KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌

  Рет қаралды 166,310

HOT 265

HOT 265

7 күн бұрын

Пікірлер: 391
@RiannahKaliat
@RiannahKaliat 6 күн бұрын
Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe
@RiannahKaliat
@RiannahKaliat 6 күн бұрын
Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend
@mayesohenry
@mayesohenry 6 күн бұрын
😢😢😢😢😢
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 3 күн бұрын
Nanenso
@mirriamnyongolo-vf6cn
@mirriamnyongolo-vf6cn 3 күн бұрын
I still don't believe
@user-fd1tu6ku1r
@user-fd1tu6ku1r 6 күн бұрын
The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.
@sithandanechirwa6376
@sithandanechirwa6376 6 күн бұрын
I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands
@HamiltonwaNamuwah
@HamiltonwaNamuwah 6 күн бұрын
Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo
@MarthaJafali
@MarthaJafali 6 күн бұрын
Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu
@user-nw6ie3xx8b
@user-nw6ie3xx8b 6 күн бұрын
I love this brother but dyela
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 6 күн бұрын
Zikomo mtambo
@emmanuelmukondia3568
@emmanuelmukondia3568 6 күн бұрын
THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.
@jamesgondwe6669
@jamesgondwe6669 5 күн бұрын
God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 6 күн бұрын
That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess
@AbelSinoya
@AbelSinoya 5 күн бұрын
Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂
@jogechawa6192
@jogechawa6192 6 күн бұрын
For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma
@EdoJohn46
@EdoJohn46 6 күн бұрын
Antambo 😂😂😂 ndikukutengeni ngati ndinu amene mudasongezera dzikuni dzamoto kuti tipse Malawi muno ndiwe galu kwabasi
@ThomasShuga
@ThomasShuga 5 күн бұрын
Very true 😢😢
@MatiasMbaula
@MatiasMbaula 4 күн бұрын
Very true
@MaggieCement
@MaggieCement 3 күн бұрын
Ndipo Inu alibe umuthu uyu za ziiii mesa iye emweyi ndiamene anapangitsa kuti tilowe mudima akuonapanowo galu zedi
@wakisamsukwa9918
@wakisamsukwa9918 2 күн бұрын
No matter how long you have gone the wrong road, turn back. Turning back isn't an offence
@HarlodAndrewbanda-vf2rd
@HarlodAndrewbanda-vf2rd 6 күн бұрын
We're still crawling to get there!! Rest in peace Dr SKC, UTM is a movement
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 6 күн бұрын
Amtambo...ngat mukufuna kut ife tikukhululukireni ...pitani ku mademo mutibwenzere dziko lathu...anthu akuopa mademo chifukwa alibe support...mabungwe onse chakwera adasiya abale ake mmaudindo
@LOKAMJ
@LOKAMJ 5 күн бұрын
Exactly
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 5 күн бұрын
DPP could have finished us . He did the right thing to rescue some of us from DPP. It was oppressing us
@InnocentMmanga
@InnocentMmanga 5 күн бұрын
😂😂😂
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 5 күн бұрын
@@ancientnkhata1137 oooooh ...May the curse of Almighty befall who is a lier...and make them the wood of hell fire
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx 6 күн бұрын
Mtambo thanks for the vital words. We now needs actions against these idiots in the government
@rexphiri6951
@rexphiri6951 5 күн бұрын
powerful words Mr Mtambo
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 5 күн бұрын
Only stupid people with commend the selfish and greedy Timothy Mtambo
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
@dhaoudhiabedinegomaseko2363 Күн бұрын
Mtambo mseu wa Rumphi Nyika Chitipa munawukana mesa munkaguba nkumaphwanya zinthu kuti musinthe utsogoleri
@SakanjiraRose
@SakanjiraRose 5 күн бұрын
I'm getting confused, he is the man who mobilized people to fight a government that was to me far much better than the this one he helped to form.
@chrisboyce2
@chrisboyce2 6 күн бұрын
SKC forever in our hearts 💔🔥 powerful words Comrade Mtambo Osafooka kms Osaopa Dziko ndi lanthu ife kuno Ku Ntcheu tili mbali yanu...
