KWANUNKHA MWAZI KU MCP.

  Рет қаралды 38,879

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

11 күн бұрын

Пікірлер: 123
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 9 күн бұрын
❤❤❤iyiyi mwanena zogwila mtima lero mwaonetsa u independent wa times keep it up
@rosekaliwo5547
@rosekaliwo5547 9 күн бұрын
Ulamuliro wa nkhanza inde pano school fees anthu tikulephera kulipira ndiye Ana aphunzire motan mmmm ambuye atithandize
@user-zq3li3qw1m
@user-zq3li3qw1m 9 күн бұрын
Zoonadi
@xinalungu9616
@xinalungu9616 8 күн бұрын
For the first time Malawi can see great roads not just miyala ya madziko. I pray that Malawi wakes up. We should wake up n balance our forums
@rameckmauranagerald9783
@rameckmauranagerald9783 7 күн бұрын
Kuyakhula mopanda mantha. Komaso mwaphawi zofunikira kwaose amalawi pabwino mkuyamikirana. Poipapo dzuzurani, rangizani akapanda kumva arekeni!!!!🎉
@user-lw2yp1rf4n
@user-lw2yp1rf4n 10 күн бұрын
Iyiyi nde yandifikapo ndithu big up Hot current 💪💪
@BwanaGD
@BwanaGD 9 күн бұрын
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 9 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@RobertCosmas-bo1uo
@RobertCosmas-bo1uo 8 күн бұрын
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@IshumaelMbewe-d4t
@IshumaelMbewe-d4t 9 күн бұрын
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@ElizabethMajiga
@ElizabethMajiga 9 күн бұрын
Apa ponkhapa mwawalakhulila amalawi🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@GiftNyirenda-q9d
@GiftNyirenda-q9d 7 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i 8 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@user-sw6rz4tz3z
@user-sw6rz4tz3z 6 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@blessingsfalamenga4575
@blessingsfalamenga4575 6 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 6 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@louisgolden
@louisgolden 9 күн бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@user-em3xq2th4g
@user-em3xq2th4g 21 сағат бұрын
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
@stevephiri1043
@stevephiri1043 8 күн бұрын
Mmoziyi ndamene amalakwisa program amakonda kuwatchinga azinzakewo kuti asamasuke
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 9 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf 7 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@ChettoSongeah
@ChettoSongeah 6 күн бұрын
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
@Erickasonya-uw8yw
@Erickasonya-uw8yw 6 күн бұрын
Bravo guys mumakwana
@kotking-xg7pp
@kotking-xg7pp 9 күн бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 9 күн бұрын
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
@HastingsJonathan
@HastingsJonathan 8 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@jelsonmlowoka8611
@jelsonmlowoka8611 9 күн бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 9 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
@user-em3xq2th4g
@user-em3xq2th4g 21 сағат бұрын
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 9 күн бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 9 күн бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 9 күн бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
@FosterMatchano
@FosterMatchano 8 күн бұрын
I like the conversation
@francismungu7749
@francismungu7749 8 күн бұрын
Guys mwasiya kugawa ma sweet ulemu wanu. Timayesa nanuso akudyesani chibansi
@khwimamtonga954
@khwimamtonga954 9 күн бұрын
Mmmm Zikhale Ng'oma nawoso akufuna u Vice President ku MCP? Mmmm awa ai body structure
