BON KALINDO 11 JULY 2024 KUNG’ALURA PA THURSDAY

  Рет қаралды 28,707

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

24 күн бұрын

Пікірлер: 223
@VungaQueen
@VungaQueen 22 күн бұрын
Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥
@FRAVIOKUNSANJA
@FRAVIOKUNSANJA 22 күн бұрын
Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana 22 күн бұрын
Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 22 күн бұрын
😂😂😂😂😂 DC ndiyakatundu zoona
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 22 күн бұрын
Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
@user-hk3hg1to4e
@user-hk3hg1to4e 22 күн бұрын
Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢
@StevieChikaonda
@StevieChikaonda 21 күн бұрын
Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 22 күн бұрын
God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever
@GoodsonDiwadiwa
@GoodsonDiwadiwa 22 күн бұрын
The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi
@FisherAction
@FisherAction 22 күн бұрын
Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 22 күн бұрын
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
@RashidSaid-lk6bb
@RashidSaid-lk6bb 22 күн бұрын
MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa
@raytavares2256
@raytavares2256 22 күн бұрын
Mr president the DC we love you and greetings from North London UK
@GRACIOUSKENAN
@GRACIOUSKENAN 22 күн бұрын
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉 ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
@EmmanuelMpalagule
@EmmanuelMpalagule 22 күн бұрын
Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,
@chimwemwemasamba2880
@chimwemwemasamba2880 22 күн бұрын
Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 22 күн бұрын
Koma Mulungu ngati kunali kufuna kwanu kuti munthu uyu awulawe u president ayi pafikapa ife anthu anu timveni kulira kwathu 😢, Ife anthu akumuzi kuti tigule sopo timadalira kuvuwula mchenga omwewo kuti tichape, onani pomwe zinthu zafikapa Yehova, ingobwerani muzaweruzepo dziko lanuli Ambuye
@vitumbikokamanga5869
@vitumbikokamanga5869 22 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤
@GamaGama-z8p
@GamaGama-z8p 22 күн бұрын
Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side
@user-or7ng3fj8f
@user-or7ng3fj8f 22 күн бұрын
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
@OwamiSimeon
@OwamiSimeon 22 күн бұрын
Born kalindo more 🔥
@DalitsoMatope
@DalitsoMatope 22 күн бұрын
Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 22 күн бұрын
The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _
@RidwanAdam-nq6lz
@RidwanAdam-nq6lz 22 күн бұрын
Booooon kalindooooo 🔥🔥
@PempheroKasimongwa
@PempheroKasimongwa 22 күн бұрын
Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤
@limbanimtitima9170
@limbanimtitima9170 22 күн бұрын
Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 22 күн бұрын
Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC
@pacharokoloviko1694
@pacharokoloviko1694 18 күн бұрын
😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC
@MartinsKhumalo
@MartinsKhumalo 22 күн бұрын
❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏
@JabesAlfaiate-t4v
@JabesAlfaiate-t4v 22 күн бұрын
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
@gwatandingo9502
@gwatandingo9502 22 күн бұрын
Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂
@texonkautera
@texonkautera 22 күн бұрын
Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula
@RafickRaj
@RafickRaj 22 күн бұрын
Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino
@user-lp8wj3vq4x
@user-lp8wj3vq4x 22 күн бұрын
Ife dzuro timadikira mademo, agalu amenewa atitopesa
@kelvinmphande3754
@kelvinmphande3754 22 күн бұрын
It's the sikusinja Gwenembe song for me
@JaxyKumwenda
@JaxyKumwenda 22 күн бұрын
Tikufuna mademo bwana osamunyengerera Chakwera
@MosesKalenge
@MosesKalenge 22 күн бұрын
ULEMU WANU MR, THE DC..... BON KALINDO 💪✊✊✊📡🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@user-wu4tl2yn9e
@user-wu4tl2yn9e 22 күн бұрын
Khaaaaaa wafika the DC
@LovelyJapaneseMaples-xc2bc
@LovelyJapaneseMaples-xc2bc 22 күн бұрын
Kuswakuswa big osaopa😊
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w 22 күн бұрын
Our president more fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌
@mbewemisoyaanenenji1908
@mbewemisoyaanenenji1908 22 күн бұрын
Boooon Kalindo , Pangolin mwana womvuta kwambiri
@RashidSaid-lk6bb
@RashidSaid-lk6bb 22 күн бұрын
Uchitsilu ndiye umeneo Sizidachitikepo
@OsmanBakali-s5x
@OsmanBakali-s5x 22 күн бұрын
Where are we going to make our hustle now😭😭😭 mpakana nchenga omweu tkatenge chilolezo? 🔥🔥🔥🔥🔥
@HannockMesiwni
@HannockMesiwni 22 күн бұрын
Njira ya ld pokavota sitikavota nkhondo ichitike ichitike
@OmegaNjati
@OmegaNjati 21 күн бұрын
Ambuye nditengeni
@AudettaYohanie-fl3oc
@AudettaYohanie-fl3oc 22 күн бұрын
Aaaah koma izizi ndiye chakwera wationjedza zedi ,koma chifukwa chani kweni kweni?
