NJIRA ZINA ZOPEZERA UMBONI WA CHOMWE CHINAPANGITSA NGOZI YA NDEGE YOMWE INAPHA DR. SAULOS CHILIMA NDI ANTHU ENA 8.
Пікірлер: 273
@campbell8988Ай бұрын
This is the type of wisdom we need, ndamva audio yanzeru since i started following this issue. Stay blessed
@evelynnzima1716Ай бұрын
My deepest condolences to our beloved sister country of Malawi. As a Zambian citizen I mourn with you. The Lord is your strength!😢
@graciouswasibu5184Ай бұрын
This is so clear
@leonardngala6148Ай бұрын
Kuyankhura koma kumeneku ithink ndinu munthu wowopa Mulungu. God bless you
@madalitsokalima853321 күн бұрын
It's not all aircrafts that carry data and voice recorders because the equipment is very expensive in most developed countries only planes that carry above 16 passengers and they are commercial,all planes are mandated to have a transponder which sends a ping that to show position for the air craft.And this aircraft being military less hope it was carrying data and voice recorders and that they were recovered safely for engineers to analyse.On top of that service records, communication between pilots and traffic control also plays a big role in investigation.
Ose anali kuja amaziwa siku lakwana inuyo mumaona ngati chilima azamfa imfa yodwala yokha kapena ndi wamuyaya mulungu uja mmamulila uja kuti zithu zikudula akumva mapemphelo aja
@yowasschitsosa5348Ай бұрын
Usapiteko tisie tiike maliro a president wathu mwaulemu
@user-lz5yv4vj6hАй бұрын
He wasn't suppose to be there
@glorynkhata1185Ай бұрын
It's accident you never pridict or know if the pilot loss the control so what ? He was not God chilima
@LeendaDeborah2005Ай бұрын
@@glorynkhata1185the pilot never lost control. The villagers that live near that place said that the plane landed perfectly do not blame the pilot 😑😑
@AaronDungadunga-ff2nyАй бұрын
Munthu amene anapanga kuti chilima ayende pa ndege akhale munthu oyamba kupereka umboni chifukwa iyeyo ndiamene ali ndi nkhani yonse ya imfa ya chilima ndipo akuziwa chilichose chomwe chinachitika ndipo ndiyemwe anapanga plan yonse ya mmene chilima amayenera kuyendera
@giftnyirenda5614Ай бұрын
Bwana ndinu munthu wanzeru koopsya. Nkanakonda nkanakudziwani. Your are a matured person, civilized.
@MphatsogiftJerejrАй бұрын
Mafana oganiza bho ena ndi amanewa kupeleka upangili ukwanila bwino
@CatherineChalemaАй бұрын
Ndipo kwambiri!
@dominicmphepo-jk8lkАй бұрын
God bless Malawi with wise and intelligent people like you bro. But such good ideas can't be welcomed now in Malawi we are amongst the weakest people. But you are talking well bro
@speakwellgladys5569Ай бұрын
May the Lord bless you brother for your wise and humane speech may the Lord give you abundant wisdom...
@yahgoshen5815Ай бұрын
Thanks brother mwayankhula bwino
@ShereenmustaphaАй бұрын
Very true. Takumvan abwana
@user-nj5vu8cd5lАй бұрын
Umbuli these record information no one can stop it... This man is talking something very sensible ❤❤
@loziStevenАй бұрын
Well said sir. It's my hope that the two devices were collected from wreckage site, are secure and will be made available during enquiry. May their souls rest in peace.
@tapiwakalako-pm1tyАй бұрын
Well said bravo may the souls of those who were in the plane rest well
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
This massage is open a Malawian eyes let work together to find what cost deaths of our peoples RIP
@chifundomatumula1652Ай бұрын
Well said but kwathu kuno chilungamo chimabisala when people in power, rich and highly trained and educated are involved coz they influence the outcome of the investigations
@LeendaDeborah2005Ай бұрын
Koma this time they will fail miserably
@StiveriaChikongaАй бұрын
Thanks for this massage 🙏
@levisonchimseu2779Ай бұрын
Kulakhula kwa wisdom brother
@BlendaMpinga-fy8dxАй бұрын
We have lost our dearest father my your Saul Rest in Everlasting peace my the good lord provide love Mary
@ArthurMzingeniАй бұрын
God bless upangili wabwino
@hendrickbanda5644Ай бұрын
My heartfelt condolences from Zambia
@vascoholland3273Ай бұрын
Well spoken, keep on giving better and good advice to the nation of Malawi, only God knows what really happened the day our beloved deputy president passed on, let only the investigation reveal the truth May the souls of the deceased rest in eternal peace 😭😭😭😭😭😭
@kachisuzimwale5641Ай бұрын
Good message
@user-nv5bd4rn8fАй бұрын
Ambuye akudalitseni. Thus strong word
@user-kw7wr4kq9wАй бұрын
We need people like u God bless you ❤❤❤❤❤
@YankhoMAcheso-ee7kwАй бұрын
Not need people like him.... We have to be like him
@EliChitupeАй бұрын
Thank you sir ❤❤
@AnthonyPhiri-bm4vsАй бұрын
Thanks polangiza ndikuphuzisa komwe koma ino ndithawi yoti athu alakhule zakukhos kwao iyi ndi imfa yowawa so do pray with it
@EuniceKalamboАй бұрын
God have mercy...