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 9 күн бұрын
Kkkkkkk 🔥🔥
@user-un8yq1gg2i
@user-un8yq1gg2i 8 күн бұрын
Hahahaha koma iyiyi nde ndiyong'alura kuyipatu kkkkkkk
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 8 күн бұрын
Hahahaha akuti 👇 "Sitidya kwanu!" 😅😅😅😅
@user-no5eb7rp1o
@user-no5eb7rp1o 9 күн бұрын
Eeeeee anyamata relo mwatokota kkkkkk muli bho kwambiri mwaveka ❤❤❤
@xinalungu9616
@xinalungu9616 8 күн бұрын
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@OssmanAbubaker-l5s
@OssmanAbubaker-l5s 5 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 9 күн бұрын
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 8 күн бұрын
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 8 күн бұрын
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
@christophermukaka7403
@christophermukaka7403 6 күн бұрын
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
@sparkdymon3429
@sparkdymon3429 9 күн бұрын
Iyi koma mwang,alulandi makosana abwana kutundako azizifusa makamaka achekwela ndimbava ndifukwa akopa ACB
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i 8 күн бұрын
Iyi ndye hot current yen yen 🔥🔥🔥
@mustafahassan9128
@mustafahassan9128 7 күн бұрын
Koma ndiye mwanena mosanyengeleratu
@user-to5of3ks3g
@user-to5of3ks3g 9 күн бұрын
Nice message
@obviouskedson6483
@obviouskedson6483 9 күн бұрын
Ife timamva nanu kukoma chifukwa mumayankhula chilungamo ,ndipo nthawi ya program yanuyo muionjezele mabwana
@user-sw6rz4tz3z
@user-sw6rz4tz3z 6 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 9 күн бұрын
Yeah! This is hot for sure.
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 9 күн бұрын
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 9 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 9 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 9 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 9 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
@yamiecharles
@yamiecharles 10 күн бұрын
Mmmmm tiyeni ticheze bwino
@MemoryKamanga-jv4jh
@MemoryKamanga-jv4jh 9 күн бұрын
Number one brothers
@sulleahmnyimbili1362
@sulleahmnyimbili1362 9 күн бұрын
Well spoken
@EugeneChiyenda
@EugeneChiyenda 9 күн бұрын
Kma iyiyi mwang'alula🥳
@DalisoulThom
@DalisoulThom 9 күн бұрын
Chanzelu apha chilima+anthu 8 kumphatizapo kasambala
@StevenFombe
@StevenFombe 9 күн бұрын
Why big people wear tinted sun glasses
@abunaseem6866
@abunaseem6866 7 күн бұрын
Ku painter eti?
@raytavares2256
@raytavares2256 9 күн бұрын
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
@augrinngunga8031
@augrinngunga8031 8 күн бұрын
Mwalakhulako zazerutu, mukamadya ma bazi guys times izakhala Ngati MBC yoonera achakwera okha
@fatimautilah5648
@fatimautilah5648 9 күн бұрын
Ati sitidya kwanu kmatu Mr wonder
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 9 күн бұрын
Watopera akanganya amenewa.
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 9 күн бұрын
Vuto lolandililatu zanu tinkhope tanuto nditamanyaziii😢
@sungirenikampu8630
@sungirenikampu8630 9 күн бұрын
Guys mumatha keep it up
@user-zo3bf3ec3g
@user-zo3bf3ec3g 7 күн бұрын
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 9 күн бұрын
Koma zikhale ng'omayo nde ayi aaaaa
@JuuuKomba
@JuuuKomba 9 күн бұрын
China chake kuseliku nkumati ndikupeleza 7 kwa ten mfiti 😢
@StevenFombe
@StevenFombe 9 күн бұрын
If yuo steal with sorrounded one day all will 😂😂
@Benson-cf6qd
@Benson-cf6qd 9 күн бұрын
Aaah koma ma boys inuyo mumakwana 😅
