We are not fools and we know where this story of Usi coming from, it started the night just before plane crash.
@chrisschikozera727117 күн бұрын
Agofuna kupusisa amalawi
@DanielMwandira15 күн бұрын
Koma why Malawi Mulungu akuloleranji izi Ku Malawi kut mpaka anthu azingoonerera chonchi
@chrisschikozera727114 күн бұрын
@@DanielMwandira gwirizano tilibe kaya ku Malawi zinazi magoona waziyamba we all know the history and history is best teacher ever bt wht happen now we bring old vision again in this country
Ali ndimphavu yanji yoposa lamulo sizongoganiza akulu izi.
@gladyschisomo432418 күн бұрын
Ayi ndithu manganya anali kale wachiwili kwa saulosi nde mmene adapitila a top awo otengedwa akuyenela kukhala wachiwiliyo basi ndipo amene adasankha manganya anali chilima yemweyo apa Mzimu wake wasangalala komwe aliko ngakhale adachoka imfa yosakhala bwino
@estherkambewa779118 күн бұрын
Constitution imati president asankhe
@user-fd1tu6ku1r18 күн бұрын
Michael Usi ndi wa MCP ndi kale
@hedgespophiwa18 күн бұрын
Is only the black box osati china chilichonse so we r waiting for the voice recorder
@augustMag17 күн бұрын
Mai Kaliati ayakha bwino Manganya apeza yekha mayakho
@user-lb6ek3ee6d18 күн бұрын
Zachamba Usi azazitenge ngati iye ndiwochenjela mission yawo yatheka koma asayiwale kuti masiku amatha ndikugona tsiku lina tidzalilaso maliro ayiye
@azunguauskay490318 күн бұрын
Iwe ukunena chilungamo
@Certified-Mbudede0417 күн бұрын
God"s time is always the best.. Not an MCP fan nor UTM but the President apanga zomwe akufuna when it comes to that
@AleksaWilliams-qc6cn18 күн бұрын
A utm kuona kwanga akanangojoina zipani zina monga udf,dpp,aford ndi zipani zina,osati mcp ayi ,,koma poti zamumtima ndizawekha iiii kaya
@LamekiSamson16 күн бұрын
Ndipo ndizoona
@RichardMatandala18 күн бұрын
U T M idapta ndanuwake bas tivomekeze
@petertaulo801418 күн бұрын
UTM is here to stay don't worry
@ulemujumbe850118 күн бұрын
Basi chidamka mchilima
@VictoriaWilliam-ms2ft18 күн бұрын
😂😂Zonama basi mwaiwala munatiuza kuti mgwirizano mwayedzeka kaye? Something fishy
@eliffagondewe821418 күн бұрын
Ndipo zodabwitsa lero akuwoneka okondwa zedi even mkaka himself 🙌
@thomasmfune515015 күн бұрын
Martha Chizuma analiso ophunzilabwino but she failed to beat the system. Money has special energy.
@LindaKapito18 күн бұрын
Anthu akubwela akafukufukuwo,mwawachuna kale azafotokoze za ziiiiii ,
@chitanibenito110918 күн бұрын
Anthu opanga kafukufuku opezedwa ndi boma sangagwire ntchito mosakomera boma, sizingatheke zachinyengo basi. Ndalama za misonkho ya a Malawi muzingoonongabe choona mukuchiziwa koma kufuna kuwapusisa a Malawi ayi tiyeni nazoni. God is watching.
@NgomaRaheem18 күн бұрын
Abasankhana kma nthawi ikuza nose muzasetera leza sua Mkaka wasangalalano cz Chilima wapita
@momuumro18 күн бұрын
We are not fools we know everything and we know from where you started your plans So Usi don't be clever here zimene umafuna zatheka komanso zimene amafuna chakwera zathekanso
@Edson-sj8vn18 күн бұрын
Utm tapachika basi Mai kaliati mokupemphani bwelerani ku chisa mbiri yanu isanaonongeke
Akatswili ofufuza achani zinthu zooneka ndi maso akazitape a utm amatenga zokambilana kupititsa kwa farao mpaka kumukhonzera chiwembu koma akhumudwa chifukwa samaembekeza kuti solution ikhara njila yakupha
@CholapitsaSamson18 күн бұрын
Man mumangomatula nkhani basi aa zosabeba L
@Tawina010118 күн бұрын
😮sono mumafuna azipanga bwanji????
@masingatichilumba826318 күн бұрын
Zofuta sindu sake😢😢
@user-et3il7pi7t18 күн бұрын
Ndizowona kupanda utm mcp siyikanawina apo musamachosele
@HitSmart-q9o17 күн бұрын
Zaipa😢
@AliceChipeta-pc3nb18 күн бұрын
Ngwirizamo wayambilaso simesa tinayezela Kaye ndale timapanga usiku ok ok
@MakandeMpambalika17 күн бұрын
Kaliyati so brief
@user-xt2gu9yt9q14 күн бұрын
Frim yao yatheka ife timadziwa koma dzopanda mphindu komabe oooo
@LamieTiger18 күн бұрын
Athu nde mwakula kula koma kumapanga zoputsa m'malo momalapa machimo mulinawowo anyday imfa ikubwera
@BorgeMario-wx5vq17 күн бұрын
Chilima akuona zonsezi.pitilizani ndi ufiti wanuwo.
