Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa

  Рет қаралды 23,403

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

15 күн бұрын

Comrade Ntanyiwa, speaking on Nyasa VoiceBox, suggests that the MCP is becoming so unpopular that even his kinsmen in Kasiya, Lilongwe, are prepared to vote him out.
Comrade Ntanyiwa polankhula pa Nyasa VoiceBox akusonyeza kuti chipani cha MCP chayamba kusatchuka moti ngakhale abale ake aku Kasiya mu mzinda wa Lilongwe ali okonzeka kumuvotera.

Пікірлер: 71
@NizigiyimanaChantal-c2p
@NizigiyimanaChantal-c2p 12 күн бұрын
God is able Mr comred❤ 🔥 we are the winers
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 13 күн бұрын
Bakili Muluzi amayenda yekha wopanda Asirikari nkuma wumba zidina, uyu chakwera m'busa wonyenga wakupha anzake ayende yekha tiwone Kodi kampeni akachitira Kuti?
@wilsonali7890
@wilsonali7890 13 күн бұрын
May Allah guide and protect all the real freedom fighters from evil people
@Amgwagwa
@Amgwagwa 13 күн бұрын
Ruto and chakwera mulibwanji
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 13 күн бұрын
Tadzuka bwino ka inu comrade ntanyiwa, mdzenjemo agweramodi okha, adzimangiliranso ngt yudas chifukwa mizimu ya anthu omwe anawapha aja idakayendabe pa dziko pano may the almighty God continue to protect comred you wherever you will go❤
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 13 күн бұрын
God bless you 🙏🙏🙏🙏🙏
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 13 күн бұрын
May God keep you safe comrade no weapon formed against you shall prosper
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 13 күн бұрын
Good Messnge Chakwela you mast go
@marryphili5419
@marryphili5419 13 күн бұрын
Amen Mr my god protect you
@wilsonali7890
@wilsonali7890 13 күн бұрын
That's the great Original Mntanyiwa ❤🎉
@REXCHARLESKAJAWO
@REXCHARLESKAJAWO 11 күн бұрын
Okay takumvani kuti simukupezeka pa FB
@GiftPhiri-tt7nn
@GiftPhiri-tt7nn 11 күн бұрын
More fire 🔥
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 13 күн бұрын
Our gentle men comrade umatiimalira panakati pakhale anthu 20 a Malawi Malawi sibwezi chakwera akutitola ngati akutitolelamu
@user-yh3ys3qn6p
@user-yh3ys3qn6p 13 күн бұрын
😊
@AngolanChinga
@AngolanChinga 13 күн бұрын
Angafune ndani machende machende ameneyo uja
@JeanKambala-gm1zr
@JeanKambala-gm1zr 13 күн бұрын
Emen Mr comlade
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona 13 күн бұрын
Amen 🙏 mulungu amene ndimampelela ine alindimoyo.
@Mcloudkatsabola
@Mcloudkatsabola 13 күн бұрын
From Malawi
@DanielJuwawo
@DanielJuwawo 13 күн бұрын
More fire ntanyiwa
@Nelsonmatenda
@Nelsonmatenda 13 күн бұрын
Comrade mumatiyimila❤
@IsmaelBilal-lh1pi
@IsmaelBilal-lh1pi 13 күн бұрын
Our freedom fighter 💪 🙏
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 9 күн бұрын
Alo akanachoka mpompano mcp ndiyakupha we don't need mcp any more 😢😢 😭 we are tired if this manyi yeniyeni
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 13 күн бұрын
BODZA ILO 😂😂😂😂😂😂😂😂
@user-dd1qq5xq1k
@user-dd1qq5xq1k 13 күн бұрын
More fire Ntanyiwa❤❤❤
@user-rd6zo8ry2d
@user-rd6zo8ry2d 13 күн бұрын
Its true
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 13 күн бұрын
Chakwera akanakhala wa nzelu za umunthu akanangopanga resign chifukwa wether he likes or not walephela kuyendetsa dziko waba pakwana
@ManecasBandera
@ManecasBandera 9 күн бұрын
Achakwera siyani yimeneyo simbariyanu utsogoreri wakuvutani zanu zada apa kalapeni m'charichi kutimunalakwira kumwamba basi
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 13 күн бұрын
Mau akulu big Allah protect like always
@serakillo8668
@serakillo8668 13 күн бұрын
Good msg ❤❤❤
@lyiemanganjira9708
@lyiemanganjira9708 13 күн бұрын
Amen
@anusahjenala1063
@anusahjenala1063 13 күн бұрын
Zoona zooona
@user-zm9nl8zn2b
@user-zm9nl8zn2b 13 күн бұрын
Yet akunka nagwetsa kwacha koma anthu oyipa ngati awa mmmmm timangokunva kuti mcp ndi yoyipa its true aaaaa yalanga anthu kotheratu
@user-hu4gu7op7n
@user-hu4gu7op7n 13 күн бұрын
❤❤
@user-tg3ju1mw9t
@user-tg3ju1mw9t 13 күн бұрын
Mutima mmalo ife a Malawi tili nga nga nga pambuyo panu, asiyeni nasatana awa
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 13 күн бұрын
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you sir
@MuhamadYassin-ye4hn
@MuhamadYassin-ye4hn 13 күн бұрын
Komaso atanyiwah Kuno ku balaka akungo tinamiza aid kulibe ndine Muhammad'yasin
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 13 күн бұрын
Yr days r numberd ulibe ntendere ukuyenda mojowajowa
@KondwaniGronyonyo
