Tanzania Vs Malawi Lake Dispute PART 2

  Рет қаралды 49,961

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

3 жыл бұрын

Mkangano olimbirana Nyanja pakati pa dziko la Malawi ndi Tanzania PART 2

Пікірлер: 110
@user-dk6yc8pl2m
@user-dk6yc8pl2m 4 ай бұрын
Kod ka sound ka munakapeza bwanj bro sound nd history zimagwilazana kwambili
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
This is very nice story to hear. Big up
@dalitson3558
@dalitson3558 3 жыл бұрын
Ndimakunyadilani braz keep it up
@hamdanmasuku4800
@hamdanmasuku4800 Жыл бұрын
Kamuzu anali wankhaza km pa nkhan iyi anayetsetsa kuonetsa luso lake thank u
@lonelynyirongo1523
@lonelynyirongo1523 3 жыл бұрын
Tanzania must stay away from our lake pls
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Azungu ndi kale anayamba kumenyanisa anthu akuda vuto ndi lakuti wakuda ndi watulo
@Littlefair7
@Littlefair7 3 жыл бұрын
You're right but akuluwa all their presentation amalimbana ndi mcp ndi zinthu zakale zomwe sitingazisinthe pano, za ziiii zeni zeni.
@wilsonephraim5606
@wilsonephraim5606 2 жыл бұрын
ngati kumalawi kuli nkhani zikulu-zikulu zomwe ndimakhala nazo ndi chidwi kwambri kut ndizidziwa mmene zikuendera imodzi mwa izo nde ndi iyiyi
@chembamisasi6983
@chembamisasi6983 3 жыл бұрын
Tsono Mozambique inatenga bwanji mbali inayo chifukwa zikuoneka kuti nyanyai inali imodzi komanso Likoma ndi Chizumulu Islands zili mkati mwa Mozambique
@alfredbanda1693
@alfredbanda1693 11 ай бұрын
We have a well documented agreement about that but not with you
@richardthera603
@richardthera603 3 жыл бұрын
Nkhani ili ku court palibenso kuti ma president angakambirane za nkhaniyi. Anapita kukakambirana zina!
@ericbishopjere4494
@ericbishopjere4494 3 жыл бұрын
I like watching these videos they r full of information
@haroonharoon1957
@haroonharoon1957 8 ай бұрын
Thanks for your information
@MarkManyowa
@MarkManyowa 23 күн бұрын
If Africa is one then why are we fighting one another? 🇹🇿
@boscotonny4273
@boscotonny4273 3 жыл бұрын
Great work Fam!
@thokokabanda5227
@thokokabanda5227 3 жыл бұрын
Thanks a lot.
@shadreckpatrickmkisi8819
@shadreckpatrickmkisi8819 3 жыл бұрын
Thanks for sharing this
@yusufkassimlumbemajawa7187
@yusufkassimlumbemajawa7187 2 жыл бұрын
Inu big ulemu wanu ndinthu Allah be with you
@danielchikota2857
@danielchikota2857 3 жыл бұрын
Take out this imagenary boundaries is not for us
@user-xp7ig3rk1d
@user-xp7ig3rk1d 2 күн бұрын
Nice
@stanleydamalekani2398
@stanleydamalekani2398 3 жыл бұрын
Nkhani iyi ndiyovuta kwambili chifukwa pali map awili
@aliuyuli7945
@aliuyuli7945 3 жыл бұрын
Well narrated
@stanleydamalekani2398
@stanleydamalekani2398 3 жыл бұрын
Kupita ku Tanzania President chakwela sanslakwitse chifukwa kutenga nyanjayo sangatenge popanda zokambilana chifukwa aliyese amaloza chake ndi chikhulupililo.
@HusseinMachemba
@HusseinMachemba 2 ай бұрын
Kom aide kudikilabetu kt kod zinantha bwanji kapena anatilanda basi
@crosbeygondwe5403
@crosbeygondwe5403 Жыл бұрын
Keep it up broo
@PatrickChilunga-pg4lt
@PatrickChilunga-pg4lt 2 ай бұрын
Solution is one Africa,or choose to remain puppets.Mzungu divided Africa.
