Zowona zowona zowona mawu oyanjanisa amenewo more fire 🔥🔥🔥🔥 🔥🔥🔥
@chrisboyce2Ай бұрын
Viva Malawi First 🇲🇼🔥 Big up Brother Salo nthawi zonse mumayima pa chilungamo
@user-tb6yh1kx3oАй бұрын
U have said it loud & clear Big up Brother men
@constancemkandawire7378Ай бұрын
United we stand divided we fall tufuna anthu ngati inu ku malawi indeed opposition party Itati imeme ma activists to join forces ku mademo aaaaaaa this ruling party can't stand the heat,enough is enough we are sick and tired of this government. VIva comrades viva
@user-fi7ko7bl6fАй бұрын
Wachiyao samapanga zatulo more 🔥 Mr kumeneko
@user-dy5bj9ck5eАй бұрын
Well done Mr chidzukulu
@bernardnambwe7753Ай бұрын
more fire mumatha
@cacksygustarf6260Ай бұрын
Malawi first❤
@AnaffSayamika-uh6vgАй бұрын
💥💥💥💥
@MustapherLinoАй бұрын
Chakwera ndi mbava
@user-mi3fw1zg8bАй бұрын
Fire mabomba
@douglaskamanga7679Ай бұрын
A brother Salo, Kodi aliyense azi Nena za mtundu wake? Ndipamene timalakwitsila zinthu a Malawi. But Malawi first better not mutundu. Mukuona bwanji? Zapa mtundu ndekuti sizatonsetu
@SolomonNjolomoleАй бұрын
😂😂kung'aluratu 🔥 🔥 🔥.
@GraceLimani-zw7dxАй бұрын
Ndipo ankaona azawo mene amamangira ma demo a chakwera ndi mtambo mpaka anawina
@user-vx5kv8dz3dАй бұрын
Zoona zoona
@user-gg9hw4oj2vАй бұрын
💪💪
@DONNEXKhama-bk1gyАй бұрын
Lets fight together 💪
@marryphili5419Ай бұрын
Zoona tinayika manyaka muboma
@WilliamBanda-o5rАй бұрын
Mwanena chilungamo opposition kugona kwambiri yet akufuna kuzalamulira
Chonde uyu ayenera kumangidwa ayi sikumenyera ufuru uku koma kutukwana munthu sichoncho nde ama khot aziti alibe umbon mene munthu akutukwana president wa ziko kut ndi wakupha nde muziti alibe umboni
@PangolinimwАй бұрын
Mangochi bro imapampadsa makovi or apolice amasiwa kut Mangochi 🙌🙌🙌🙌
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
Brother salo zoona ena amangotokota koma akuopanso
@user-gj4li2gc8oАй бұрын
Ichi ndi chitsiru cheni cheni nde uganiza kut president wa ziko angalephere kumanga kanyumba r u serious koma ngat ndi jealous zikomo ,anthu inu akumwera muli ndi nkwiyo waukulu mene anzanu akuyendesera ziko ndipo ngat Pali anthu amene awononga zikoli ndi inuyo anthu akumwera ndi ma president anu ,kamuzu zikoli analisiya pa bwino koma ndi uchitsiru wanu ,munagulisa ma kampani onse a boma pano mukuvutika mwayamba kulila ndipo mulila zenizeni sitingakuvoteleni kut muzabwelelenso ayi takana
@ThomasPeter-zt2ju29 күн бұрын
Machendeko man Ulibe nzeru
@sarahmphande6108Ай бұрын
Chilungamo chokha choka
@isaacchiwaula731Ай бұрын
Zimenezi ndiye anthu nkumayamikira? Zili ndi phindu lanji? Awawa angayendetse dziko? Basi comment, kuma-commentar zopusa ngat izi? Shame on u. Nokha mukuyankhula kut mumayenda pansi mutavala silipansi while president-yo ali ndi ulemerero, ndie onunkha kukhwapa ndindani 😂😂😂😂😂😂 ndiwe munthu onvetsa chisoni aise
@ThomasPeter-zt2ju29 күн бұрын
U don't know what ur talking mutu wako mwazaza mamina okha oka