@IvieMwabile
@IvieMwabile 22 күн бұрын
Akufuna kutimpha agalu amenewa.go deeper
@JohnAsendi
@JohnAsendi 22 күн бұрын
Kkkk Boma amalawi kutifinya tiwona zinthu shop chaine chasala ndi maepute katoni okhaokha ndatawira kunnjenga ndiyemukulesa mukufuna kundipha chani mukandiphera kuzenje komweko 😮😮😮😮
@babranzima8120
@babranzima8120 22 күн бұрын
Ndizisilu zaathu zathu ananyerapo chenga iyewo chakwera
@BatsonKadzuwa-tl3rp
@BatsonKadzuwa-tl3rp 22 күн бұрын
Zoonadi mboni ndineyo nditachita ngoz ku Queens ndinalipira kut andithandize
@loycemmadi9303
@loycemmadi9303 22 күн бұрын
And it's the song for me😂😂😂😂Winiko Ayi ndithu
@duncainjimmy
@duncainjimmy 22 күн бұрын
Mulungu adalenda dothi osati Chakwera ai
@user-ko1lk3br4r
@user-ko1lk3br4r 22 күн бұрын
Mafuta ayamba kuchoka ku Mozambique kukafika ku area 50 ku Lilongwe kudzela pa njanje ai zikomo
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 22 күн бұрын
Mafumu aku ntcheu mtima wawo ukuwawa alibe dyera ndi mafumu odziwa kulira moyo wa munthu sizocheza
@gwatandingo9502
@gwatandingo9502 22 күн бұрын
Koma mpaka chenga mmmm mawonjeza
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f 21 күн бұрын
Koma funso nkumati kuti, Kodi Chakwela ndi Zikhale wacheyo, samachita manyazi konse akamamva izi? kapena umunthu wanu unatha?? The DC tell them shit
@annamazingashaibuh6276
@annamazingashaibuh6276 22 күн бұрын
Uyu ndi nyoooo kwa nyooo ulemu wanu aaaa mchenga athu anayambira kale za mchenga athu amadyera momo abale eishh sambi
@user-kw7wr4kq9w
@user-kw7wr4kq9w 22 күн бұрын
We only need solutions not only kulalika
@dinahmunthali5324
@dinahmunthali5324 22 күн бұрын
Ine nyimbo ndi zomwe zimandi waza koophya ati Sikusinja ndi Gwenembe amkaimba agogo awake DC popita ku Mzuzu akudutsa mu chikangawa 😂😂😂😂😂 DC makina 😂😂
@BillyMhone-jp3kn
@BillyMhone-jp3kn 22 күн бұрын
We are in a Failed State and Chakwera uyuu achoke
@JonathanChimwaza
@JonathanChimwaza 22 күн бұрын
Chakwera ndi president olephera ananena kale atupele kuti chakwera sanakhalepo nduna relo sizi
@HawardStainly
@HawardStainly 22 күн бұрын
Akubwila fodya wamagogo wakuzino uja,(maganga).
@user-xd1cm7tm7t
@user-xd1cm7tm7t 22 күн бұрын
The dc our poor president in Malawi
@IsraelMtawali
@IsraelMtawali 22 күн бұрын
Chakwera is apus must go
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage 22 күн бұрын
😅😂ayi ziliko mpaka boma kugulitsa ntchenga😂😂😂😂
@loycemmadi9303
@loycemmadi9303 22 күн бұрын
Mr kalindo munafika aaaah kukanapezeka ambiri ngati inu bwezi dzikoli titaona zina aaaah
@densonchiwaya8439
@densonchiwaya8439 22 күн бұрын
Mau awaa sikalindoo
@LinoMatchado
@LinoMatchado 22 күн бұрын
Iyayi na ya mchenga yokhayo boma likunena zoona chifukwa mchenga is in the group of minerals and any mineral is a government property which is minored through the government permission. Everywhere in the world illegal mining is prohibited citizens are allowed to collect sand ndi wilibala basi not with a thipa truck then you have to go face the law which is in the constitution every country.
@KnowledgecGodwin-xo4pw
@KnowledgecGodwin-xo4pw 22 күн бұрын
Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.
@MouriceChimkondo
@MouriceChimkondo 21 күн бұрын
Kkkkkk
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 22 күн бұрын
Ndipo zoonadi chonsecho sanapangile anthuwo chochita
@TutuAlfred-y2l
@TutuAlfred-y2l 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂. Zosatheka sizidzatheka nanga chenga ndichani uyo wasala pang'no kt amfe ameneyo chisilu chamunthuyo muuze ambere Ku muloza border kuno aone kt angatile ife kuvuula chenga.
