Chilima Simtsogoleri Wabwino - Bon Kalindo

  Рет қаралды 28,718

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

Ай бұрын

On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo says, Vice President Saulos Chilima is not presidential Material. If he was he would have show solidarity with the poor Malawians who are suffering under Tonse Alliance.
Ku Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo akuti, Vice President Saulos Chilima is not Presidential Material. Akadakhala akadawonetsa mgwirizano ndi Amalawi osauka omwe akuvutika pansi pa Tonse Alliance.

Пікірлер: 82
@Luxemaven8686
@Luxemaven8686 25 күн бұрын
Bon Kalindo you have gained a supporter!!!!
@user-qq1uj7ct6n
@user-qq1uj7ct6n Ай бұрын
booooon kalindo Mo fayaa. keep on to give us truly updates. inu mumalankhula chilungamo chokha chokha
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o Ай бұрын
Honest speaking Mr DC Big up
@LoyidKarebe
@LoyidKarebe Ай бұрын
Go ahead Mr kalindo we are following you
@user-iq5xk6ju7y
@user-iq5xk6ju7y Ай бұрын
Komatu a Kalindo munthu osamuipitsa choncho. Inu musamunene Chilima kuti oipa lero. Mwagwira naye ntchito limodzi. Kuipa kwa munthu amadziwa ndi Chauta basi. Inunso muli ndi zonyansa zanu.
@VincentNgabuhvincent
@VincentNgabuhvincent Ай бұрын
khala chete iwe
@HakeemJossam
@HakeemJossam Ай бұрын
aaaaah kuipa kwa munthu amakuziwa ndan? mxiew
@ellahmwams831
@ellahmwams831 Ай бұрын
Mr kalindo moto 🔥 🔥🔥
@AlastairGutt
@AlastairGutt Ай бұрын
Kalindo is matured now
@ishmaeldama8906
@ishmaeldama8906 Ай бұрын
Bon he is talking the truth, but u can see other people they talking sheet, be very careful my fellow Malawian, we must wake up guys, zinazi sizotengela kupita ku school, khalani pansi moganiza bwino, malangizo awuleletu awa,all the way from johannesburg
@Littlefair7
@Littlefair7 Ай бұрын
Who spoke that spoke?
@homeremedys3748
@homeremedys3748 Ай бұрын
Mukunena zoona big, koma mmalawi opusa akuona ngati chilima ndiwabwino
@devimatope9980
@devimatope9980 Ай бұрын
man of integrate😂😂😂 Bonnnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri from Njeza village ..T/A mabuka, mulanje😊😊😊😊😊
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Ай бұрын
Chakwera ndi Chilima wooooyeeee,muwaphe A Malawi onse mukatha mutenge mitemboyo muitafune Mukhute,popeza ndalama mwawa bera Kale,koma muziwe masiku amatha ndikugona adaku voterani wokha samaziwa zoti Chibwenzi chankhwangwa chokoma pokwera, Amalawi mukaza voteranso awa izo ndi zanu wanthuwa ndi aka Nyimbi Anunkhisa Malawi.
@beakab2378
@beakab2378 Ай бұрын
Zooona zokhazokha, Chilima wakhala duuuuu a Malawi tikulira, olo one day osalankhulapoyi mmene m"boma mukubedwera ndalamamu, nde atifune pano? Ine ndamitsikatu, he won't get my vote
@EagerChicken-qj6xu
@EagerChicken-qj6xu Ай бұрын
Kodi inu mumkamuuza chilima ngati ndani? Osachita naye msanje. Pangani zanu akulu
@user-zm9sf2mj7u
@user-zm9sf2mj7u Ай бұрын
Mbambande mr presdent bon kalindo kwathu kwa chulu zinthu sizilibwino tikukhalangati tili mkamwa mwa mikango
@RodwellLupiya
@RodwellLupiya Ай бұрын
Bwana Born Kalindo pqjatu ndinu amene munamukakamiza Chilima kuti avomere kukhala vice president lero mukumunyozaso . Komaso inuyo mumatiuza kuti sindinu wandale koma chosecho mukuwauzaso anthu kuti akqvotere aford , udf kqpenda dpp.