@user-te4ii6sz2v
@user-te4ii6sz2v 6 күн бұрын
We quote more political speeches than prayers. This was not a political rally
@JosephHill-fy1bb
@JosephHill-fy1bb 5 күн бұрын
Ntambo is not a pastor.... Just watch pastor's preaching time...
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 6 күн бұрын
Ndikakumbukila ifa yaathu amenewa mtima umawawa
@PatriciaMbewe-xn7ke
@PatriciaMbewe-xn7ke 6 күн бұрын
Kwambiritu
@YohanePatrick-lc2lq
@YohanePatrick-lc2lq 6 күн бұрын
Man ife amalawi tikufuna dpp enawa abodza ngati iweyo Timothy anakuchosa ku mcp chifukwa cha katangale
@user-zf9xs3zj9b
@user-zf9xs3zj9b 6 күн бұрын
Wakuba mtambo akutiona ngati amalawi ndife galu anthu mwa sandutsa ndale ndi maliro a Dr saulos chilima 😂😂😂
@MisheckAselo
@MisheckAselo 6 күн бұрын
That's true they is nothing to celebrate 60 years, it's like we help chakwera, kumkuyu ndi zikhale ng'oma kudya mitsonkho yanthu. Ayi momwemo 😂
@ChiletsoChembe
@ChiletsoChembe 3 күн бұрын
Amalawi please! Let's pray to God forgive us and punish those who mudder saulos chilima
@user-ub1mw7ce5p
@user-ub1mw7ce5p 6 күн бұрын
Well spoken, comrade Mtambo.
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 күн бұрын
He has missed the trail. Uyu watha. Ndipo akamati ngati wina amawona ngati wayimisa agenda, atanthawuza kuti munthu wina anachita kuphedwa? Kulankhula kopanda nzeru
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 күн бұрын
Nanga munthu angati anyamata oganiza bwino akumanena wena Lwarwa aaaah guys Mtambo anaganiza bwanji?
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 6 күн бұрын
Mtanbo akuyakhula za ndale zikugwilizana bwanji ndi mwambowu
@ErickIssah
@ErickIssah 6 күн бұрын
Ndipo inu
@JohnSingano-f1p
@JohnSingano-f1p 6 күн бұрын
The voice of a lion always brings confusions
@ConfidenceBanda-g8k
@ConfidenceBanda-g8k 6 күн бұрын
Koma ndipo poletsa kupepherapo ndie nduchitsiludi,mobwereza amene amaletsa kupepherayo nchitsiru
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 5 күн бұрын
Well spoken comrade mtambo criticism singalephere as Malawian we were born like that, keep it up comrade
@jonathanmalanda7742
@jonathanmalanda7742 5 күн бұрын
A Mtambo ikani za mapemphero kuti mzimu wa skc uuse mumtendere
@TnmMpamba
@TnmMpamba 6 күн бұрын
Watching live from Salima, Khombedza
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 6 күн бұрын
mtambo walankhula za mzeru kuposa namachende chakwera
@ChifundoWillard
@ChifundoWillard 6 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@tingamasi106
@tingamasi106 6 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
@LukeMkandawire-cr7en
@LukeMkandawire-cr7en 2 күн бұрын
😅😅😅
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 6 күн бұрын
Koma tizikukhulupirirani ndithu a Timothy???
