KU HOT CURRENT KWATENTHERATU

  Рет қаралды 16,009

HOT 265

HOT 265

12 күн бұрын

Пікірлер: 45
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 10 күн бұрын
Hee bwanji pamaliro achilima munalephela kusegula mlomo chochi bwanji simunena kuti chakwera ali ndi dyela loipa mpaka kupha munthu sure chifukwa cha 5years😢😢😢 machende ake
@user-lb6ek3ee6d
@user-lb6ek3ee6d 10 күн бұрын
Malawi ndi chitsazo chabwino cha kusauka koma zikukhala zovetsa choni kwambiri mpaka pano ma President adakalibelabe a Malawi ndi President yekhayo yemwe amandisangalatsa Professor Dingu wa Muthalika zimu wawo ukuse mu ntendere adasitha zithu kwambiri osati izi tikuziona panozi manyaka enieni the must go out stupid Government
@yusufbakali
@yusufbakali 10 күн бұрын
Nduna zaboma zosezakuba zimangidwe it only one way katangale akhoza kuta akamangidwa no belo ndende basi akagwire
@stevenchirwa5028
@stevenchirwa5028 10 күн бұрын
Don't just talk we need action to change Malawi 🇲🇼
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 10 күн бұрын
Kkkkkk anyamata inu leroli ndakupatsani 100 pa 100 ❤❤❤ guys iyiyi ndiye hot current
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 10 күн бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏Anyamata lero muli bwino kwambili 🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@ahmedmsume1489
@ahmedmsume1489 9 күн бұрын
Akuonesana zikwanje inu lero mwatasa 😂😂😂😂
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 10 күн бұрын
Abida mia wapelekera bwino kwachakwera😂tiona dzinthu yakumbuyo😂😂
@JustinChiwale
@JustinChiwale 10 күн бұрын
Khoswe akakhala pakhate sapheka Malawi we can't fight against corruption
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 10 күн бұрын
Lelo mwayakhula zokomela athu osaukano. Osati zachamba zanu zinja.
@williamdaka79
@williamdaka79 8 күн бұрын
Apo mwanena ndithu omva amva
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 10 күн бұрын
Ajona mwamvatu malango anga kkk cz ndeumabowa bolako lero ❤
@RaymondKaumba
@RaymondKaumba 9 күн бұрын
Vuto ndale zanthu zimapatsa mphanvu president.koma democracy parliament ndiyomwe imakhala ndi mphanvu yolemba ACB director azipanganso report Ku parliament basi
@SamukLungu-zg7fl
@SamukLungu-zg7fl 10 күн бұрын
Talk guys we are together but don't eat baz from chakwera
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 9 күн бұрын
Kumalawi tili ndivuto katangale sangathe. Chifukwa ndi culture. Katangale ngati mukufuna kuti athe choyamba president akhale oopa Mulungu komaso akhale osanama chachiwiri azikhala ndinthawi yotendera ma office mwazizuzi osawawuza anthu ogwira ntchito. Chachitatu a police a traffic army ikhale yachilungamo ndipo asavere boma pankhani za katangale. Simungathane ndikatamgale pamene oteteza ziko ndi amene akuchita katangale ndiye mukugani anthu angasiye katangale
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 9 күн бұрын
Nkhani ya police kuti alibe uniform sapata zili bwino ngati akuvutika choncho chifukwa apolice wo ndi amene akumanga anthu akamazuzula boma so azivutika motero
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 10 күн бұрын
Kuti katangale kuti athe muphe chakwera ndi chimbava choipa kuchokela kumpingo that's why he kill chilima
@TarPoor-ye9jx
@TarPoor-ye9jx 8 күн бұрын
Lero ndaziwa kut anthu chilungamo akuchziwa koma mantha mcp ndi chakwera anthu atopa nawo kkkk 😂😂anthu amaba koma tonse yalepera pazonse kuba kuli pa high too much
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb 10 күн бұрын
Amene sanachimweko ayambe kumugenda miyala
@StevenMjMbama
@StevenMjMbama 10 күн бұрын
Guys big up kwinako muzitchulako mayina aaaanthu amene akumapanga katangale
@IssacMateyo