@user-yh3ys3qn6p
@user-yh3ys3qn6p 24 күн бұрын
Chisilu mbuzi 😢😢😢
@macksonkalasa9668
@macksonkalasa9668 Ай бұрын
Koma kumanidwa udindo kulira mpakana 4 years
@EagerChicken-qj6xu
@EagerChicken-qj6xu Ай бұрын
Musamuipitsile mbiri a chilima inunso simulibwino.
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Ай бұрын
Yes you are really talking
@BrightKuyaka
@BrightKuyaka Ай бұрын
Zoyankhula za bon kalindo zatitopetsa tsopano, katakwe ndi bakili muluzi tv
@frankiechasokoneza5802
@frankiechasokoneza5802 Ай бұрын
Zakutopetsa not zatitopetsa bwana
@SamuelChauluka
@SamuelChauluka Ай бұрын
Ingosiyani osamamvela bas,,,,, za ziiii
@user-ep7cg9bb4m
@user-ep7cg9bb4m Ай бұрын
Nkhanira yakwachulu yokha mwapala. Miyambe mwazimvetsa zinthu mmene zikuchitikora. Bwerani ndi ma demo anuwo tione ngati simuyaluka
@KondwaniMunthali-lx5jc
@KondwaniMunthali-lx5jc Ай бұрын
Ndiye tivotele ndani utiuze kalindo manyi ako
@esternguluwe
@esternguluwe Ай бұрын
Bwanji adzangotiimra bon kalindo yomweyo pa u president,akuoneka ali ndi nzeru kwabasi
@user-ic7fq5yn6r
@user-ic7fq5yn6r Ай бұрын
Yes DC akunena zovona
@georgebalala3048
@georgebalala3048 27 күн бұрын
Shaaaa this was days ago
@SibwenzaLevisoni-gm6rv
@SibwenzaLevisoni-gm6rv Ай бұрын
Ndipo nkhaniyi ndioona big up DC
@PeterkinsJanuary-fv9wd
@PeterkinsJanuary-fv9wd Ай бұрын
Bon kalindo ulemu wanu
@JonathanKamwetsa
@JonathanKamwetsa Ай бұрын
Ipondeni Fadala........ You're a real son of Malawi........
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q Ай бұрын
Apadi akunena zoona zaka zonse takhalayi chilima ali.duuuh nde angabwele kwa ife kutiwuza chani ??
@WilliamBanda-un5eg
@WilliamBanda-un5eg Ай бұрын
Dzapangeni nawo compete bwanji because it seems mukudziwa zambiritu
@MercyPhiri-nh9jy
@MercyPhiri-nh9jy Ай бұрын
Zoona amasankha tsogoleri ndi mulungu. Inu musaweluze
@DesmondKanguwe
@DesmondKanguwe Ай бұрын
Kalindo ndiwamisala uyu
@SanudiJaymofred
@SanudiJaymofred Ай бұрын
Kalindo to the people
@Nomsa77
@Nomsa77 28 күн бұрын
Vchifukwa choti azakhala pa u president ndichifukwa achakwera amuphera..... Chifukwa chani mdziko mumalowa anthu osaziwika bwino
@GiftAsirKhwanya-ok2gu
@GiftAsirKhwanya-ok2gu Ай бұрын
Akunena zoona kalindo
@ShukuSh-vi1hk
@ShukuSh-vi1hk Ай бұрын
Ndizoona zimene akuankhula karindo chifukwa nthawi yakampeni ndiiyeyo amene amanyamula thumba la 50 kg sichakwera iyayi
@CheloyaaChikwatuu-ob2mt
@CheloyaaChikwatuu-ob2mt Ай бұрын
DC ❤❤❤
@PeterPadambo-kk5oh
@PeterPadambo-kk5oh Ай бұрын
