'AMANDIYAMWISA MALISECHE DAILY '- MMWENYE AWUZA WA NTCHITO ADZIMUYAMWA MALISECHE

  Рет қаралды 55,187

Hanifa Mw

Hanifa Mw

Ай бұрын

MMWENYE AWUMIRIZA WA NTCHITO KUTI AZIMUSEWERETSA MALISECHE
Kupeza ntchito ndi chinthu chokoma kwambiri kwa munthu aliyense makamaka uyo amene wakhala nthawi yayitali akuyisakasaka ndipo ali ndi anthu amene amadalira iyeyo monga makolo, ana komanso mkazi. Pamene munthu wapeza ntchito ndiye kuti amakhala ali ndi chiyembekezo chachikulu kuti zinthu zake zisintha ndipo amene amamudalirawa ayamba nawo kukondwa. Komatu zimenezi sizili motero kwa mkulu wina wochokera mu mzinda wa Lilongwe. Mkuluyu amene dzina lake sitilitchula anapeza ntchito yophika kwa mmwenye wina a Jayesh Kumar Dalwad amene anali wothandizira ntchito za mkulu wa kampani ya Shayona Cement Corporation ku Kanengo analibe malingaliro akuti chimwemwe chake chakuti wapeza ntchito chitha posachedwa ndikuyamba kukhala moyo wa mavuto.
Atakhala kwa nthawi yayitali asanapeze ntchito, mkuluyu amene amakhala kwa Mtsiriza mu mzindawu anali akukanika kusamalira ana ake atatu, koma mu mwezi wa January 2023, iye anapeza ntchito ngati wophika ku nyumba ya bwanayu imene ili ku malo amene kuli ma office a kampani ya Shayona yi ku Kanengo. Atangogwira ntchitoyo kwa mwezi umodzi, mwezi wotsatira wake umene ndi wa February zinthu zinayamba kusintha ndipo akuti abwana ake aja anayamba kumamawuza kuti adziwasisita bondo lawo.