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 6 күн бұрын
My question too 😢😢
@AndrewLanken-v3u
@AndrewLanken-v3u 5 күн бұрын
He has got nothing to give malawians never
@MagretIdimu-u7w
@MagretIdimu-u7w 2 күн бұрын
We're heart broken 💔 SKC still remains in our hearts 😢😢😢
@DannielOnions-fy3dc
@DannielOnions-fy3dc 5 күн бұрын
Thanks so much 🙏 keep it up please we need people like 👍 u
@SteveKumwenda-t3d
@SteveKumwenda-t3d 6 күн бұрын
Chitsiru ichi, ndiponso uku sikumapemphero
@abwinoamatani4921
@abwinoamatani4921 6 күн бұрын
A ndale ndabodza kumene. Ndi chifukwa chake olo akuba ndalama zambiri-mbiri akavala amangokhala ngati avala chithumba chaku chigayo
@user-io2uw2me9f
@user-io2uw2me9f 5 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@AndersonChiponola
@AndersonChiponola 2 күн бұрын
Mtambo ndamene anapangitsa zonse izi palibe chomwe angayankhule Mutu wake sumayenda bwino ameneyo chifukwa anamuchotsa unduna wagwa nayo Mbuzi iyi
@user-ie5pc4ox8i
@user-ie5pc4ox8i Күн бұрын
Ada awawa bwenz Ali MUNTHU wapamwamba kwambir kma Anapanga zausiru ngat akufuna timukhulukire ayambise mademo
@RitaKainga
@RitaKainga 5 күн бұрын
Zikomo Inu nonse amene mwalimbabe mtima kupanga mwambo uwu though asatana akutchinga,Mulungu wathu ndwabwino,sanalepherepo,imfa iyi ndyovuta kuiiwala
@JohnAsendi
@JohnAsendi 6 күн бұрын
Antambo vuto chinthu chimozi mumafuna ndalama Chonde muzikhala ngati Born Kalindo chifukwa amati pavute pasavute asayimira amalawi ndipo akuti imila amangidwa amangidwanso pomwe enanu mumatifuna pomwe zakuvutani tikukukuwerenganitu INEYO NDIKUCHALENJA zoti wina aliyese aime payekha kuyambira Apita. Tupele. Raz. Nankhumwa. Shahana. Osati Chakwera Amayi Joyce banda ndi phulezdent Kalindo. Ndiye tikavote masankho mawa mwachilungamo mopanda kubela angawine ndi Kalindo chifukwa ndi amene akuoneka kuti angatithandize osati Ena inu 😁😁😁😁😁😁😁😁😁
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 6 күн бұрын
Inuyo
@user-ww4ei5fb7d
@user-ww4ei5fb7d 5 күн бұрын
Kalindo ndiolimba mtima, ofunika kumuvotera. 😂
@JohnAsendi
@JohnAsendi 5 күн бұрын
@@user-ww4ei5fb7d zoonadi sister osati enawa akuoneka ngati akuti konda koma mmitima mulibe chikondi
@LulezLele
@LulezLele 6 күн бұрын
Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 күн бұрын
Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa
@user-bq5ev7de1l
@user-bq5ev7de1l 6 күн бұрын
Apm my vote ✊
@JosephJosab
@JosephJosab 6 күн бұрын
Mtambo ndi kape
@surgeon1621
@surgeon1621 3 күн бұрын
Malawi has become a very sad country. Everyone is just fighting for their own stomach. A person like Mtambo shouldnt be applauded like that as if he wasnt a minister in this government. What achievement can he show malawians to prove he is a better man for malawians. A lot of people want to use Chilimas death to gain points for themselves and yet they have no substance themselves. Too much sentimentalism without constructive knowledge
@emmanuelmukondia3568
@emmanuelmukondia3568 6 күн бұрын
Idol worship
@user-jx8us9bc1o
@user-jx8us9bc1o 6 күн бұрын
I totally agree with you
@user-nj1pv8hj2x
@user-nj1pv8hj2x 6 күн бұрын
Ndipo live i agree with you big time 👍👍👍
@amourvido8027
@amourvido8027 5 күн бұрын
And they don't realize it, they blindly do it💔
@hendrixchimalizeni750
@hendrixchimalizeni750 5 күн бұрын
Usaweluze pakuti kuweluza ndikwake namalenga
@blessingskutchuwi8635
@blessingskutchuwi8635 3 күн бұрын
Take it if it was your DAD.... 😔 Bwez iliso Idol worshipping
@kamangamathias2001
@kamangamathias2001 6 күн бұрын
What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 күн бұрын
Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise
@MaggieCement
@MaggieCement 3 күн бұрын
Iyeyu anali boma momwemonwapanga chani atinyase apa chifukwa anamuthothamo modzi mwa anthu okhutisa mimba iyeyo aligulu lomwelo hiya zokuba basi😊
