Kod inu mukut 82yrs kwa Merica Joe Biden sikhalamba koma sakulamulira kod anthu inu chakwera akukusangalasani chan makamaka monga simukuwona zithu mene zikukhalira dzikomo simungasiyanise iyayi ndi nthawi ya dad nonse amene mukudana ndi adad. Nonse ndinu afiti mumatamba ndi chakwera agalu
Chibanja party mbolizanu ndi gogo wanuyo lwalani zowona...
@Musa1828-l5d7 күн бұрын
Dzitsiru inu boma tinalanda bhobho apa mukuphaso Chilima siuchitsiru umeneu
@user-pt8wb4vw6r7 күн бұрын
Wopanda manoyo sitikumfana ayi
@BrightLuciano7 күн бұрын
Adadi omwewo
@user-mk7fh5ml8s7 күн бұрын
Dpp bomaa!!
@user-gj4li2gc8o7 күн бұрын
Za zii chipani Cha ufumu ichi
@TaweniChavulaKamwendo7 күн бұрын
Eee
@GeorgePhiri-ub2of7 күн бұрын
Zopusa ku dpp kulibe dimockalase
@SaidiMbawa-st6bj7 күн бұрын
Madala team
@felixsaidi67157 күн бұрын
Ndee yabwino kusiyana ndi m'BUSA WAKUBAYI
@SaidiMbawa-st6bj7 күн бұрын
@@felixsaidi6715 ubwino wake aliyese ali ndi masapota ake
@UseniMailosi7 күн бұрын
Motor kuti buuuu
@Bonisiwentamo7 күн бұрын
Mafuno abwino dpp mwaChitabwino
@marryphili54197 күн бұрын
More 🔥🔥 DPP tikufuna zomwezo basi
@GeorgePhiri-ub2of7 күн бұрын
Dpp inatha kalekale kunangokhala madala peter ndi anamalomba basi ndiye pawipa pali mtsogoleli apa? Zazi kaya kwanu konko ife kuno kuibeko
@Extratremendouszeus7 күн бұрын
Inu ndimasapota a aweta ng'ombe.tikudziwa...zifwamba
@RaymondKaumba7 күн бұрын
82yrs ..state house is not old age home
@WilliamKawina-y7d7 күн бұрын
Ma advisers a Peter sakumulangidza bwino,nthawi yomwe mukufuna kutenga boma simumachosa anthu.koma zomwe akupanga a dpp mmm zoti akupwetekeni ndi omwe mukuwachosawa kaya akudziwa.msonkhano kungopanga kamodzi basi
Kkkkkkkk guys mumatha kuyankhula Nigeria ndidzika lolemela kwambila Pano pa Africa Lili number one president wao ndiwakulu kuposa Peter America is richest country in the world Koma president wao Joe Biden ndiwakulu tikufuna Peter abwelele mu boma
@spargomw7 күн бұрын
Oro atakhala nd zaka 120 ife tikumufuna, zitsiru za chinyamata zili m'boma panozi zikupanga chani? Chikuni chachikulu kusunga moto.❤❤❤❤❤ Peter❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉
@user-gj4li2gc8o7 күн бұрын
Useless party ever
@user-rz9rm4cb8x7 күн бұрын
Useless ndi ambuyako a lazalo
@ZionekaMember7 күн бұрын
Ndinaziwa kut upanga comment zosemphana ndi gulu wadya zambiritu
@ShamilahSaizi6 күн бұрын
Ndipo alibe manyazi amapanga comment za dpp Malo moma comment a za nyau zinzakozo. Manyazi mulibe
@GeorgePhiri-ub2of7 күн бұрын
Chapani chabanja zazii zenzeni
@bisweckchimphamba84977 күн бұрын
Wa MCP sasowa ndipo mudzamudziwa ndima comment ake,uli ndi ufulu nawenso kukayamba chipani chako mnyumba mwakwanu
@ChristopherBokosi-gx4bm7 күн бұрын
Koma pali anthu amasapota coz amachekela chigawu chapakati chakwela his useless president to be honest here guys we have to stand together as Malawians to search a good leader chakwela is useless leader is better to bring DPP back again