Пікірлер: 51
@MelissaMondey
@MelissaMondey Ай бұрын
It's bad!!!😢😢😢 plz amalawi munthu ameneyo amangidwe
@AndyGama-m3u
@AndyGama-m3u 5 күн бұрын
Ayi wachitola chikwama Nanga ma million onsewo pajatu ndalama zilimunyasi
@user-ey6in8is5h
@user-ey6in8is5h Ай бұрын
Mumabweretsa nkhani zofunikira koma musinthe speed yamalankhulidwee
@sharonicier001
@sharonicier001 Ай бұрын
Ndipodi ife kuti tinve bwino bwino palitu ntchito 😂😂😂🤣🤗🤗
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn Ай бұрын
Mwina ndi manyado,ineso sizimandiwaza
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje Ай бұрын
Muthu kwanu ndimulolela kupanga zimenezo zaziii zauchisili ngati zimenezo
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj Ай бұрын
Umphawiwo wakula bwanji mpaka kuvomeleza zimenezo bwanji osawulura kapena kusiyana ntchitoyo kuyamba zochita zina
@mercynamangale98
@mercynamangale98 17 күн бұрын
Aaaaaa zauchitsiru basi,amangidwe ameneyo basi
@IsaacMwale-hu9kg
@IsaacMwale-hu9kg 24 күн бұрын
God have mercy on us
@e.r.mchanel1460
@e.r.mchanel1460 Ай бұрын
Eishhhhhh zosayenda bwanji
@user-xe3xo5mu9k
@user-xe3xo5mu9k Ай бұрын
Aaaa zanchamba bass Iyeyoso anagwirizana nazo bwanjibosangosiya nchitoyo bwanji nonse machende anu 😂😂😂😂😂😂😂
@giftblack7690
@giftblack7690 Ай бұрын
Hahahaha ine olo zitavuta maka sindingapange zauve ngati zimenezo
@HellenGondwe-d1g
@HellenGondwe-d1g 15 күн бұрын
Mpaka Chaka kumalorera zimenezo mavuto ake amtundu wanji
@CollinSepamatla-xk2lw
@CollinSepamatla-xk2lw 18 күн бұрын
Mchitsilunso bwanji ameneyo
@user-lf6qf2tw5o
@user-lf6qf2tw5o Ай бұрын
Km guys kwathu komwe tizilandila nkhanza zoterez amalawi ena kumavomeleza km mmm 😢
@ElediaChingoma
@ElediaChingoma 19 күн бұрын
Eshiiii
@StellahChikupira
@StellahChikupira Күн бұрын
Kulakwa 😢
@EmmanuelMoyo-hy5ni
@EmmanuelMoyo-hy5ni Ай бұрын
Umphawi ndi mavuto
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 28 күн бұрын
Amangidwe mwenyeyu
@PetroJack
@PetroJack Ай бұрын
Sad
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly Ай бұрын
Osamuluma nchilawakewo bwanji kkkkk ndikuluma maphwala akewo bs yesyes kkkk
@twavysibale4751
@twavysibale4751 Ай бұрын
We shouldn't Allow this in Malawi, that's not acceptable here,..
@IdiWilliam-uo8tw
@IdiWilliam-uo8tw Ай бұрын
Koma ndikhani iyiyi boma lamalawi limayenera kumuitanitsa mwenye ameneyu kuonetsa kukwiya nazo
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Ай бұрын
Boma lake litiro brother???😂😂😂😂😂
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Ай бұрын
Osaiwala kuti Chakwera ndi chilima nawonso ndiodanatu ndi chilungamo ndie izi zangoyenera kumachitika basi
@FloridaOssy19
@FloridaOssy19 Ай бұрын
Mmmmmm 😢😢😢😢
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Ай бұрын
Boma la Tonse Alliance ndilodana ndi chilungamo nalo ndie atha kukamumanganso bambo olakwilidwayi poti
@RobertKwazizira
@RobertKwazizira Ай бұрын
Umfiti amabungwe loweleranipo chilungamo chichidwe basi
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem Ай бұрын
Umphawi szinthu
@UmariBakari
@UmariBakari Ай бұрын
Channel ichi ndichonama
@charityamos2183
@charityamos2183 Ай бұрын
Uchisiru bas
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 13 күн бұрын
Kupusa bwanji samakadandaula ku ma bungwe ndi opepera
@mercybwanali-qe3dv
@mercybwanali-qe3dv 27 күн бұрын
Chanma lindimo umo😂
@GidionJonas-sr4zr
@GidionJonas-sr4zr Ай бұрын
Iiiiii shaaaaa!!!
@CatherineDesire
@CatherineDesire 11 күн бұрын
,,,😂😂mzimaiyo akunama amafunanso nae amagwilidzana naeso akufuna chipepetso eti 😂😂😂😂🤸🤸🤸🤸🤸
@ChikondiKwengwere
@ChikondiKwengwere 4 күн бұрын
Sinzimayitu
@juniortsegula3847
@juniortsegula3847 Ай бұрын
Asaaaa 😂😂
@MilacleSankhani
@MilacleSankhani Ай бұрын
Km ndye bola andicose ntcito
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
Mmmmmm koma abale zina ukambva yohhh kukhwima kapena?
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 27 күн бұрын
Munthu ukuvutika kut ukufuna ntchito umapanga chitheka so I don't blame him ndipo iyeyo amkafuna kusamala ntchito komanso amkakukumbikila mavuto akwao koma munthuyi adangokhala oipa basi
@ErnestAllex
@ErnestAllex 21 күн бұрын
Chitsiru ndiiyeyo vuto longochoka koweta ng'ombe 😒😒
@mercybwanali-qe3dv
@mercybwanali-qe3dv 27 күн бұрын
Nseu wamangochi wu zikukhala bwanji?
@user-hp4rl8cv3h
@user-hp4rl8cv3h Ай бұрын
Why Malawian we allow such pple
@janemsiska3345
@janemsiska3345 28 күн бұрын
Zovuta aaa
@augustMag
@augustMag Ай бұрын
Bad news 🤔🤔🤔🤔
@clementMuyafula
@clementMuyafula 24 күн бұрын
Amabungwe kuno changu
@lonnythom
@lonnythom Ай бұрын
Koma amwenye sazatheka 😢
@mailos.laisoni7001
@mailos.laisoni7001 16 күн бұрын
Ndipo kwambiri
@FatimaRehemah-gi4mp
@FatimaRehemah-gi4mp 13 күн бұрын
ma gay achimwenye🤨🤨🤨
@alickkachepa3801
@alickkachepa3801 19 күн бұрын
Mmmmmmm zotsayenda
Heartwarming: Stranger Saves Puppy from Hot Car #shorts
00:22
Fabiosa Best Lifehacks
Рет қаралды 20 МЛН
Самое Романтичное Видео ❤️
00:16
Глеб Рандалайнен
Рет қаралды 4,6 МЛН
버블티로 체감되는 요즘 물가
00:16
진영민yeongmin
Рет қаралды 110 МЛН
Nancy vs Che Nkope - Zikhale Ngoma Kapena Drums?
10:46
CHE NKOPE
Рет қаралды 26 М.
Gibo walila tritah atathesa chibwezi....
7:04
Sam Malvitha
Рет қаралды 41 М.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 91 М.
Ekedi na Sekuru Kanengo padare kuchiweche akafira pasowe cheshomba part 7
1:26:08
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
Raila: Be aware of the WRATH of history
23:42
Herman Manyora
Рет қаралды 42 М.
MMENE JOE GWALADI ANAPANGIRA MA MILLION AKE
13:30
Hanifa Mw
Рет қаралды 26 М.
Mkazi Wasanduka Njoka Tikufuna Kugonana
16:09
Hanifa Mw
Рет қаралды 25 М.
ZOMWE AYANKHULA A NAMIWA
32:47
HOT 265
Рет қаралды 47 М.
Heartwarming: Stranger Saves Puppy from Hot Car #shorts
00:22
Fabiosa Best Lifehacks
Рет қаралды 20 МЛН