@KondwaniGronyonyo 13 күн бұрын
Ndipo ntanyiwa 2025 azakhala pompo kumaonelela mcp ikuluza, God bles you ntanyiwa
@LilianKachala-yz2xf
@LilianKachala-yz2xf 13 күн бұрын
Za ma lD zo polembetsa ma vote ai. Kunonso anthu ambiri Sitinalembetse ku CK
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 9 күн бұрын
Aaaaa wabodza momwe tagulitsira fodya kuno ku kasiya tingakane chakwera akulu inu bodza mudzafa nalo
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 13 күн бұрын
Ndipo agwelemo okha muzina la yesu athu oipa asatana
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 13 күн бұрын
And we will never and support UTm akufuna aputsitse anthu. Ife ndi a dpp, komaso udf. Sitizakujhulupilirani Mai kaliyati zokhazija munayankhula ku maliro a soja lusius banda, we will never trust you again mama. Andale ndioopsa.
@reagangama
@reagangama 13 күн бұрын
Zoona pension akutizuza nayo.Ikambe ñthawi zonse
@user-rm2xv8ys1i
@user-rm2xv8ys1i 13 күн бұрын
Ndipo sitikuchifunadi ndipo tikuona kutalika 2025
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 13 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngat madzi
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn 13 күн бұрын
Comred inuyo ndinu mmalawidi chifukwa kenakalikonse ukukaziwa ndimakhulupililakuti inuyo mwatumidwandithu ndinzimu wothandizila kulilakwa amalawi
@user-jj3oo6jh1l
@user-jj3oo6jh1l 13 күн бұрын
Fire 🔥 🔥 comrede
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 11 күн бұрын
Ma pension anthu Sakupatsidwa
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 13 күн бұрын
Chilungamo zibthu sizilibwino pa Malawi, a Chakwera ndi MCP yake paulendo 2025.
@MerryWayson
@MerryWayson 13 күн бұрын
Ndipo auzeni amve , dzenje limenero ndilao a MCP agalu achabechabe mulungu sangakutae mtanyiwa ndipo mulungu azikutetezani
@user-pl2lj6mh1z
@user-pl2lj6mh1z 13 күн бұрын
Chakwela a choke atikwana palibe chimene akuchita zamanyi
@Robertmkango
@Robertmkango 13 күн бұрын
Mumafunini kumakakhara ku malawi koko ngat bon kakalindo zikakharabwino mukuyakhura nose mulilimozi kumeneko chokani
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 13 күн бұрын
Zazii zenizeni kusowa zochita dzinamizanani chotcho mukhumudwa 2025 chakwela sakuchoka
@KistyNgwira
@KistyNgwira 13 күн бұрын
see
@MuhamadYassin-ye4hn
@MuhamadYassin-ye4hn 13 күн бұрын
zoonad ationjeza azipita
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 13 күн бұрын
Chikungondithela bundle yanga chitsiru ichi
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 13 күн бұрын
Chakwera must go
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili 13 күн бұрын
Auze amvemvemve
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 9 күн бұрын
Chakwela must go we don't want you
@EliphazMaxwell
@EliphazMaxwell 13 күн бұрын
Auzen
@MalekanoChikaonda
@MalekanoChikaonda 13 күн бұрын
Achakwela mwadzka bwanj
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 13 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 13 күн бұрын
Mcp yakupa yangasa
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz 13 күн бұрын
Chakwela mbudzi ya munthu
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz 13 күн бұрын
Mcp yatha
@user-sr4fe5bb2w
@user-sr4fe5bb2w 13 күн бұрын
Ine ndi waku kasiya koma chakwera ndimamukonda koopsya Inu kasiya yake mukunena ya kwa Goliati kapena
@user-jd9yz5hp7y
@user-jd9yz5hp7y 13 күн бұрын
Choka iwe wanyawu kangwele uko ndi buzi limodzi ndi changwera wakoyo
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 13 күн бұрын
😢
@user-qn9vc8em6z
@user-qn9vc8em6z 13 күн бұрын
Inunso ndiomvetsa chison ingokhalan chete
@henryhenry6632
@henryhenry6632 13 күн бұрын
Who cares?
@tasmania527
@tasmania527 13 күн бұрын
You're a big liar. Konseko kufuna kukokera mavotii kkkkk
Zifukwa Zomwe Zingapangitse MCP Kuchoka M'Boma - Concerned Citizen
11:18
- А что в креме? - Это кАкАооо! #КондитерДети
00:24
Телеканал ПЯТНИЦА
Рет қаралды 7 МЛН
Llegó al techo 😱
00:37
Juan De Dios Pantoja
Рет қаралды 22 МЛН
마시멜로우로 체감되는 요즘 물가
00:20
진영민yeongmin
Рет қаралды 31 МЛН
MVAMA CCAP
1:26:09
MVAMA CCAP NKHOMA SYNOD (Rev. Yassin Gammah)
Рет қаралды 3,2 М.
Ku MCP Kuli Nkhanza - Samuel Lwara
25:39
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 10 М.
NKHANI MADZULO APA 22 JULY 2024
16:35
DZIWE TV
Рет қаралды 2 М.
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 239 М.
Usizi Umfazi Womuntu Edliwa Umfana Omncane.
22:44
TRANSFORMATION LIVE
Рет қаралды 27 М.
- А что в креме? - Это кАкАооо! #КондитерДети
00:24
Телеканал ПЯТНИЦА
Рет қаралды 7 МЛН