Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe
@RiannahKaliat6 күн бұрын
Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend
@mayesohenry6 күн бұрын
😢😢😢😢😢
@actuarialscience22833 күн бұрын
Nanenso
@mirriamnyongolo-vf6cn3 күн бұрын
I still don't believe
@user-fd1tu6ku1r6 күн бұрын
The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.
@sithandanechirwa63766 күн бұрын
I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands
@HamiltonwaNamuwah6 күн бұрын
Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo
@MarthaJafali6 күн бұрын
Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu
@user-nw6ie3xx8b6 күн бұрын
I love this brother but dyela
@user-zk7jw9up6m6 күн бұрын
Zikomo mtambo
@emmanuelmukondia35686 күн бұрын
THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.
@jamesgondwe66695 күн бұрын
God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?
@mishecksipolo71536 күн бұрын
That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess
@AbelSinoya5 күн бұрын
Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂
@jogechawa61926 күн бұрын
For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma
Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape
@AlinafeMuleso3 күн бұрын
Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa
@user-bq5ev7de1l6 күн бұрын
Apm my vote ✊
@JosephJosab6 күн бұрын
Mtambo ndi kape
@surgeon16213 күн бұрын
Malawi has become a very sad country. Everyone is just fighting for their own stomach. A person like Mtambo shouldnt be applauded like that as if he wasnt a minister in this government. What achievement can he show malawians to prove he is a better man for malawians. A lot of people want to use Chilimas death to gain points for themselves and yet they have no substance themselves. Too much sentimentalism without constructive knowledge
@emmanuelmukondia35686 күн бұрын
Idol worship
@user-jx8us9bc1o6 күн бұрын
I totally agree with you
@user-nj1pv8hj2x6 күн бұрын
Ndipo live i agree with you big time 👍👍👍
@amourvido80275 күн бұрын
And they don't realize it, they blindly do it💔
@hendrixchimalizeni7505 күн бұрын
Usaweluze pakuti kuweluza ndikwake namalenga
@blessingskutchuwi86353 күн бұрын
Take it if it was your DAD.... 😔 Bwez iliso Idol worshipping
@kamangamathias20016 күн бұрын
What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?
@AlinafeMuleso3 күн бұрын
Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise
@MaggieCement3 күн бұрын
Iyeyu anali boma momwemonwapanga chani atinyase apa chifukwa anamuthothamo modzi mwa anthu okhutisa mimba iyeyo aligulu lomwelo hiya zokuba basi😊
@AlexKaunda-ny2eg6 күн бұрын
More fire mtambo chakwera machende ako😂
@PhillspicJere6 күн бұрын
You will gain nothing bro potukwana munthu wankulu, matsoka agwa pakutu panu
@LukeMkandawire-cr7en2 күн бұрын
Watan😅
@EdwinMakwangwala4 күн бұрын
Only God is our rest not this politicians. God help Malawi
@arthurmanyozo12896 күн бұрын
Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus
@LunnahMtambo6 күн бұрын
More fire bro ,love from ccter namtambo cp
@LloydLuwis6 күн бұрын
Keep morefire mr tman
@WiscotDzombe11 сағат бұрын
Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza
Mtambo mtima wake ndi wadyera mmene wachoka ku MCP akufuna apeze not adzidyera kudzera kwachihanna ndiye in leronso asabwere ndimabodza ake ofuna podyera watipwetekesa ngati dzikoli Lili pamoto nfichifukwa Cha iyeyu ndi galu kwabasi
@MorrisMapiri-d6z4 күн бұрын
It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.
@nicholasshema90164 күн бұрын
Awawa anachoka value cz iyeyi akusapota Chihana Athu akuwauza apa kuti apite chitsogoro ndi achipani chinaso so he z speek speechles
no no anthu mzimvetsa zinthu u know very well kuti 6 july ndisiku la padara kumalawi ufulu omwe mkulankhupa lero nkhani yake ndi 6july nde mmafuna asiye za 6july apange za ma candle aa imfa si ya chilima yekha ati anthu akufa dairy .
@SajeFurniture-wj1ueКүн бұрын
Nkulu wake yemweyu anatibweretsera mavuto, how can we trust him
Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa
@promisegregory83975 күн бұрын
Amalawi wake up Mtambo ndi kape this guy he is after Money ndi kape machende Ake,amangofuna Ku watenga amalawi ngati makape
@nafejonga9726 күн бұрын
Rest in peace, my president .. we are still fighting
@YahayaUndiya6 күн бұрын
Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo
@jelsonmlowoka86115 күн бұрын
Anali momwemo mu galawundi bwanji zinamukanika
@user-uk3bz1hr5t5 күн бұрын
Mtambo you are a reason behind all this problems malawians are passing through,You escalated demoz that paved a way for MCP to get in power,see now where we are now.😢
@KondananiNjakwa4 күн бұрын
Mtambo was a Minister anapangapo chani? Amuchosa lero azioneka wanzeru? Ndale zopusa izi. 6 July mapemphero anali ku BICC basi.
@ChilangoNdalama6 күн бұрын
Big mtambo timakunyadiran
@CharityKangulero6 күн бұрын
❤❤❤ Exactly
@user-oc8nj3or6y4 күн бұрын
But we needs people who can at least change something in this country 😢😢apart from this government that we have now😢😢
@augustinechibbalazi88976 күн бұрын
Politics will never transform Malawi. I suggest,all party presidents,some traditional and religious leaders should jointly accost the H E and matters of philanthropy and patriotism concerning current national teasers.Neither invective nor censure wll bring democratic solidarity in our beloved nation.There is need for deliberation with the HE and his Vice President.Avoid self centredness,power hunger, political chauvinism and cupidity.We are no longer ease!
@henryphiri61004 күн бұрын
Chilima anaphedwa ndi Zikhale Ngoma,Chimwendo,ndi Kunkuyu.
@georgenundwe5 күн бұрын
Why do we choose kusadziwa pamene everybody knows pretty well kut kuli global crisis ya economy.....and one expects milakuli that we do best than the lest ....lets.be the champion of telling Malawians the.truth
@estherkambewa77914 күн бұрын
Eeesh zoopsya, taking advantage on poor people.
@KondananiNjakwa4 күн бұрын
Kodi zoti nsewu ukulimidwa pano sakudziwabe Mtambo? Kapena anatuluka mdziko muno? Anthu ndale mumapanga mosaganiza sure. Mapemphero adasanduka nsonkhano wa ndale? Useless politicians with no future