@zeckbmalawi8017
@zeckbmalawi8017 8 ай бұрын
We always love you sir
@danielchikota2857
@danielchikota2857 3 жыл бұрын
We are devided not by our choice
@bestonjoseph2193
@bestonjoseph2193 3 жыл бұрын
Where are the records of the boundaries
@oliversichela5657
@oliversichela5657 Жыл бұрын
British are a problem even us here in Zambia we are facing the same problem over one part of our country
@user-uf9mn1du3h
@user-uf9mn1du3h 2 ай бұрын
Keep it up
@umaliisah6920
@umaliisah6920 3 жыл бұрын
We follow u
@OustinYusuf
@OustinYusuf 4 ай бұрын
But why this President he go there to do what chakwera is very crazy This is lake Malawi
@manessmandebvu5888
@manessmandebvu5888 3 жыл бұрын
Taziwa ndithu
@issacdiaton6526
@issacdiaton6526 3 жыл бұрын
Mumakwana brother ulemu wanu koma nanja ndiyathu ife a malawi
@blessingsngwila4858
@blessingsngwila4858 2 жыл бұрын
I like ur information my brother ur the best
@LusajoNgabo
@LusajoNgabo 4 күн бұрын
try us
@PaulMkandawire-oo7by
@PaulMkandawire-oo7by 14 күн бұрын
So pali pano ili mumanja mwa ndani
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 2 ай бұрын
Bolaso bakili abale amaziwa story
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Chakwera mbola munthu wothawa dzamulungu
@osamabinraden9391
@osamabinraden9391 3 жыл бұрын
💪😎🙏🙏🙏👍👍👍
@leonardjika2100
@leonardjika2100 4 ай бұрын
AFTER MY ORTH OF THE OFFICE OF PRESIDENT NO ONE WILL CLAIM OUR WATERS SO HELP ME GOD
@hajaleemalinjemuhammad219
@hajaleemalinjemuhammad219 3 жыл бұрын
We must stand up ✊💪 and to say nyaja ndiyathu chifukwa zikungooneselatu kut nyanjayi ndiyathu our president must know this " if he continue to keep quiet about our lovely Lake Malawi one day it will be ruling by Tanzania for sure, president wathu akuyenela azuke ateteze nyanja imeneyi Tanzania akula ndi maboza basi
@lutufyodixon9997
@lutufyodixon9997 3 жыл бұрын
It's a lake of no one. Every country should enjoy richness of natural beauty of africa
@hajaleemalinjemuhammad219
@hajaleemalinjemuhammad219 3 жыл бұрын
I think your sarvege, you don't know what are you talking or even! Can you look oldest map and then you must look the last map you can find that Lake Malawi is belongs to Malawians not Tanzanians, and if you follow this history properly you can see that all VIPs of Tanzanians was accepted that all parts of Lake Malawi is belongs to Malawians not Tanzanians "so today there is no way to come Tanzanians and craim about our lovely Lake Malawi". And don't say we should keep quiet to allow Tanzanians get profit for our lovely Lake Malawi no! Yes we know that we're neighbours nde asatilowe choncho chifukwa nkhaniyi ikuoneselatu kut nyanjayi ndiyathu look before it's two times that British were used this oldest map for boundaries of Malawi and Tanzania that means Lake Malawi is belongs to Malawians. This Tanzanians they just have a jealous for us because we can get rich easily through this Lake. All and all Tanzania must stop dreaming about our lovely 💗 Lake Malawi.
@jimmyjay9950
@jimmyjay9950 3 жыл бұрын
@@hajaleemalinjemuhammad219 I don't understand when u said u will be rich coz of that lake maybe u forgot one things that Tanzania is richest when it comes naturally resources ..u guys are talking about lake Tanzania as alot of them such as Victoria,manyala , Tanganyika to mention few so stop dreaming my brother
@hajaleemalinjemuhammad219
@hajaleemalinjemuhammad219 3 жыл бұрын
@@jimmyjay9950 the things that am talking is already documented that Lake Nyasa is belongs to Malawians so you guys your busy to claim the thing that is not for you,. You must stop that and it seems that you don't know history of Lake Nyasa, l quiet you
@luganoessom1464
@luganoessom1464 3 жыл бұрын
@@hajaleemalinjemuhammad219 probably you are right but there is no water bodies between two countries which are under control of one country,and Tanzania will not control this lake never they have their own part and we have ours but taking it completely from them is a worst idea because we will take it but we will never enjoy it and it's resources. We will be paving the way for terror attacks across the lake.
