Wazipeza zitsilu Ku chiladzuluko, osakuthamangitsa?
@hmshohagshohag94832 ай бұрын
Palibe chanzeru mukukamba inu, Chakwera anakupeperesani kale apa Chilima wanuyo azamuvotera ndi ambuyake .kodi a Amalawife mumatitenga ngati zitsiru eti
@user-hy4el8ov1l2 ай бұрын
Muthu wandale ndi satana lero akubwela ndi boza 😂😂😂
@LovemoreSalima2 ай бұрын
Huleyutu wayamba Tikuthamangitsatu ndi maduka, Usamale hure iwe.
Kkk koma malawi eee alibe manyazi akwen inu mwano wake
@francisvisage27052 ай бұрын
Musagawe nsalu inu, gawani chimanga ndi kukwanilisa munalonjeza
@binalidjeyshabahzombamalawi2 ай бұрын
Mbuz yosafunikira kaliat
@user-hm9nc7lz6e2 ай бұрын
Patrisha kawanamidze ana ako osakhala wamkulu ngati ine mmanfesto yanun : mwapanga chani mdiwe chisiru iwe kwabasi koma ndiwe wabodza eeeeeeereee satana
@PleasantMagombo2 ай бұрын
Anthu osowa zochita awo.
@JonesChingaya-yf4gg2 ай бұрын
Mau amati awiri sayenda limodzi asanapangane, inuyo m'mene mumalowa mu alliance munagwirizana lero musayambe kusintha chichewa kamba koti zakuvutani. Zipitani tiyese anzanu, anzeru si inu nokha ndi a Chilima kulinso ena.
@FrancisNyayiАй бұрын
Kodi mwanva speechyi anzanga ine sinkunva mpaka ndaika bluetooth ine 😢
@chikumbutsomarch44842 ай бұрын
Manyazi mulibe
@musamakanjira2 ай бұрын
Wati ma Mp ali ku boma komweko alephera nanga Saulosi si ali ku boma konko
@user-is5dl7np9g2 ай бұрын
Palibe chamzeru chomwe mukunena mayi opusitsitsa inu, a malawi mwawatola
@LinessiTambala2 ай бұрын
Mwachedwa
@user-iu3bf6oe1x2 ай бұрын
Amp my vote
@lingstonenagoli77292 ай бұрын
Mayi asazampatsabe mpando,anthu oipa akuononga dziko ndi awa
@user-vu9rt8gj3o2 ай бұрын
Mbuzi iweee
@ThoccoBondo-mx7vt2 ай бұрын
Aaaaaaaa nanunso mwasowatu zokamba wadya katatu ndani inunso anthu ndi omvesa chisoni kwambiri fertiliser wosaka mtengo mwamugula kuti mitu yanu mwaiwala nsanga nsanga
@innocentnjoka70142 ай бұрын
DPP woyeeeeee❤❤
@GodsonLindan-hn4kp2 ай бұрын
Akaliati ndinu chitsilu eti, ndinu munthu opanda chisoni.ndichifukwa mumawasiya mai anu akuvutika ndi basiketi ya tomato galu. Ngati chilimayo Ali bwenzi lanu ndie mwauponda.
@PeterPhiri-nd6op2 ай бұрын
Sopano apa muli muboma bwanji osapanga zosezi agalu inu
@llewellynkhungwa47122 ай бұрын
Kweee is back....💪
@user-pb1yr1jx5gАй бұрын
APM MY VOTE ❤
@HarryRefred2 ай бұрын
Ukuzikolakola wekhatu 😂😂😂😂😂 muziwona katatu😢😢
@TressLuka2 ай бұрын
Munatigwilitsa fuwa lamoto Inuuu aaaa😢
@KereeditseMotsetseАй бұрын
Kalonga ndi chilima machendako nose agalu ndionukha kumatako kaliyati mayi
@user-hy4el8ov1l2 ай бұрын
Mayiwa ndi aboza 😂😂😂
@user-lg1bw8fx5m2 ай бұрын
Zakudya katatuzo tazisiyani izo yambani Zina komaso ngat ndale mwatopa nazo muyeseko business ya kaunjika musatichimwitse
@user-vp5mf6bd3o2 ай бұрын
Ndinu mai ovesa chisoni mulungu sakondwera ndi boza ngati limeneli
@NgomaRaheem2 ай бұрын
Zopusa et azakuvotera amako galu Chilima wakoyo azikalamulira kunyumba kwako demet fertilizer K4.595 alikut
@PeterThawi-jc7zlАй бұрын
Kodi fredokiss akutaniko uku😂😅😂😂😂😂😂😂😂
@spargomw2 ай бұрын
Palibe chanzeru chomwe mwayankhula.Ulendo uno simutinamizaso. Malawi pano adazindikira ndipo zimenezi muziyankhula mnyumba mwanu nd ana anu
@farlenmkorongo2 ай бұрын
Vuto simumaziwa kuti vice president ku malawi amachita kutumidwa ndi president, nde ngati president anamuyimisa iyeyo akanatani
@user-ov7yw4bq7y2 ай бұрын
Koma amalawi maona ngati chani? zobvetsa chisoni truck yansalu ithandiza chani pamoyo wa munthu mulungu awone anthu awa
@user-hm9nc7lz6e2 ай бұрын
Iwe usatitenge ngati ndi chisiru wamva amalawi timazithandidza tokha sitimadadalira prezdent
Mzimai oipa uyu za dpp unasunga zija ukabweze kwa eni aka adad mzimai oipa iwe
@isaacchipatala16182 ай бұрын
SKC my vote
@Mustapher-fb4qpАй бұрын
Amasuleni anthu abwerere ku dpp
@Blessings-td4cr2 ай бұрын
Awa ndi mamafiya,,,fundo zao zikuwakola okha,Iwo alikuti panopa? Tonse alliance adapanga ndi ndani? Mwapanga dala kuthesa mulandu kuti mutinyasepo panopano.
@MAPAGASTUDIOS2 ай бұрын
Tentiyo a dpp anakubwerekani yosachapatu komaso zakuti mukutibera misonkho mubomamu zodziwa chilima wanuyotu osangobwerera pambuyo bwanj mpepeseni APM basi
@AngungaThatcherNgoma2 ай бұрын
Onse a ndale ndi a BODZA. DPP, UTM, MCP, e.t.c, e.t.c nga BODZA. Dziko lino likufunika lilamulidwe ndi Asirikali basi. Am tired of the Politicians. Maganizo anga.
@mcsellahntv68962 ай бұрын
Onse Alliance sopano, eeeeh! Mbuzi zokhazokha.
@isaacchipatala16182 ай бұрын
UTM for life
@fatsanichibwana94382 ай бұрын
DPP WOYEEEE!!!
@user-le9su3mt7r2 ай бұрын
Dpp tatopa nawoo apanga Chali mbili zakale
@KereeditseMotsetseАй бұрын
Amayi kaliyati pakholopako
@PeterThawi-jc7zlАй бұрын
Ku Malawi kuli zipani ziwiri...osamanamizana ma kape Inu.MCP and DPP basi.enanu mukutaya nthawi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