@IssacMateyo 10 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@g_forcemusician4242
@g_forcemusician4242 10 күн бұрын
2025 we choose wisely
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 10 күн бұрын
Bon kalindo anayakhula kt aku prison akudandaula kt iwo palibe amapita muziwaganizila km mukati wamisala
@Austinyonah
@Austinyonah 10 күн бұрын
Kuyankhula kwabwino
@AustinNkhula-j6y
@AustinNkhula-j6y 10 күн бұрын
Ttv awunikileni anthu aziwe zenizeni tatopa ife ndianyapapiwa
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py 10 күн бұрын
Ambuye mulungu wanga mudapereka mwana wanu modzi yekha yemweyo kufera ifeyo ochimwa kudzuzika yesu chifukwa chaife , kodi ngat mudalora mwana wanu modzi yekha kufera ife ,simungalore yehova wina osakhala mwana wanu kuti angofa yekha kutulo osadwara ai kuti afere ifeyo amalawi tatopa naye ndiy skhale Chakwerayu ambuye ndimvereni mbuye wanga Chakwerayi atifere ife chifukwa wanyañya tikumvutika musadzuze ndimatenda ai akangogona apitilirekonko kuti tipume mbuye wanga ndimvereni yehova chskwerat akutidxuza musakhare chete yehova akhoza kumayesa ngat mulibe phamvu ngat safera kutola koma afeeee chakwera kuti nduna zake ziziwe kuti inuyo mdinu owopsa yehova
@AustinNkhula-j6y
@AustinNkhula-j6y 10 күн бұрын
@@Trancy-xt4py eee koma yaa
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o 10 күн бұрын
we shall be singing like this for how long
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 10 күн бұрын
We need to change this leadership
@Moses51
@Moses51 10 күн бұрын
Chakwela ndigalu kwabasi
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 10 күн бұрын
Lelo maimatu pachilungamotu kunenachoona chomwe ngakhale ife akumudzi tikuziona masomu boma ili linangolowelamo Kuba basi, chifukwa chilima anangomunamizila kuti apeze mphata Obama bwino, after kuona kuti bodza anapangila chilima kunamizila Kuba, anaona kuti kubako otsogolela anali chakwela chifukwa anatetsa mulandu cholinga amuphe chifukwa anadziwa kuti chilima amadziwa zonse. Chakwela chakwela iweyo mulungu azikupangila za bwino
@Moses51
@Moses51 10 күн бұрын
Aphana 🤣🤣🤣🤣
@IssacMateyo
@IssacMateyo 10 күн бұрын
Aona nyekhwe 2025
@DalitsoulNchengah
@DalitsoulNchengah 10 күн бұрын
Ulemu wanu
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 10 күн бұрын
Anthu ena anagontha ku makhutu chifukwa cha matemberero
@HarryMsudzula
@HarryMsudzula 10 күн бұрын
Sinanga ntchito zina akanatha kugwira aprison like kugadira mayeso ameneb anaipereka ku mdf omwe sizimayenera kutero malinga ndi nature yantchito yawo
@KanjoIsaac-u1w
@KanjoIsaac-u1w 10 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkk
@SandramKambalame
@SandramKambalame 10 күн бұрын
Boma ilili ili ndi manyaka
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 10 күн бұрын
Kikikikiki
@MusaManati-ho4zf
@MusaManati-ho4zf 10 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 10 күн бұрын
In Malawi we consider corruption as a problem.It is not a problem but the result of something.Therefore,to end corruption in Malawi we must list down main causes of corruption and get rid of them.
@giftmwango3214
@giftmwango3214 9 күн бұрын
You don't know what you are talking about
@IssacMateyo
@IssacMateyo 10 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@IssacMateyo
@IssacMateyo 10 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
Clowns abuse children#Short #Officer Rabbit #angel
00:51
兔子警官
Рет қаралды 57 МЛН
БОЛЬШОЙ ПЕТУШОК #shorts
00:21
Паша Осадчий
Рет қаралды 10 МЛН
Chihana speaks tough
6:38
Suleman Chitera TV
Рет қаралды 71
DALITSO KABAMBE CHIFUKWA CHANI ADATULUKA DPP.
26:26
HOT 265
Рет қаралды 7 М.
Clowns abuse children#Short #Officer Rabbit #angel
00:51
兔子警官
Рет қаралды 57 МЛН