Chilima sanalakwise kanthu, cholinga akawukira muzimunena kuti amangowukira kulikonse? Apa pokha nde ayi, boma ili tinalivotera chifukwa cha Chilima, nde atulukeko chifukwa? Mesa kuli mavoti ake, musiyeni Chilima akhale, nthawi ikakwana ayankhula
@grandwellkatumbi4763
@grandwellkatumbi4763 Ай бұрын
Aziyankhula zichani Nanu Inu chilima wanuyo
@daveskachiphaphi
@daveskachiphaphi Ай бұрын
Tabalirankon aku mwera usabwere ndi mademo Ako pano pakati chita kwanuko
@user-zs9hn3kv3e
@user-zs9hn3kv3e Ай бұрын
Impossible ngati munthu akugwira ntchito mmboma sangayankhulepo zotsutsa boma man limenelo nde bodxa
@user-ty1vq9lq6w
@user-ty1vq9lq6w Ай бұрын
Zitsiru ndizomwe zingakhulupilire chilima opusa omwewa ndizomwe zikunamizika chilima zaupresdent alibe nazo ntchito koma iye azingodyelera mimba yakeyo
@josephchika173
@josephchika173 17 күн бұрын
Amakomadi akamwalira munthu sure
@NtabaKali
@NtabaKali Ай бұрын
Yaaa
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx Ай бұрын
Chilima waonetsa kudekha ndipo sadaukire koma kalindo ndale zidakulani
@grandwellkatumbi4763
@grandwellkatumbi4763 Ай бұрын
Dziko likamaonongeka mtsogoleri wabwino sadekha ....chilima akudekha zichani pamene zinthu zikufoila mdziko muno
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Ай бұрын
Akutitenga ife uchitsilu pomwe achitsilu ndiyiwowo amalawi asukutsula ngati tinachotsa mbuyawo kamudzi chifukwa chankhadza chakwela nde ndanitso galu kwabasi
@HakeemJossam
@HakeemJossam Ай бұрын
anatipwetekesa asabweleso
@vitumbikokamanga5869
@vitumbikokamanga5869 Ай бұрын
Chilima usogoleli mlibe ose ndi adyera same like chakwera 😅
@BrianBanda-nn1gt
@BrianBanda-nn1gt Ай бұрын
Ndizoona ndikugwilizana nazo
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Ай бұрын
Aaaa chilima angoputsisa MCP tsingapase utsogole chifukwa chakwela akumva kukoma ndibanja lawo lotse nso dzoti chilima akudziwa chilungamo koma manyadzi uchitsilu mutayeni tiwone 2025 dzizatha bwa
@homeremedys3748
@homeremedys3748 17 күн бұрын
Munthu amakondedwa anamwalira Pamalawi
@ShabanMajor
@ShabanMajor Ай бұрын
iwe ndikumenya bwanji mulimbana ndi DC wanga
@YohaneFoster-vq7wp
@YohaneFoster-vq7wp Ай бұрын
Kalindo akufuna atibalalise Ali ndi reason behind
@SangwaniNkosi
@SangwaniNkosi Ай бұрын
Chilungamo chimawawa,Koma DPP ayi ziko linaliko bwino mnthawi yimeneyo
@francischikaya3146
@francischikaya3146 Ай бұрын
Iwe sukuimirira a Malawi koma chipani china chomwe aliyense akuchidziwa. Ukulimbana ndi Chilima nthawi zonse bwanji? Kodi kwinako kulibe zofooka zawo. Usawaike a DPP ngati ndi Angelo lero. Sitinaiwale zomwe amachita padzana paja. Tikudziwa kuti mtunda wa kwanu ndi omweo. Usatinamize ife takana.