@ireentaombeАй бұрын
Following with interest
@OkalekaleАй бұрын
Kufotokozela bwino,nzika ya nzeru.Ambiri ndi okhudzidwa koma kulira ndikosiyana-siyana.Tiyeni tilireni,tiyike maliro,then kafukufuku achitidwe mosasiya kanthu mpaka zidziwike zeni-zeni zomwe zinachitika,inali ngozidi kapena umbanda.
@angelmalawiofficial9172Ай бұрын
Well impact information Leader
@ThomasMphande-f8d22 күн бұрын
Inu abwana mnapitadi ku school mnthu wa school amalankhula motelomo zikomo God bless you.
@micheckphiri5447Ай бұрын
This is a good talk
@CynthiaPatel.E.BАй бұрын
A big respect to you sir
@aggieguda8660Ай бұрын
God bless you Mr
@Yungjoe786Ай бұрын
Thank you sir
@YamikaniLoyaАй бұрын
This massage makes a lot of sense
@thomluciouss736028 күн бұрын
May the lord show his grace through our brothers and sisters who lost their lives due to this accident
@user-ul7rb4bn5eАй бұрын
Well said 👏👏
@benchilenje9856Ай бұрын
Mwayakhula Mr
@Hellenistic109Ай бұрын
God bless you sir
@PatrickMailosАй бұрын
Mavuto abwerakale pano Kaya atimanga. Atimange basi chakwera wapha chilima 😭😭😭😭
@John-to8glАй бұрын
Nice one 👍 bro message yamphamva imeneyi, maka potiziwitsa bwino lomwe dza tizida Tosunga information tamundegeti kuti timakhala malo olimba or Ndege itayaka moto komano tizida timeneti sitikhuzi ndi moto, I hope tizida timeneti tilipo, ambuye alemekezeke
@brightadam110Ай бұрын
Awa ndimaganixo womwe ndimaganiza cox ndidavaposo zama devices amenewa kuchoka kwa bwana wanga wa chi China 🇨🇳
@joaquegerman2250Ай бұрын
God bless you man
@ImmedGerrardАй бұрын
Respect🙏
@AlexKaunda-ny2egАй бұрын
Ambuye wakumwamba bwelesani nthenda yamisala pa mbeu yose ya chakwera ndi azake ose achiwembu😢😢😢
@joaquegerman2250Ай бұрын
God bless you
@user-je8jm5uy1qАй бұрын
Zikuwawa abale 😢😢😢😢😢 taluza anthu dziko Muno
@KenDuwehАй бұрын
Kom Chilungamo chimaziwika nthawi ikakwana ndipo muzachita manyaz kut Amalawi aziwa chilungamo sopano akuteng step ina yot kuyikilaba kumbuyo sizagwira😢
@user-nb1ns6ye1vАй бұрын
Perfect said 😢
@innocentsathasteven4093Ай бұрын
Sad story to loosing anthu omwe amatipatsa chiyembekezo Pa malawi mizimu yawo iwuse mu myendele
@kayzeesambani7153Ай бұрын
Respect,🙏
@user-qs7nx7wi4jАй бұрын
Loud and clear milandu sorted km funso tizinthu timeneto tilipo
@bensawanga9662Ай бұрын
Leader par excellence.MHSRIP 🙏
@user-wd9yd1bg9nАй бұрын
Komanso ma phone a ma passengers can also be used because amongest passengers one might think of recording or eri
@greenwellmponda2363Ай бұрын
Malawi 🇲🇼 my country,mourning together here in Zambia 🇿🇲
@lucassakala3352Ай бұрын
Too sad rip our brothers and sisters we believe almighty is with your souls Amen
@JafaliAkimu-ll1bfАй бұрын
aboma azifufuza chani aboma ndi amene apha anthuwa anachoseranji zimenezo nfusen kunkuyu 'chakwera 'zikhale ng'oma ' ndi asilikali ndi apolice achita kuphedwa ndi mcp umboni ndiwuti
@wisdommunthali5202Ай бұрын
Umboni ngati muli nawo tionetseni ugwire ntchito
@jamesjanaАй бұрын
That's only way to find out the foult of the crach of our plan
@user-lg2ws2ki3dАй бұрын
Respect Sir
@wilsonnoahkadyamaliro1358Ай бұрын
Well Spoken
@bennyfuratiro8617Ай бұрын
Eish ndiri kudandaura ini why why mara, forever in our hearts