@LoveBanda-sw1nu
@LoveBanda-sw1nu 22 күн бұрын
😅😅😅😅kumalawi mkokoma ndithu bwanawa akutiposa zochita
@MouriceChimkondo
@MouriceChimkondo 21 күн бұрын
Following boss
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 22 күн бұрын
The Dc bon kalindo good Messnge
@user-nn4bf1kw9h
@user-nn4bf1kw9h 22 күн бұрын
Ing'alureni 🔥🔥
@user-hb1ll8lj3v
@user-hb1ll8lj3v 22 күн бұрын
Gwenembe ND sikisinje yemweyo 😂😂😂😂
@ChondezVick
@ChondezVick 22 күн бұрын
The DC himself 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 22 күн бұрын
Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo 22 күн бұрын
Ng'alula DC
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx 22 күн бұрын
Malawi belongs to Malawians and not Chakwera with his incapacitated cabinet
@EsnartGirivin
@EsnartGirivin 22 күн бұрын
Osakhala presdent bwanji abon kalindo Tayambitsani chipani cha amphawi
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 22 күн бұрын
Koma ndikale lonse sindinambve zimenezi koma zikuchitikaz zabwino bwino? Yohhhh Ambuye Mulungu kumwambako tsikani ndithu anthu tikubvutika eishhhhhh zochititsa manyazi tu mpaka mchenga
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 22 күн бұрын
Sikusinja ndi Gwenembe😅😅😅😅😅😅😅 Nyengo yokhadxula kukhazula
@annamazingashaibuh6276
@annamazingashaibuh6276 22 күн бұрын
Kkkkk koma ndipo akavoteraa nda amawooo hiyaa mau Mr Bon
@JamesKambale-s2c
@JamesKambale-s2c 22 күн бұрын
Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu
@happychimwemwe-1805
@happychimwemwe-1805 22 күн бұрын
Umakwana booooon kalindo
@samuelgambatula2415
@samuelgambatula2415 22 күн бұрын
Tiyambe mademo.... Ulemu wathapo apa
@stanfordnsona
@stanfordnsona 21 күн бұрын
Kalindo umatitsekula maso
@jameskamanga628
@jameskamanga628 20 күн бұрын
Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk
@BeatriceRobert-jq6ci
@BeatriceRobert-jq6ci 22 күн бұрын
Koma chakwera pathako pako komatu chaka chamawa sitikulora zoputsa iweyo or utani u kuchoka basi
@ClementbWatches
@ClementbWatches 22 күн бұрын
Mmmmm koma Boma ili nde eeee mpaka chenga azikhoma sokho iiiii zachilendo mu dziko la malawi. Koma chakwela wapengad et. Ndikumat ndizawinaso 2025 pasanapako bas
@user-qc7qg4cy6k
@user-qc7qg4cy6k 22 күн бұрын
Totally agree the dc
@Vascomw
@Vascomw 22 күн бұрын
Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza
@ZainuluNsalule
@ZainuluNsalule 21 күн бұрын
Good
@SamuelChiwere
@SamuelChiwere 22 күн бұрын
😂😂😂😂 apa ndiye Government yawonetsaso kubwabwana mchenga akufuna atanthauze chiyani kuti zimveke ndiye timvaso kuti mpale ndi chimanga tisamakagawitse kuchigayo
@KnowledgecGodwin-xo4pw
@KnowledgecGodwin-xo4pw 22 күн бұрын
Mumatimilira mr president
@christophermukaka7403
@christophermukaka7403 22 күн бұрын
Kalindo ndisaname mukuwatsegula anthu koma bvuto opposition ili weak
@MariamJaffali
@MariamJaffali 22 күн бұрын
The DC boooooon kalindoooooooo
@Sugerman-tw4do
@Sugerman-tw4do 20 күн бұрын
Big Bos DC mumakwa
@LamseyChimah
@LamseyChimah 22 күн бұрын
@user-no2mx4go8p
@user-no2mx4go8p 22 күн бұрын
Mpakana licence 😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌 zili kumalawi nzatose akatenge licence ndi driver 😂😂😂😂
@InnocentBanda-g6i
@InnocentBanda-g6i 22 күн бұрын
❤❤
Spot The Fake Animal For $10,000
00:40
MrBeast
Рет қаралды 185 МЛН
A teacher captured the cutest moment at the nursery #shorts
00:33
Fabiosa Stories
Рет қаралды 51 МЛН
Electoral Chamber of the TSJ began hearing process
38:04
TeleSUR English
Рет қаралды 2 М.
Bon Kalindo Response To H E Chakwera's SONA.
15:53
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 38 М.
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 23 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 55 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 242 М.
BON KALINDO 2 AUGUST 2024 KUKHADZULA KWA PA FRIDAY
15:27
Malawi Trends TV
Рет қаралды 3,8 М.
Spot The Fake Animal For $10,000
00:40
MrBeast
Рет қаралды 185 МЛН