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 6 күн бұрын
More fire mtambo chakwera machende ako😂
@PhillspicJere
@PhillspicJere 6 күн бұрын
You will gain nothing bro potukwana munthu wankulu, matsoka agwa pakutu panu
@LukeMkandawire-cr7en
@LukeMkandawire-cr7en 2 күн бұрын
Watan😅
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 4 күн бұрын
Only God is our rest not this politicians. God help Malawi
@arthurmanyozo1289
@arthurmanyozo1289 6 күн бұрын
Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus
@LunnahMtambo
@LunnahMtambo 6 күн бұрын
More fire bro ,love from ccter namtambo cp
@LloydLuwis
@LloydLuwis 6 күн бұрын
Keep morefire mr tman
@WiscotDzombe
@WiscotDzombe 11 сағат бұрын
Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 5 күн бұрын
Osaoopa ai......ku Malawi kulibe president
@edsonnyasulu5394
@edsonnyasulu5394 5 күн бұрын
Exactly Andale akale achoke boma achinyamata alamulire dziko nkhalamba ndi mfiti komaso ndiankhaza
@VincentAndrew-jz2gf
@VincentAndrew-jz2gf 5 күн бұрын
Atambo ,Ulibe Zelu unaphetsa Athu Ambili
@AustinBornface
@AustinBornface 5 күн бұрын
Malawi timakhala ngati tili pa stage tupanga drama kma ayi ndithu ndi action
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 күн бұрын
Munayambira kukonaza dziko mudzamaliza liti komanso palibe chimasintha mumaona ngati umphawi wamalawi ndiye podyera panu komanso polemerera panu palibe chanzeru chkmwe wayankhula mtambo apa
@PeterThomas-lw3io
@PeterThomas-lw3io 6 күн бұрын
Rest in peace 🕊️ chilima anagwira chito yaikulu DPP mu 2014 ikanafela giya komano chilima anapanga zotheka kuti Peter akhale tsogoleri muchomwechotso mu 2020 wayigwira ntchito yathangata kumuyika Crazy Chakwera akulamulila koma njilu ndikupanga mission plane yakumupha yooohhh Chakwera ngoyipa
@markjames-v1f
@markjames-v1f 19 сағат бұрын
Chomwe mkukanikila kutiyimilira ndichan boss wanga
@anoldkapolo4493
@anoldkapolo4493 Күн бұрын
Kkkkkkkk aMtambo mabodza ndipo zikatere timati zawo zinaona kungolo, bwanji Mtambo osango gawa chakudya kwa anthuwo kapena muwamangira nyumbazo. . Kufuna ndalama kumeneko , osangopita kukapanga dimba . Chakwera akumenyera nkhondo ife alimi ndipo 2025 ndiboma choncho A Mtambo akunama
@AngellachifundoMwale
@AngellachifundoMwale 4 күн бұрын
Mumatipangisa ndinu omwe muli ndikuthekela kolamula dzikoli koma chonsecho simutithandiza and iwee ntambo uli nkuyankhula koma osakwanilisa mxiii unduna uja unali pheeeee ife tikuvutika pano fukwa cha nzerru zomwe unatilimbikisa ife kuti tikavotere mcp yet lero ukuti usintha ziko mub 2025 yet wakanika zaziii
@AbdulKhan-j2h
@AbdulKhan-j2h 6 күн бұрын
Mpava iyi atidye bawo bwanji Sumatuluka uli nduna pano abakuchosa ukufuna kodwela amalawi timaiwala
@user-ok7bq9es3y
@user-ok7bq9es3y 5 күн бұрын
Timothy unali ndi molaro kale iwe because of Msundwe barracks, size yako ndi Chimwendo. Ulibe faz iwe
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 6 күн бұрын
LUWALA ANGASINTHE CHANI MBAVA YA MNTHU
@MACKDADFFDANIEL
@MACKDADFFDANIEL 2 күн бұрын
Vuto athu kumalawi safuna kumenyela athu ovutika kom mimba zawo zomwe akuyakhula uyu ntambo ngati Ali ndi nzeru chonsecho momwe anali nduna samayakhula PAno anamuchotsa wayamba kuwalalatila athu omwe anawasiya a kugwila ntchito mbuzi ya muthu uyu ndipo ndipo ndiyemwe anapangitsa kut athu azivutika mpaka lelo
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 6 күн бұрын
Akulesa bwanji ma pephelo akuopa chani tiyeni nazo pephelo ndi chida
@MarriamBakalie
@MarriamBakalie 4 күн бұрын
Mtambo ndiwe galu kwabasi usamawapusise a 🇲🇼 anthu anakuona kale galu iwe zako zinada kale machende ako osavinidwa mbudzi
@taombeedward5026
@taombeedward5026 3 күн бұрын
The biggest problem mtamboyu
@user-wz1or9ud9i
@user-wz1or9ud9i 5 күн бұрын
Mzimu wa chilima awasowetse mtendere anthuwa mpaka anfe amene anapha chilima.