@Satier47
@Satier47 10 ай бұрын
😢 pa chakwera😂😂😂
@MikeSenki-pj3ns
@MikeSenki-pj3ns Ай бұрын
zili pati pano
@richmanjimmy271
@richmanjimmy271 Жыл бұрын
KOMAIYAMBA RITI OROINANTHA ZIRIPATI
@richmanjimmy271
@richmanjimmy271 Жыл бұрын
ZIRIPATI ZAHISITORE YANYANJI YAMARAWI NDITAZANIYA
@salaam1089
@salaam1089 2 жыл бұрын
Kkķkkk umantha mbare
@isaacmbewe5585
@isaacmbewe5585 Жыл бұрын
No ya 48 ndi no yomwe ili kumapeto kwa no ya Track driver Jason moyenda yemwe anakwatila mwana wa achemwali anga anamwalila akhala ku Lilongwe ku Likuni ndipo amayigwilitsa ntchito akabwela kuno ku Zambia
@isaacmbewe5585
@isaacmbewe5585 Жыл бұрын
Komaso iyo no ya 79 ili kumapeto kwa no yomwe ananditumila mkazi wina ndipo dzina lake anandiuza ati ndi charity sinikudziwa komaso nombalayo siyamuno mu Zambia iwoneka inachokela dziko lina
@isaacmbewe5585
@isaacmbewe5585 Жыл бұрын
No INA ya 48 ku last ndi ya Saulos Ngulube mwana wa akulu apingo opuma kudela kwanthu.
@mwamibukulu7745
@mwamibukulu7745 3 жыл бұрын
if two countries bordered by water bodies the center of the water bodies must be its border!!
@hassanjameskananjie9349
@hassanjameskananjie9349 2 жыл бұрын
What nonsense it is this
@ibrahmdoka7486
@ibrahmdoka7486 Жыл бұрын
The lake belongs to Malawi
@zachariahlungu3577
@zachariahlungu3577 2 жыл бұрын
Zikomo bambo
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 жыл бұрын
A chakwera ngombwambwana sangatenge nyanja
@brightphiri8657
@brightphiri8657 3 жыл бұрын
tiziti muja anabwera president waku Tz ku malawi ankalamulira ndi chakwerayo? nkhani ya ma neighbours sinyanja yokha.ma president amumbuyomu sanaithense nkhani yanyanjayo mbwanji? musaiwale kuti malawi it's a randlocked country tikumafuna ma neighbours munjira zambili nkhani sinyanja yokha.
@brightphiri8657
@brightphiri8657 3 жыл бұрын
and palibe anganyamule nyanja, nkhaniyi njongokambilana,
@brightphiri8657
@brightphiri8657 3 жыл бұрын
iyayi nkhani siimeneyo dziko silingayime kuyenda chifukwa cha nyanja. pali zambili zomwe tanzania ikufuna kumalawi and malawinso chimozi mozi ikufuna zambili ku Tz .that's why mukugona kuti ma president onse akulephera kuyithetsa nkhaniyi koma mayiko akuyendabe.
@brightphiri8657
@brightphiri8657 3 жыл бұрын
and mundimvetsetse achikulire moti panopa asodzi aku Tz akupha nsomba mnyanjamo full time chimozimozinso asodzi akwathu zawo zikuyenda.
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 жыл бұрын
Chakwera nchitsiru alibe nzeru
@user-ty7mc9mg1f
@user-ty7mc9mg1f 10 ай бұрын
Britain and German were wrong
@Thewarrior7093
@Thewarrior7093 10 ай бұрын
That entire lake belong to malawi 🇲🇼, that is why it is called lake malawi , Tanzania is just being selfish but i know that the whole lake belongs to malawi and TZ knows it
@MalangaMartin
@MalangaMartin 22 күн бұрын
🇹🇿 vs 🇲🇼
@luganoessom1464
@luganoessom1464 3 жыл бұрын
Hey guys let stop this stupidity ,how do you think is possible for the lake to be under control of one country and our neighbors will be there watching it and it's wave🌊 and fish 🐟, and watching us swimming?🏊🏊😁😁In normal sense that's impossible ,and none of us will be safe .
