Hee bwanji pamaliro achilima munalephela kusegula mlomo chochi bwanji simunena kuti chakwera ali ndi dyela loipa mpaka kupha munthu sure chifukwa cha 5years😢😢😢 machende ake
@user-lb6ek3ee6d10 күн бұрын
Malawi ndi chitsazo chabwino cha kusauka koma zikukhala zovetsa choni kwambiri mpaka pano ma President adakalibelabe a Malawi ndi President yekhayo yemwe amandisangalatsa Professor Dingu wa Muthalika zimu wawo ukuse mu ntendere adasitha zithu kwambiri osati izi tikuziona panozi manyaka enieni the must go out stupid Government
@yusufbakali10 күн бұрын
Nduna zaboma zosezakuba zimangidwe it only one way katangale akhoza kuta akamangidwa no belo ndende basi akagwire
@stevenchirwa502810 күн бұрын
Don't just talk we need action to change Malawi 🇲🇼
@user-un6qv6sj3h10 күн бұрын
Kkkkkk anyamata inu leroli ndakupatsani 100 pa 100 ❤❤❤ guys iyiyi ndiye hot current
@RobertLuka-wy9cl10 күн бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏Anyamata lero muli bwino kwambili 🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@ahmedmsume14899 күн бұрын
Akuonesana zikwanje inu lero mwatasa 😂😂😂😂
@AlexKaunda-ny2eg10 күн бұрын
Abida mia wapelekera bwino kwachakwera😂tiona dzinthu yakumbuyo😂😂
@JustinChiwale10 күн бұрын
Khoswe akakhala pakhate sapheka Malawi we can't fight against corruption
Vuto ndale zanthu zimapatsa mphanvu president.koma democracy parliament ndiyomwe imakhala ndi mphanvu yolemba ACB director azipanganso report Ku parliament basi
@SamukLungu-zg7fl10 күн бұрын
Talk guys we are together but don't eat baz from chakwera
@thulanimpphiri68739 күн бұрын
Kumalawi tili ndivuto katangale sangathe. Chifukwa ndi culture. Katangale ngati mukufuna kuti athe choyamba president akhale oopa Mulungu komaso akhale osanama chachiwiri azikhala ndinthawi yotendera ma office mwazizuzi osawawuza anthu ogwira ntchito. Chachitatu a police a traffic army ikhale yachilungamo ndipo asavere boma pankhani za katangale. Simungathane ndikatamgale pamene oteteza ziko ndi amene akuchita katangale ndiye mukugani anthu angasiye katangale
@thulanimpphiri68739 күн бұрын
Nkhani ya police kuti alibe uniform sapata zili bwino ngati akuvutika choncho chifukwa apolice wo ndi amene akumanga anthu akamazuzula boma so azivutika motero
@AlexKaunda-ny2eg10 күн бұрын
Kuti katangale kuti athe muphe chakwera ndi chimbava choipa kuchokela kumpingo that's why he kill chilima
@TarPoor-ye9jx8 күн бұрын
Lero ndaziwa kut anthu chilungamo akuchziwa koma mantha mcp ndi chakwera anthu atopa nawo kkkk 😂😂anthu amaba koma tonse yalepera pazonse kuba kuli pa high too much
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb10 күн бұрын
Amene sanachimweko ayambe kumugenda miyala
@StevenMjMbama10 күн бұрын
Guys big up kwinako muzitchulako mayina aaaanthu amene akumapanga katangale
@IssacMateyo10 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@g_forcemusician424210 күн бұрын
2025 we choose wisely
@paulpaseli631010 күн бұрын
Bon kalindo anayakhula kt aku prison akudandaula kt iwo palibe amapita muziwaganizila km mukati wamisala
Anthu ena anagontha ku makhutu chifukwa cha matemberero
@HarryMsudzula10 күн бұрын
Sinanga ntchito zina akanatha kugwira aprison like kugadira mayeso ameneb anaipereka ku mdf omwe sizimayenera kutero malinga ndi nature yantchito yawo
@KanjoIsaac-u1w10 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkk
@SandramKambalame10 күн бұрын
Boma ilili ili ndi manyaka
@peterchikwakwa847610 күн бұрын
Kikikikiki
@MusaManati-ho4zf10 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@augustinechibbalazi889710 күн бұрын
In Malawi we consider corruption as a problem.It is not a problem but the result of something.Therefore,to end corruption in Malawi we must list down main causes of corruption and get rid of them.
@giftmwango32149 күн бұрын
You don't know what you are talking about
@IssacMateyo10 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@IssacMateyo10 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe