Koma munthu waimba bwino uyu, kip it up, osamaopa pa chilungamo
@stevinmuhone877 Жыл бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💃💃💃💃 vuto lake anthu awa sizikuwakhunza or tingayankhure motani mmmmmmmmm
@CalistoZidanna-kj2st11 ай бұрын
Yes !!!this is good music and iyeyo akuyenela ayivere b4 3 hours
@marryphili54193 ай бұрын
More 🔥🔥 ndimomwemo basi ananenadi
@user-dn5sf3md5t3 ай бұрын
KOMATU WABAYA MWANA WELL DONE APSE NTIMA ZENIZENI GALU KWABASI CHAKWERA ANLONJEZAYEKHA ATULEPANSI UDINDO EYAAAAAAA GALU KWABASI NDI BWEREZASO CHAKWERA NDI GALU MBUZI YA MANU PANSI
@josephncekane4567 Жыл бұрын
He sang the best ever song with sense n strong messege. I'm sorry to say this but this government they all Mbuzi I repeat they all Mbuzi, they have not even single feeling of willing to save the people of Malawi
@IshmaelKamwana-sv6bo9 ай бұрын
This is nice songs agalu amenewa tatopha nawo
@amabhohlela.3492 Жыл бұрын
Tiope ndaninso!!!!Chilima ananenakale #OSAOPA.
@ibrahimatibu8784 Жыл бұрын
Akulu wakulu aku malawi koma kuba katundu wa anthu ovutikanso chakwera ndi mwana sakuziwa kathu bola Peter mutharika uja kusiyana ndi izi mbuzizi
@user-ws1eo3rc7l3 күн бұрын
Yomweyo galu iwe 😅
@MourinhoJabur21 күн бұрын
💥💥💥💥💥 chilungamo
@user-eh1mg3ww6d4 ай бұрын
Koma angatule panopa sakugona kufu funa njila yoti adzabele ma voti koma Muthu mmm ayi ndithu m,busa wa satana
Chimuthu chopanda nzeru koma kugokakamira paphando
@user-nf3ik3ff6y21 күн бұрын
Good Messnge Chakwela you mast go
@PatriciaMbewe-xn7ke24 күн бұрын
Ndaimvera mobwerezabwereza😂
@SAULOKANJINGA-fc6ir4 күн бұрын
👍👍
@rasulmaulidi22244 ай бұрын
well done boys..
@user-qm1qb2jp4s3 ай бұрын
Good music with full of msg tonse did nothing but taking malawi to bagamoyo😢
@lamulatusaiti7581 Жыл бұрын
Waimba nyimbo imeneyi mulungu amusogolele ndipo aimbeso nyimbo ina yoposa pamenepa ... Mbuzi zonsezi zimve zenizeni zeni
@enerstntakhala4679 Жыл бұрын
Ndithyole dance koma oimba uyu anaganiza
@chimwemwe2 Жыл бұрын
They should not be intimidating you because its the people that gave them power and thy are now abusing the power by mistreating the same people that gave them power. Keep speaking for the voiceless brother 🙏🙏🙏🙏🙏 I love it❤️
@phillipkapata3790 Жыл бұрын
Kkkkk ndipo ikuvinika guys🤣🤣🤣🤣
@alexjeremanuel254110 ай бұрын
Nyimboyi ili bwino kwambiri 100% ndipo a Malawi pakufunikanso osaopa, osagona tulo ndikuzunzika chifukwa cha magulu ena a wanthu azinyengo, akuba, ozikonda ndi akupha
@WilliamNhlane-fd9hi19 күн бұрын
I'm feeling sorry for people who are in Malawi things are not good on the ground tingotchona mu Capetown
@fridaygonela22 күн бұрын
IZI ndizoona waimba zoona titsatile sadick Mia ndi achilima
@user-gs7wc3nx3qАй бұрын
Kkkkkkk iwe wayimba bwino wava ndipo usaope ayi pitiriza man
@angellasamuel8186 Жыл бұрын
Koma guys alusonu tamati fikisilani mauthengo ndipo musamaope akufuna azitiopseza akapolowa mphenvu dyera Ku nthiko
Umatha ayise ndikanakuziwa ndika naku pangira order pa Mukuru 1000 rands
@Extratremendouszeus24 күн бұрын
Bola akanalonjeza kut tidzamudule mutu akakana kupanga resign Km mutuwo tikanadula ? 😅😅😅😅 MCP WOYEEE😅
@user-zv1so2pd7u Жыл бұрын
😂😂😂😂😂😂😂💯
@jagudanicolas5436 Жыл бұрын
Or chakwerayo wa ikondaxo atule pansi basi
@africulturetv6498 Жыл бұрын
True cry
@lamulatusaiti7581 Жыл бұрын
Inu zoona chimanga kugula anthu pa mpaka k 25 000 thumba limodz chimanga chomwe chimagudwa k 4000 kapena k 5000
@bilalikamwendo1629 Жыл бұрын
Odiiiiii ndijaze ine 💃💃💃💃💃💃💃💕💓💓💓💓 Chakwela atule pasi udindo waulephela komaso akadulidwe m.jando kut adziganiza dzabwino🤐
@user-ic4qi7yy5l11 ай бұрын
Koma zongo paikana izi kuti aziti nyimbo iyi waimba ndi Billy kaunda pomwe wina wangotenga instrument ya billy yagalatiya koma voice yaleka naso Billy akaimba mau amaveka ngat alindichifine koma awa ati ayesere zawakanikaso!!