@GoodluckMwenifumbo-dk8jk
@GoodluckMwenifumbo-dk8jk 5 күн бұрын
Anthu ambiri osutsa pano ndi a MCP Zoona mpaka kuwaopseza amipingo,a MCP mwafikapotu
@AngellachifundoMwale
@AngellachifundoMwale 4 күн бұрын
I feel hurt mukamaimabr apaa nkumafuna kutinamiza kuti tikuvotereni sibwino unduna wanu inuyo munapangapo chani antambo nde lero muzinena ngati inu anzeru ??? Kutiona kupusa Malawi sichoncho
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 5 күн бұрын
Good Messnge Mr Mutambo
@abwinoamatani4921
@abwinoamatani4921 6 күн бұрын
Nanunsotu mukutichitsa manyazi, 60 eyes ndekuti chani?
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 6 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@LimbikaniMakwandu
@LimbikaniMakwandu 5 күн бұрын
Only chilima not you mtambo RIP CHILIMA
@user-lz4kc5ob1t
@user-lz4kc5ob1t 5 күн бұрын
inetu ndimangokuveran anyamata a mcp ndimaziwa kt simunakumane nazo uyo mtambo ngat ndinu madolo kkkkk
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 күн бұрын
Mtambo mtima wake ndi wadyera mmene wachoka ku MCP akufuna apeze not adzidyera kudzera kwachihanna ndiye in leronso asabwere ndimabodza ake ofuna podyera watipwetekesa ngati dzikoli Lili pamoto nfichifukwa Cha iyeyu ndi galu kwabasi
@MorrisMapiri-d6z
@MorrisMapiri-d6z 4 күн бұрын
It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.
@nicholasshema9016
@nicholasshema9016 4 күн бұрын
Awawa anachoka value cz iyeyi akusapota Chihana Athu akuwauza apa kuti apite chitsogoro ndi achipani chinaso so he z speek speechles
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 5 күн бұрын
Amtambo naye ine ndinakhumudwa naye ndipo ndinataya chikhulupiriro mwaino mwatulukirano nthawi yonseyi munali momwemotu mu Timbaland wakudayo ndiye pano mukutinamizaso chani apaa iyaaa😊
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 6 күн бұрын
no no anthu mzimvetsa zinthu u know very well kuti 6 july ndisiku la padara kumalawi ufulu omwe mkulankhupa lero nkhani yake ndi 6july nde mmafuna asiye za 6july apange za ma candle aa imfa si ya chilima yekha ati anthu akufa dairy .
@SajeFurniture-wj1ue
@SajeFurniture-wj1ue Күн бұрын
Nkulu wake yemweyu anatibweretsera mavuto, how can we trust him
@GibsonBakha
@GibsonBakha 5 күн бұрын
Andale inu musamatiwawitsemutu muma gofuna ndalama agalu inu
@KenChitete-pg3ws
@KenChitete-pg3ws 6 күн бұрын
Vote yanga yikupita kwa afford
@vinceynyone6693
@vinceynyone6693 5 күн бұрын
Viva mtambo Viva🔥👏👏
@WilliamTemboh
@WilliamTemboh 6 күн бұрын
Km tkukhulupilileniso amtambo kapena mukufuna tindalama plz tell me coz munatpweteketsa
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 6 күн бұрын
Apitenso pansewu atibwenzere dziko lathu...ndiyemweyu adatipereka
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 6 күн бұрын
Ndipo ndi yemweyu analisiya dziko ku anthu otamba akewa, apa angotibwenzerapo dziko lathu lakale lomwelija
@HenriqKwilasi2022
@HenriqKwilasi2022 5 күн бұрын
Iwenso ndi mfiti chifukwa ukupanga za ndale mtambo
@SylvesterHarry-n7c
@SylvesterHarry-n7c 6 күн бұрын
Timothy mtambo adali momwemo adagwiramo ntchito palibe chimene adapanga nduwadyera uyu
@user-qs2tx7wt6g
@user-qs2tx7wt6g 5 күн бұрын
Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa
@promisegregory8397
@promisegregory8397 5 күн бұрын
Amalawi wake up Mtambo ndi kape this guy he is after Money ndi kape machende Ake,amangofuna Ku watenga amalawi ngati makape
@nafejonga972
@nafejonga972 6 күн бұрын
Rest in peace, my president .. we are still fighting
@YahayaUndiya
@YahayaUndiya 6 күн бұрын
Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo
@jelsonmlowoka8611
@jelsonmlowoka8611 5 күн бұрын
Anali momwemo mu galawundi bwanji zinamukanika
@user-uk3bz1hr5t
@user-uk3bz1hr5t 5 күн бұрын
Mtambo you are a reason behind all this problems malawians are passing through,You escalated demoz that paved a way for MCP to get in power,see now where we are now.😢
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 күн бұрын
Mtambo was a Minister anapangapo chani? Amuchosa lero azioneka wanzeru? Ndale zopusa izi. 6 July mapemphero anali ku BICC basi.
