Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥
@FRAVIOKUNSANJA22 күн бұрын
Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse
@GanizaniKamvazaana22 күн бұрын
Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
@INNOCENTMOFOLO-io8tg22 күн бұрын
😂😂😂😂😂 DC ndiyakatundu zoona
@LysonMtalika-tb6fk22 күн бұрын
Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
@user-hk3hg1to4e22 күн бұрын
Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢
@StevieChikaonda21 күн бұрын
Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪
@EllenPhiri-xt8pt22 күн бұрын
God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever
@GoodsonDiwadiwa22 күн бұрын
The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi
@FisherAction22 күн бұрын
Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp
@GospelSoldiers-sr7np22 күн бұрын
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
@RashidSaid-lk6bb22 күн бұрын
MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa
@raytavares225622 күн бұрын
Mr president the DC we love you and greetings from North London UK
@GRACIOUSKENAN22 күн бұрын
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉 ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
@EmmanuelMpalagule22 күн бұрын
Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,
@chimwemwemasamba288022 күн бұрын
Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤
@GamaGama-z8p22 күн бұрын
Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side
@user-or7ng3fj8f22 күн бұрын
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
@OwamiSimeon22 күн бұрын
Born kalindo more 🔥
@DalitsoMatope22 күн бұрын
Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you
@InnocentEdasi22 күн бұрын
The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _
@RidwanAdam-nq6lz22 күн бұрын
Booooon kalindooooo 🔥🔥
@PempheroKasimongwa22 күн бұрын
Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤
@limbanimtitima917022 күн бұрын
Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂
@ChimwemweBottomani-hc5ju22 күн бұрын
Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC
@pacharokoloviko169418 күн бұрын
😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC
@MartinsKhumalo22 күн бұрын
❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏
@JabesAlfaiate-t4v22 күн бұрын
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
@gwatandingo950222 күн бұрын
Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂
@texonkautera22 күн бұрын
Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula
@RafickRaj22 күн бұрын
Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino
Iyayi na ya mchenga yokhayo boma likunena zoona chifukwa mchenga is in the group of minerals and any mineral is a government property which is minored through the government permission. Everywhere in the world illegal mining is prohibited citizens are allowed to collect sand ndi wilibala basi not with a thipa truck then you have to go face the law which is in the constitution every country.
@KnowledgecGodwin-xo4pw22 күн бұрын
Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.
Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo
@KunyengaMoyo22 күн бұрын
Ng'alula DC
@ChimwemweKondowe-nj4lx22 күн бұрын
Malawi belongs to Malawians and not Chakwera with his incapacitated cabinet
@EsnartGirivin22 күн бұрын
Osakhala presdent bwanji abon kalindo Tayambitsani chipani cha amphawi
@user-do2cs8nf4b22 күн бұрын
Koma ndikale lonse sindinambve zimenezi koma zikuchitikaz zabwino bwino? Yohhhh Ambuye Mulungu kumwambako tsikani ndithu anthu tikubvutika eishhhhhh zochititsa manyazi tu mpaka mchenga
@ChimwemweBottomani-hc5ju22 күн бұрын
Sikusinja ndi Gwenembe😅😅😅😅😅😅😅 Nyengo yokhadxula kukhazula
@annamazingashaibuh627622 күн бұрын
Kkkkk koma ndipo akavoteraa nda amawooo hiyaa mau Mr Bon
@JamesKambale-s2c22 күн бұрын
Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu
@happychimwemwe-180522 күн бұрын
Umakwana booooon kalindo
@samuelgambatula241522 күн бұрын
Tiyambe mademo.... Ulemu wathapo apa
@stanfordnsona21 күн бұрын
Kalindo umatitsekula maso
@jameskamanga62820 күн бұрын
Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk
@BeatriceRobert-jq6ci22 күн бұрын
Koma chakwera pathako pako komatu chaka chamawa sitikulora zoputsa iweyo or utani u kuchoka basi
@ClementbWatches22 күн бұрын
Mmmmm koma Boma ili nde eeee mpaka chenga azikhoma sokho iiiii zachilendo mu dziko la malawi. Koma chakwela wapengad et. Ndikumat ndizawinaso 2025 pasanapako bas
@user-qc7qg4cy6k22 күн бұрын
Totally agree the dc
@Vascomw22 күн бұрын
Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza
@ZainuluNsalule21 күн бұрын
Good
@SamuelChiwere22 күн бұрын
😂😂😂😂 apa ndiye Government yawonetsaso kubwabwana mchenga akufuna atanthauze chiyani kuti zimveke ndiye timvaso kuti mpale ndi chimanga tisamakagawitse kuchigayo
@KnowledgecGodwin-xo4pw22 күн бұрын
Mumatimilira mr president
@christophermukaka740322 күн бұрын
Kalindo ndisaname mukuwatsegula anthu koma bvuto opposition ili weak