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 Жыл бұрын
Joint ownership is the key 👍
@josephzulu2372
@josephzulu2372 3 жыл бұрын
Those you think they were against Malawi on the Lake dispute issue, like Chisano, the stance they took was to bring peace between the two countries. What is wrong with sharing? If the lake is shared then the dispute will come to an end.
@cza421
@cza421 2 жыл бұрын
It's more sensible that the lake is shared.Its is not feasible that the shoreline should be the border line.What about the Tanzanians along that lake? Does it mean they are not entitled that lake? Malawi is been selfish on this one
@edwinchimbuto8364
@edwinchimbuto8364 2 жыл бұрын
@@cza421 tanzania has lake victiria.. its about the possibility of oil. they want a part of it.
@Littlefair7
@Littlefair7 3 жыл бұрын
Africa needs to unite and stop talking about mikangano ya nyanja, nothing wrong with Chakwera's visit to Tanzania, there is alot that malawi can learn from tanzania, koma akulu awa anada nayo kukhosi MCP, muphunzire kuyiwala zakale ngati mukufuna kupita chitsogolo, tonse timadziwa kuti Kamuzu anatizuza koma zinachitika and we cannot reverse whatever happened then, muziyankhula zomanga ndi kulimbikitsa osati zobwerera mmbuyo, africa needs unity now than ever before.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
Ndipo ngati simukufuna kumva zakale chomwe mukumakhalira jijirijijiri kumvera ndi chani? Pitani ku ma channel ena chifukwa apa amakambapo history basi. Sangasiye kukamba za MCP chifukwa MCP idapulura mtundu wa amalawi
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
Olo ineyo sindidzayikhululukira MCP mpaka kalekale chifukwa idapha amalume anga. Iweyo ndiwe chitsiru ukulankhula mopusa choncho chifukwa MCP sidaphe anthu kwanuko
@Littlefair7
@Littlefair7 3 жыл бұрын
@@bakilimuluzitv3371 Well said, I've exercised my democratic right and nowhere in my statement did i say our lake should be taken by Tanzania, but we don't need to fuel chaos where there can be a peaceful amd lasting solution, why do you wanna blame chakwera for visiting magufuli? That's wrong, you're wrong, we cannot be enemies with tanzania just bcos of a small lake, a thing that can be discussed and resolved peacefully, we're tired of wars in Africa, don't you see what's happening in DRC? If this lake malawi issue is not handled carefully innocent blood can be shed. Be careful brother.
@Littlefair7
@Littlefair7 3 жыл бұрын
@@charlesmuyaya8839 Tapitani uko achitsiru inu, olo musakhulukire MCP ndiye mupindula chani? Mukakhala inu ndiye amene Kamuzu anakupeperetsani, simukamba za nzeru, kupepera basi.
@Littlefair7
@Littlefair7 3 жыл бұрын
@@charlesmuyaya8839 Iweyo ukandiuze kuti ndisamonere, do you own this channel you idiot? Wayidziwa liti this channel? Ndinaymba kupanga follow this channel from its inception, ndimayamikira komanso ndimadzudzula, si ine ombwambwana ngati iweyo, mbuzi.
@nelitopedrofiniasse
@nelitopedrofiniasse Жыл бұрын
Espalhados
@jamesmhango2619
@jamesmhango2619 Жыл бұрын
Common sense : the border should be in between. Aristotle wrote about the golden mean.
@festongrido8189
@festongrido8189 3 жыл бұрын
Ndimbuzi ameneyu ulamuliro wamukanika
@dorikakamwendo6970
@dorikakamwendo6970 3 жыл бұрын
The lake belongs to Malawi
@wilsonephraim5606
@wilsonephraim5606 2 жыл бұрын
exactly !
