Ife sitikumufuna Kuno Ku ndilande chakwera wanuyo tizamupha ndthu asamale
@Wyson-bo3sp5 ай бұрын
Kutsalemekeza msogoleli adayambitsa ndi ndi omwe akulamulilawa. Chomwe umadzala ndi chomwe umakolola. Andele muphunzilepo kanthu. Zilibe kanthu koma president ayenela adzikemekezedwa. Zidachitikadzi zidalakwika
@gracemkandawire876911 сағат бұрын
Koma iyi nde the best discussion,,bravo Wonder and a Bishop osaiwala state Brian
@patrickmacheso50625 ай бұрын
Ndipo Chakwera akuyenera kupeza mavuto oposa awa,, APM anapangidwa zipongwe zoposa izi,, Chomwe anabvala ndi zomwe akukolora lero,, Ndipo I think let's expect more violence between this Government of Chakwera.
@tasmania5275 ай бұрын
Musatinyase apa ndi APM wanuyo. You are glorifying APM as if he changed Malawi in his 6 yrs of power. That old man was sleeping on his job, and the only new thing he can bring into government assuming he is given the mantle of leadership, is enriching fools that have surrounded him- the likes of Chimwemwe Chipungu, Namalomba, Chaponda, Mpinganjira Junior, Chisale, and APM's wife. Ask Liberia; they are regretting electing an old man for president. Why are some Malawian minds still stuck in the past? People have really lost their minds to think APM can change malawi's economy. I think our tribalism and regionalism are making us poorer and poorer. A nation that lacks factories to produce things for export can not transform even if it changes 10 leaders in 10 yrs.
@patrickmacheso50625 ай бұрын
@@tasmania527 I think you have a point but I want to assure you that even APM is old but he's better than Chakwera the Fake Pastor,, People are dying every day with hunger,, and the price of commodities is going up each and every day,, Chakwera is the worst President we never had before.
@emmanuelsambo11585 ай бұрын
The principle of sowing and reaping. APM adagendedwa ku Ndilande. Mchitidwe uwu chonde usapitilire, respect the presidency
@eliffagondewe82145 ай бұрын
Anayambitsa wokha mcp thawi yomwe amapanga campaign 2020 now kukolola anthu a ayankhulana koma amkazitenga zopanda tchito bola mulowe mu boma lero ndizimenezi. 🔥🔥🔥
@user-uc1pd1tc2x5 ай бұрын
Ndipo Chakwera akuyenera kuphedwa basi akangopitanso ku Blantyre
@user-tw2zf7bj3e5 ай бұрын
Abishopu ndagwilizana nawo abusa oyamba ndi osiliza kukhala president zithele pa chakwelayu
@user-hf4xb5ij3o5 ай бұрын
Apm my vote
@kestenlemucha8316Күн бұрын
Bishop-yi waybaponso kuzipangila campaign apa
@amoschataika12845 ай бұрын
Big up Brothers.
@user-qn2nu4xs9i5 ай бұрын
Imfa isanafike pakhomo....ngakhale mphaka, amasowa😢😢😢😢...lero Ma Congo angofa mosadziwika..ntsogoleri kukuwizidwa..azimai kugwidwa ku Cocain...iiiiii.... koma 2024 ithabwino???
@homeremedys37485 ай бұрын
Security yamalawi ili very weak, army comanda akuyenera kutula pansi udindo, izi zikusonyeza malawi defence is very bad, zigawenga zitha kukudilizani mukukanika anthu amaliro opanda nfuti what more zigawenga?
@user-ir4ph3mp7f5 ай бұрын
Zinthu zina zimangofunuka strong power achakwera aaaaa alibe nzeru za usogoleri ife amalawi tikulira mokweza 😢😢😢
@VincentAndrew-jz2gf2 күн бұрын
Kagwireni tchito pls Fokofo
@HildatoweraMhango-et4mz5 ай бұрын
Achakwera chonde apeweko ku ndilande zoona akudzala zomwe anakoloradi koma mulungu watembenuza flag adziwe zimenezo awa aphaso anthu achakwera chifukwa chokalandira chimanga asabwereso ku 24
@MaxwellChiwaya-tv7kn5 ай бұрын
Vuto anthu omwe ali mbali mwawo akumva kukoma ndiye kut awauze APRESIDENT zoona zimawavuta
Zitsilu ndi inuyo pamenepa mumakolezera zinthu zopanda pake. Kodi mulipo angati inuyo? Mwachepa inu ka. Zigwirani ntchito za office. Kodi ndinu andale a Brian Banda? Tulukani mu office. Mumalimbana ndi President bwanji?