Very true Madam, we need to have strong party for alliance
@user-qq1uj7ct6n26 күн бұрын
Zipani zonsenzi zili pansi pa DPP. so lingaliro labwino kubwerera Ku DPP watching from Cape Town
@EmmyYafete26 күн бұрын
Very true mandam ,ndazikonda kwambili bwerelani kwa amai anu basi tingwetse MCP ,
@Namphuno25 күн бұрын
You have proven to have big brains than other men in UTM, you have our support
@paulkalizangoma590426 күн бұрын
This is what Malawians were waiting to hear from you. You made a right decision. Thumbs up to you all. We are fully supporting you, and we shall be behind you forever.
@EnetChiomba26 күн бұрын
Eishii koma apapa zikhala bwino bwanji ndipo zitero ndithu❤❤
@augustMag26 күн бұрын
Mau amphamvu Mai atigwira mtima Bambo wanu APM akulandilani ndi manja awiri sangalore kuti ana Ake asowe kopita iye qlipo
@LubaniLameckmbewe26 күн бұрын
I totally agree with you
@MarcosDjussa16 күн бұрын
Komatu amai awa alankhula zomanga Malawi wasopano God bless you mama
@BentryMwagomba26 күн бұрын
Thanks madam for the advice
@PeterNamphwanya26 күн бұрын
You is best futures ❤❤ 100% that's one plan A not B ❤❤❤❤❤❤❤🎉
Thenks utm popangangwilizano ndi dpp atiphera saulosi achoke fayaa
@SteveChapola26 күн бұрын
Mai kaliyati libikisani anthu ife sitifuna mcp
@SolomonNjolomole26 күн бұрын
Bravo madam I second you❤❤
@user-wb3us4pg4b26 күн бұрын
kod ndindan mai akukamba zanzeru yi
@user-te4ii6sz2v22 күн бұрын
This is practical and very positive politics. Let's follow this path. I never new that in UTM there are some pipo who think like this. There is so much unnecessary noise which pipo think is politics but nope. God bless you.
@user-fi7ko7bl6f25 күн бұрын
That's good idea Ma, l salute you 💪💪 power to the people.
@user-hu7qs5be4j26 күн бұрын
May wanzelu kwambiri inu 😊
@RodreckSamikwa26 күн бұрын
Powerful ❤
@miketholiwa176224 күн бұрын
Brilliant idea. Ichoke MCP
@masterchitabwino89826 күн бұрын
UTM ndi DPP palibe udani if anything UTM yabadwa kuchokera ku DPP. Peter is cool ndiyemwe anamukonda SKC kuti ayambe ndale.
@isaihmagani569726 күн бұрын
Chabwino ndakumvani nde tinene kuti UTM itsogole ngatidi Pali kumvanadi
@user-lp8wj3vq4x26 күн бұрын
Well done mama nkhani.imeneo ndiyabwino tiyeni ku dpp. Amene akufuna ku mcp sianthu.amenewa