@aoloathumani10
@aoloathumani10 Жыл бұрын
Go and take it
@anniekhonje7853
@anniekhonje7853 3 жыл бұрын
From my view Tanzania doesn't own it .All who brought this problems us is Britain..
@dastahchikwekwe7864
@dastahchikwekwe7864 3 жыл бұрын
Akuluwa amalongosola bwino nkhani koma ika fika pa Tonse alliance amayiwononga nkhani yonse seems like he doesn't like Tonse alliance for u to be good just explain what u know dont accuse anyone your stories will be good
@thokokabanda5227
@thokokabanda5227 3 жыл бұрын
Vuto ndi iweyo chifukwa umasapota tonse alliance. Ndie ukufuna asamanene chilungamo? iwenso ulibe nzeru. Tonse alliance yatokhala mulungu kuti asamayinene?
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
Uyu amanena za aliyense osati tonse alliance yokha. Umvere ma video ake onse Pena amanena za Bakili Muluzi, Pena za DPP, MCP. Samasankha, musiyeni munthuyu amanena zoona zokhazokha, sali ngati ma wayilesi okonderawa ngati zodisk ndi times
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 жыл бұрын
But he is right. Chakwera mmene ankabwera kuchokera ku tanzania ananenapo chani zokhudza nyanja? Chakwera is an idiot
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 жыл бұрын
And mu nkhaniyi wapanga blame peter mutharika, chakwera and even joyce banda. Ndie chomwe waonapo iweyo kuti walakwitsa ndi podzudzula Tonse alliance pokhapo? U must be insane
@peterkondowe9265
@peterkondowe9265 3 жыл бұрын
Nyanja ndi chilengedwe cha Mulungu ili chete yokomela aliyense. Kumbali zose ziwili ngati titamenyane chifukwa cha nyanja ovutika tikhala amphawi ife komanso ndalama za mafutawo zipita mumatumba mwawo nyanja isala yowonongeka. Mwachisanzo kayelekela tapindula nayo chani ngati ziko? ? Kuma wona zokakamila komanso a TZ ndima neighbours anatigawa ndi asamunda a satana osamayiwala kuti kale makola a navuka ndi zisilu anzungu kusiya kwawo kuzagawa ntundu
@brightphiri8657
@brightphiri8657 3 жыл бұрын
iwe ndi mbora ya reporter.moti siukuziwa kuti malawi ndi tanzania ndima neighbours? ukungoganiza za nyanja yokha bwa, ? kuganiza mopelewera and mopepera
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
Iweyo ulibe nzeru. Munthu wangodabwa kuti Kodi Chakwera athetsa bwanji mkangano umenewu ngati akupita nkumakamwelera nawo limodzi? Chifukwa olo mmene anabwera pa ulendo umenewu sanafotokozepo china chilichonse chokhudza Nyanja. Posachedwa pompa timva kuti Chakwera wapereka Nyanja kudziko la Tanzania. This narrator is 100%right
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 жыл бұрын
Chakwera nchitsiru alibe nzeru sangatenge nyanja.
@kondwanitembo386
@kondwanitembo386 3 жыл бұрын
@@danielmaluwa7896 pita ukatenge iweyo
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
Ndie tisiye kuteteza Nyanja just because a Tanzania ndi ma neighbours athu? Are you serious? Real president must protect the territory whatever the reason. Zina zonse zikuyenera kubwera pambuyo.
@spencerfweta733
@spencerfweta733 3 жыл бұрын
@@charlesmuyaya8839 Any drilling for oil or gas will cause havoc to the beauty of the lake and its flesh sparkling water
아이스크림으로 체감되는 요즘 물가
00:16
진영민yeongmin
Рет қаралды 57 МЛН
Cat Corn?! 🙀 #cat #cute #catlover
00:54
Stocat
Рет қаралды 15 МЛН
Tanzania Vs Malawi Lake Dispute PART 1
13:51
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 31 М.
Kamuzu Banda House|Ngulu ya Nawambe
2:36
My Malawian Life Experiences
Рет қаралды 79 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
BAKILI MULUZI KUCHEZA NDI BRIAN BANDA 11/05/2024.
58:38
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 29 М.