бұрын
Olo ingo zisiyani.
@wonganichakakanyirenda329925 күн бұрын
Chilungamo chizaziwika basi
@NdamvaScnp25 күн бұрын
Mcp yakumpha
@PeterKayuni-n2r25 күн бұрын
Yaaaaa
@user-ml2vw1dc9c25 күн бұрын
Akubanja anena chilungamo ndipo tadziwa basi otukwanawa ndimowa ndifodya
@AufiThera25 күн бұрын
Mwapha Munthu
@OscarKJekapu2 күн бұрын
Ndinu zitsilu malibe chazeru
@MatthewsJohn-kv8fj8 күн бұрын
Chinachitikq ndichan kuti ndege igwe??
@FloridaMakwinja-eq2ek25 күн бұрын
Ndichifukwa chani akumanga wina aliyense woyankhura fir the whyy Later kumafufuza
@languitoneelias997226 күн бұрын
Well come dont forget kuti every accident has acause,car ,motor bike,an aeroplane lets just calm we wiil have good answers dont talk things without umboni because its acrime
Posaikira kumbuyo chipani km malire a ufulu akalankhulidwe ndiofunika kwambri kuyambiri kuzako, makolo , pantchito ngakhale pa mudzi izi ndizofunika koma ndale zikutiyiwalitsa zosezi.
@HalisonSolomon15 күн бұрын
PALIBE CHANZERU MUKUYANKHULAPO APA NDI ANA OMWE AKUDZIWA KUTI CHAKWERA NDAMENE ANAPHA CHILIMA, OSAMAYANKHULA MOZEMBA KAPENA MUKUOPA KUKUKWEZANI NDEGE NANU IYAAAAAA, MUKAONA KUTI ZOKAMBAZANU NDI ZOZEMBAITSA KUIKIRA KUMBUYO BOMA NDIYE MUTSEKE MA PROGRAM ANUO MUSATINYASENAZO , ANTHU ALI NDI UFULU OYANKHULA TIRI MU DEMOCRACY, MUKAKAMBA ZA POLICE KUMALAWI KULIBE A POLICE KULIBESO ACHITETEZO
@user-dg5pc6rz1b25 күн бұрын
Zao izo or cent sidadyepo nde worries what bisani
@GeraldMkwewu-gd5eb26 күн бұрын
Inu achina wander dyani ndalamazo ndi chakwera zisiru lnu times palibe chazeru pano
@user-dn3gp6yi4y11 күн бұрын
Palibe Cha zelu chomwe mukukamba apa tiziwa kusogoloku a MCP akazagwa m,boma
Mmalawi wina aliyense akudziwa chozachita 2025 sikuti azavota chifukwa cha mayankhulidwe anu koma nkhalidwe
@chadreckchibwithala149325 күн бұрын
koma eee msova a dpp
@Musa1828-l5d25 күн бұрын
Zitsiru izi zinadya ndalama
@ThokozaniSaiti25 күн бұрын
All of you one day you will pay one by one for what you did to Chilima and others
@lacfunnytv12515 күн бұрын
Nonsese
@DiversonChimenya-h2u19 күн бұрын
Khoswe akakhala pa khate sapheka zikanakhala kuti Dr saulosi chilima sanaphedwe bwezi panopa zosatilazo zitawulusidwa kale kale chifukwa black box siyikanasowa koma kusowa ko ndikumwe kukupangisani kuti muziyikila kumbuyo boma limeneri
@BerthThomas-v9l25 күн бұрын
Munagulidwa Ndi mcp agalu inu
@JTUPHIRI26 күн бұрын
Guys Malawi wathapo basi tivomeleze, mpaka wonder kumayankhula moduka mutu chonchi! Ndiye amene angatiimile ndindani?
@RABSONSIKELO26 күн бұрын
Dziko silinathe vuto lilipo ndilakut mumakonda ma negative
Taziyayakhurani zanzeruuu ngati ma citizens amalawi bax bzy talking foolish thing yr stupt you tow gys mukuwona ngati mwawinaaa time yovata ikubwerah muzarirah ng,weee😂😂😂😂