Kodi paja ka chipani ka UTM kali ndi ma MP angati paja? Chipani cha UTM chasanduka servant wa MCP womakaperekera madzi kumsonkhano kkkk
@BwanaGD2 ай бұрын
Gulu la amalawi opusa nde ndili anthu amalawi yose yachita kuwadziwa kuti ndi mbava zachita kupulumutsana ku onyolo nde mukutiuza ziti apa kupusatu uku simukuminabe ana anjoka inu
Nawo awa .kachipani kopanda ma Brunch ma Area .mukawinira kuti nanu
@user-hm9nc7lz6e2 ай бұрын
Mbava iwe panga zako ndi mbava mzakoyo chilima amalawi samuvotere
@user-vh9uk1jy7w2 ай бұрын
Mukunama guys
@thokoJames-gp8mk2 ай бұрын
Kusowa mfundo zowauza wanthu
@gladysbonongwe10382 ай бұрын
Za nzii
@user-ib6jc4es3s2 ай бұрын
Wakuba nagakhale wanzelu panyopanu
@moosakananji18792 ай бұрын
Inu mmalo moti muzilimbana tose allawas Kaya mati Chan kupusa
@thomluciouss73602 ай бұрын
If Peter is not going to win 2025,Atupele is going to rule Malawi not UTM or MCP your time is over
@OrtonKabbichi2 ай бұрын
Utm no mutu Malawi alipamoto Chifukwa cha makape inu
@maxwellchapita-df4tw2 ай бұрын
Zaziii
@LeahNundwe-wh6vz2 ай бұрын
Mukutitolatu andale inu Sitidya ndale ifetu tisiyeni osamatinamiza nti miyambi toti "maliro akatuluka mnyumba sabwelera" DPP yalamulira kawiri, MCP yalamulira kawiri nde maliro mukunenawo nde ATI?
@HarrisonMwanga-xy4sc2 ай бұрын
Iyaa president wao okuba awa,peter muthalika,okuba ndalama zathu kazache kumakangowalamula a bank mundipase,ndalama mwa kuti,kutenga ngati boma la nyumba mwao.utm,ndi chilima okuba ndi mwenye zina,lache ati Satan kaya zoputsa, mmalawi muno chasala, munthu akapedzedwa,ndi chamba osamugwila,okuba akagwile okubatso?tawabveni,zisilu pasipo .
@VictoriaWilliam-ms2ft2 ай бұрын
Zaziiii
@patriciakenmuir2 ай бұрын
Mavuto pa malawi
@ShabanIssa-il6nc2 ай бұрын
Mukanena kuti maliro sabwelera nyumba awondimaliro nanga akaziwa ndan kuti MCP itilamulanso kkkkk kusowa mfundo Achilima o ndi amene akusangalala chifukwa akudya ndlama zaboma ife tiyeni tizingolima bas kapolo sakwiya
@BASHILUMangwetu2 ай бұрын
Tachoka iwe zachamba basi mulowa kt
@NelsonKadzakayesa2 ай бұрын
Nkhope yomangowala koma boma lirilonse kumangokhala kupanidwa ku chitseko sikupusa kumeneko? Vice president wamtundu wanji womangoti sindiri pa chiongolero? Akhungu zimutsatirani popeza wakhungu akatsogola inu nkumamutsatira mumakagwera limodzi. Vice President wosalankhula a Malawi akuzunzika mesa ameneyu ndi uja ankati fetereza tidzagula 4,000 lero muli duuu kubisala chifukwa Cha boza koma umbava basi ndiye ntchito yomwe mumatha
@user-wm2sv8dw5d2 ай бұрын
kayatu😂😂😂
@user-hd7wq2yc6m2 ай бұрын
Chipani cha utm ndi chipani chakuba misonkho ya a Malawi pamodzi ndi chipani cha mcp ,utm musayembekezere kuti mungawine jiiiiiii mwakhululikilana mbava zokhazokha iwe ukuyowoya apo ndiwe wa mahala iwe? Chindere cha munthu kulya katatu kuli nkhuni? Feteleza wa K4495 alikuti ? 1 million jobs ilikuti ? Ivo vikuvina apo navyo vyavyamba vekhavekha uchindere pera munya anthu sakumveranisoni zokamba zanuzo zautsiru ayi mwagwa nayo
@MaxwellKaziputa2 ай бұрын
Mbuzi zenizeni, rubbish
@user-rg4du4vu9r2 ай бұрын
Zaziiii mwakhuta khuta uko mimbagwa nkumakuwa zinthu zopanda mutu apa muzithaima chaka chamawa ndipomwe muzaziwe kt khobwe sinyemba