@giftmingo9293
@giftmingo9293 Ай бұрын
Boma la Chakwera silizakhala labwino kwaiwe only if utakhala Minister. Unduna sapatsa zitsiru ngati iwe. Anthu a kwa Chulu akakuthibula bwera uzazione. Kulira 4 years kufuna udindo kkk😂😂😂😂
@henrykapinga1433
@henrykapinga1433 Ай бұрын
Kkkkkk
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx Ай бұрын
Uyu ndi wamisala chilima ndi otumidwa so sakadaima mkuyankhula mudakati ndi oukira
@giftmingo9293
@giftmingo9293 Ай бұрын
Uzitiuzanso za DPP ifeyo lero? Moti ukakhala umati aMalawi angamvere ndithu iweyo kkkk
@SAIKINGFRIDAY
@SAIKINGFRIDAY Ай бұрын
Eh komatu akulu awa chilima anakulakwilani chani muja munayambila kumunenamuja mpakapano or kukuyankhani osangomusiya bwanji ndiwankulutu ameneuja amadziwa chimene akupanga nde zinazi ife mumatinyasanazo zomalimbana ndimunthu oti samakuyankhani
@user-dy4gc2hr5e
@user-dy4gc2hr5e 27 күн бұрын
Zoonadi zianthu zoipa kwambiri 😂😂😂😂😂😂😂
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Ай бұрын
Kalindo ngati ndi chamba uzavula galu iwe ukukhale wachilungamo ndiwe mulungu?? Ndiwe galu kwambiri usatibowe uziyankhulira amako ndi anthu akwanuko
@SamuelChauluka
@SamuelChauluka Ай бұрын
u a big fool
@MalakamMillie
@MalakamMillie Ай бұрын
Chilima ndi witch craft mbuzi mwana wajoka amati tizidya katatu madzi awulere magetsi awulere fetelizer wochipa. chilima ndifiti kwambili
@BazaarShaibu
@BazaarShaibu Ай бұрын
Aka ndi kachilungamo
@LovelyGalaxy-rb7yl
@LovelyGalaxy-rb7yl Ай бұрын
Zinthu zake
@user-lr2wx5xd9d
@user-lr2wx5xd9d Ай бұрын
The DDCccccccccccc
@AnnoyedFallingLeaves-zp8dy
@AnnoyedFallingLeaves-zp8dy Ай бұрын
The problem with Kalindo is that he wants to be the master minder of Chilima. But he has to understand that Chilima has brains. My instincts also tells me that he is indirectly campaigning for DPP.
@user-se4cf9qp8b
@user-se4cf9qp8b Ай бұрын
This is true. Kalindo is 4 dpp
@EvanceSungani-cv9jk
@EvanceSungani-cv9jk Ай бұрын
In your minds but he talks vry true posatengera za ndale,,,,,and all of this akuya khula ndizoona,,,, nokha mukuziwa mene adalankhulila chilima mu campaign ya 2019 analankhula zambili mbili zokomera Ife achinyamata koma ndzt wakwanilitsapo,,,,,inuso musamangosutsa zilizonse you supposed to see the true
@Littlefair7
@Littlefair7 Ай бұрын
I fully agree with you, Kalindo is taking advantage of illiterate masses.
@GRACIOUSKENAN
@GRACIOUSKENAN Ай бұрын
Which brains dear, you talking about??? No he is bad man also,can he preform good speak today how??
@EmilyBakali
@EmilyBakali Ай бұрын
Kkkkkkkkk
@paulbanda9638
@paulbanda9638 Ай бұрын
Izi ndi nkhani za amalawi ngakhale a president anayankha nkhani ya America mu chichewa, translate in English nonsense
@angelj3771
@angelj3771 27 күн бұрын
It a better to dellete this video. You have cursed him
@josephchika173
@josephchika173 17 күн бұрын
Lero akuti anali tsogoleri wabwino tooo bad
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 18 М.
Zifukwa Zomwe Zingapangitse MCP Kuchoka M'Boma - Concerned Citizen
11:18
Мы никогда не были так напуганы!
00:15
Аришнев
Рет қаралды 6 МЛН
Самое Романтичное Видео ❤️
00:16
Глеб Рандалайнен
Рет қаралды 4,6 МЛН
NERF WAR HEAVY: Drone Battle!
00:30
MacDannyGun
Рет қаралды 51 МЛН
Получилось у Вики?😂 #хабибка
00:14
ХАБИБ
Рет қаралды 7 МЛН
Raila, Kalonzo present as President Ruto signs IEBC Bill into law
40:07
Citizen TV Kenya
Рет қаралды 139 М.
Bon Kalindo Response To H E Chakwera's SONA.
15:53
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 37 М.
BOMBA! ROQUE SILVA DEIXA MOÇAMBIQUE, E DECIDE VIVER FORA!!😱
19:20
Moz na diáspora
Рет қаралды 86 М.
Raila: Be aware of the WRATH of history
23:42
Herman Manyora
Рет қаралды 30 М.
Elizabeth Mkandawire Saolos Chilima sister (speech)
4:20
Media Quake
Рет қаралды 27 М.
Jomo wamukana Bon Kalindo
4:20
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 57 М.
Ekedi na Sekuru Kanengo padare kuchiweche akafira pasowe cheshomba part 7
1:26:08
Мы никогда не были так напуганы!
00:15
Аришнев
Рет қаралды 6 МЛН