Wina aliyese osauka amene mane a kt chakwela ndi boma lake lili bwino ameneyo amagwa khunyu srs mutu siukugwila (shit)
@amadichembe40689 ай бұрын
Mwaswela bwanji achimwene anga Kodi nkhanga zilipo? kkkkkkkkk I like it nkhanga zaona
@ashikalam86169 ай бұрын
Big up Big man ❤😅
@user-nz8mq4ff3e9 ай бұрын
Nkhangaaaaaaaàaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaasaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaàaaaaaaaaaaassssaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaàaaaaaaazaoooooooooooooooooooooooo oooooooooooooooooooooonmwadzuka bwanji a Malawi anzaga kulikonse kumene muli Lelo pa 4 th october this Mr tanyiwa Limpopo AFM Rodio
@BILLYMACHOMBE-fw5nn9 ай бұрын
hugs great to Great
@robertchitsulo80069 ай бұрын
Nice
@user-wd7lk7nx7m9 ай бұрын
Chikwera galu weniweni
@ArmandosebastiaoLano-yw5iv9 ай бұрын
Fire
@alickalick65099 ай бұрын
Chakwera amawona ngati ndizophweka kukhala otsogolera dziko apa waziwonera yekha basi akapume sitikumufunanso amutengenso Chilima onse achokepo
@MathewsMANDUTU-lh6oo3 ай бұрын
Mvuto ndife amalawi kutengeka,,,,, muzadya katutu,,, thumba la fertilizer 4,500,,, passport 14000,,, ndi kutengelani ku Canaan,,, Maka ndi utsogoleri wa chakwera, ameneyi ntchito zake ndi zitatu monga satana, kupha, Kuba, ndi kuononga. (Capetown south Africa)