@ChilangoNdalama
@ChilangoNdalama 6 күн бұрын
Big mtambo timakunyadiran
@CharityKangulero
@CharityKangulero 6 күн бұрын
❤❤❤ Exactly
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 4 күн бұрын
But we needs people who can at least change something in this country 😢😢apart from this government that we have now😢😢
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 6 күн бұрын
Politics will never transform Malawi. I suggest,all party presidents,some traditional and religious leaders should jointly accost the H E and matters of philanthropy and patriotism concerning current national teasers.Neither invective nor censure wll bring democratic solidarity in our beloved nation.There is need for deliberation with the HE and his Vice President.Avoid self centredness,power hunger, political chauvinism and cupidity.We are no longer ease!
@henryphiri6100
@henryphiri6100 4 күн бұрын
Chilima anaphedwa ndi Zikhale Ngoma,Chimwendo,ndi Kunkuyu.
@georgenundwe
@georgenundwe 5 күн бұрын
Why do we choose kusadziwa pamene everybody knows pretty well kut kuli global crisis ya economy.....and one expects milakuli that we do best than the lest ....lets.be the champion of telling Malawians the.truth
@estherkambewa7791
@estherkambewa7791 4 күн бұрын
Eeesh zoopsya, taking advantage on poor people.
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 күн бұрын
Kodi zoti nsewu ukulimidwa pano sakudziwabe Mtambo? Kapena anatuluka mdziko muno? Anthu ndale mumapanga mosaganiza sure. Mapemphero adasanduka nsonkhano wa ndale? Useless politicians with no future
KWAGWANJI - KUSANTHULA ZOMWE ZACHITIKA KU UTM 12 July 2024
1:16:26
UTM YATHETSA  MGWILIZANO LIVE LIVE MOTI ZOMWE AYANKHULA NDI IZI
23:38
Malawi Trends TV
Рет қаралды 69 М.
Мы никогда не были так напуганы!
00:15
Аришнев
Рет қаралды 6 МЛН
Final muy increíble 😱
00:46
Juan De Dios Pantoja 2
Рет қаралды 54 МЛН
Abusa akuti vote yao atengapo anapanga mistake❎ 😂😂😂
24:19
Malawian Cameras
Рет қаралды 22 М.
Evance Meleka... paying last respect to soldier Lucius Banda
2:52
Gabriel Banda
Рет қаралды 27 М.
Akufuna kupha mafumu a ku Ntcheu; Umboni wa mfuti 400 tili nawo
8:45
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 78 М.
KAMLEPO KALUA KUYANKHULA MOSANYENGELERA
29:23
HOT 265
Рет қаралды 35 М.
BON KALINDO LERO PA 12 JULY 2024 | KUPITILIRA KUNG'ALURA |
15:11
Dr Sam Kazibwe: Kiki ekituusizza Ruto ku bizibu bino byonna?
48:01
SamKazibwe Dispatches
Рет қаралды 4,1 М.
M'busa Yasin kularika mwa mphavu pa maso pa Chakwera ndi anthu onse
9:54