Koma chakwela uli ndi sambi.. kusunga mgwilizano kwa bwanji uku? Munthu oyipa iwe
@D.RJALLI-qo6yd18 күн бұрын
Farkas utm ur are the full iwe ausi mbolo yako iwe galu
@HalisonSolomon17 күн бұрын
ZAUSIRU USI NDI MUNTHU YEMWE ANALI NGATI SIMONI PETRO ODZIWA MOMWE ANGAPEREKERE YEDU KUTI APHEDWE USI SI WA UTM USI NDI WA MCP NDIPO AMALAWI MUSAONENGATI USI ANGATHANDIZE MAKAWI CHIFUKWA UYU ALI LIMOZI MU MCP ,
@OmegaSanjama16 күн бұрын
Mungoononga ndala kutenga anthu akunja kudzafufuza kod kuno kulibe akadauro ogufunza iwo afufunza bwanji dziko lino ndi lanthu t
@MaryChavula-jz3di17 күн бұрын
Anthu andale ndi oipa ndipo asamatipusitse koma adziwe naye kuti adzaziwona zomwe Ankawona chilima ndi anzake
@user-xe5lb4uf3n18 күн бұрын
Kafukufuku azatiuza chiyani bodza limenelo akafika muwauza zochita. Malawi akudikilira Limpopo Fm ndi Bakili Tv
@fradrickMuvula18 күн бұрын
Great
@Certified-Mbudede0417 күн бұрын
Y'all saying Usi had a plan on this!. Where are your heads. Akanayisiya UTM you could have been talking kuti it was also a plan!.. Tamaganizani pena xina kumangoona. Sizoti mungasithe VP inuyooo aah
@VictoriaPwele6 күн бұрын
😮
@user-si7po9sd5i18 күн бұрын
Tiyedzeke kaye
@mkhulukinyata519814 күн бұрын
Ine mukamamutchula uyu Ernest Thindwa yu kuti ndi Kaswiri pa ndale" Ayi ndithu ine zimangondiseketsa kuti yaaa ku Malawi yee kkkk.. Munthu wamzeru zake sangamayamikire Chakwera pomusankha Michael Usi kukhala Vp ayi . Ife monga a Malawi " Chomwe tikudziwa ndichoti Michael usi wangosankhidwa ndicholinga choti awaphimbe a Malawi kumaso " Ndicholinga choti tidziti kuti Chilima sanaphedwe ndi iyeyo Chakwera yo
Tikudikila mwana wa chilima Sean kuti adzapitilize chipani Cha bambo ake ngati president
@user-og4oe5yp4w17 күн бұрын
Germany, France,u.s.a Israel ndi amodzi palibe angapereke zotsatira zabwino komanso akuziwa kale kuti on that day network izakhala ikuvuta believe me komanso guys ndege ija idagudwa ku Germany komweko apapa pilibe chiyembekezo chabwino
@user-wq9ex2sf3b5 күн бұрын
Azafufuza bwanji black box munalibe afiti imwe
@user-ow3tp3vu3c17 күн бұрын
Mmm 6 july mpaka kulepheleka???😮😮😮😮 Hahahaha koma boma iliri mmmm zovutatu
@JamesIngeni-ku3qj18 күн бұрын
Let's just pray kut kafukufuku kanyende mwachilungamo
@DoYouKnow383818 күн бұрын
Kafukufuku sangayende mwachilungamo chifukwa akupangidwa influence ndi andale.
@MarthaJonathan-ci8mh13 күн бұрын
Bola osapachitikeso ngozi ya ndege
@user-qz5gj3tf2t16 күн бұрын
Oziwa za ndale za ziii palibe chiziwa iwo amenewo
@FionaKhoma17 күн бұрын
Ofufuzawo akanabwera kudzera kwaamabungwe boran km ngt akubwera chifukwa chot aitanidwa ndiaboma atiyakha bodza chifukwa achunudwa kare auzen abwerere
@hopembendela17 күн бұрын
Fuso ndiloti akaswili amenewo amene wawaitana ndi ndani ngati ndi lili boma amalawi musayembekeze chilungamo chilichose apa
Aaa akadaulo ake at?mesa osewa ndi akongeresi muti ndife Ana?
@pempheroraynnoxmpesi871315 күн бұрын
Kaliati judged it
@mussakapalamula199018 күн бұрын
Pachoka nzako Pali Malo. Koma Manganya usamale.
@user-jk8sh7fh2d18 күн бұрын
Koma kaliati ndi mamuna ndi nkazi? Ai munthu uyu amaopsya kumfikila ngati si nkazi ubwino wake amauona ndi kwawo komweko ati amathandiza koma iiiii ai mai owoopsya kwambili
@LeendaDeborah200518 күн бұрын
Chakupangitsani ndi chani kunena choncho??
@InnocentEdasi18 күн бұрын
U t m yathah basi..., Manganya ndiwa M C P
@user-wq9ex2sf3b5 күн бұрын
Miko usi ndi imozi wa fiti zinapha chilima agalu 🐕a MCP
@ebenezerkamanga601618 күн бұрын
Iweyo ku nkuyu panyo pamako
@awezafalesi387314 күн бұрын
Abale chonde musathe za mkamwa kodi si Chilima yomweyo aika amalawi pa moto amati tizidya katatu zinthu zitsika mtengo lero mmmmmmm inde za imfa sitikusangalala ndi mmene afela