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w 9 күн бұрын
Komadi ma junior police akuvutika ,srs
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂 apa mwatha manthatu
@amosmuluwane4182
@amosmuluwane4182 7 күн бұрын
Lelotu anyamata mwawalankhulila amalawi pitilizani
@user-zq3li3qw1m
@user-zq3li3qw1m 9 күн бұрын
Every day kusokesa uniform ya police zovuta zedi
@user-qe3iu7jy4h
@user-qe3iu7jy4h 9 күн бұрын
Ayi palibe chabwino kulibwino undindo asiyile wena
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zg
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zg 9 күн бұрын
Brilliant idea 💡
@mathewsmakina7845
@mathewsmakina7845 9 күн бұрын
Mukamatero tililimodzi pamenepo
@jamusnamwino-br2iz
@jamusnamwino-br2iz 9 күн бұрын
anyamata musamale muphedwatu mcp sifuna anthu oyankhula chilungamo
@EllenChione
@EllenChione 9 күн бұрын
Ndakutayilani kamtengo guys
@ShagaFologonya
@ShagaFologonya 9 күн бұрын
Mmakwana uzo ndi mzao
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 9 күн бұрын
Iyayi bomali linaziyipisila kale
@RuthMkangala
@RuthMkangala 9 күн бұрын
Koma kumeneko
@madsondzintchira9831
@madsondzintchira9831 6 күн бұрын
Abodza awa sanena zoona komaso oopa kwabasi bwanji analephela kutuuza zoona nthawi ya maliro anyamata wanthu skc timakubukila zbs isakudziwa ndalama pa imfa ya bingu atolankhani amakwela mu tengo kuti anene zoona Koma pano mmmmmmmmmma radio ake cabbage oneka oliba koma mkati madzi okhaokha
@DalitsoulNchengah
@DalitsoulNchengah 8 күн бұрын
Ulemu
@McstanleyChalema
@McstanleyChalema 9 күн бұрын
Mtsogoleri yekhayo adali ndi kuthekera koteroko adali Akamuna a Bingu seconded by Akamuna Dr Saulosi
@RitaKainga
@RitaKainga 9 күн бұрын
Exactly!
@RitaKainga
@RitaKainga 9 күн бұрын
Thanks you 2 guys there,Komano kod mmesa achakwera anatiuza Kut adzamanga aliyense ochita katangale m'boma lawo? Ndy chilowele amenebanamuona mkumanga ndi achilima okha? Plz plz t mkwabwino kusangalatsa Mulungu than munthu mzako
@Yamikaniwalasi
@Yamikaniwalasi 9 күн бұрын
😂😂😂😂
@BlessingsSeleman
@BlessingsSeleman 9 күн бұрын
Zofunika osambisala munda wa mtedza timadabwatu koma apa mwabwera
@user-ce8ud5ed5y
@user-ce8ud5ed5y 9 күн бұрын
Mumakwana gayez
@JimmyGenda
@JimmyGenda 9 күн бұрын
Hello Guys. Please continue hitting the nail on the head.
@ChiccoDzikolo
@ChiccoDzikolo 9 күн бұрын
More fire gentlemen, Malawi wathu ndiyemweyu,Osaopa kuzilangiza nkhutukumve ndi mbala zimenezi
@user-wi8xw9qh7n
@user-wi8xw9qh7n 9 күн бұрын
Chakwera must go before September pls God is looking for us
@RemaniNkhoma
@RemaniNkhoma 9 күн бұрын
bora bingu ndi ng'ono wake pta osati uyuyu chakwerayu ndimbzi
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 9 күн бұрын
Chilungamo chimamasula, azibambo inuyo mulungu azikudalisani ndikutetezani mukugwila tchito, from cape town
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 9 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂 ndemvu zamwayi apolice akumadula zikhadabo atavala nsapato kkkkkkkkkk
@CalvinThomson-ys5zf
@CalvinThomson-ys5zf 9 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 uyu ndiwamwano ati kuwenga zikhadabo autavala nsapato
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 9 күн бұрын
@@CalvinThomson-ys5zf kkkkkkkkk akutero kuli kutha kwa nsapato kkkk
@EnockBwaila
@EnockBwaila 9 күн бұрын
Apapa ndiye mwabwera madolo ulemu wanu that is democracy
@DavieKalonga-y5j
@DavieKalonga-y5j 9 күн бұрын
Pitilizani kumatiyakhulira chilungamo pa hot current
@juliochiwalo
@juliochiwalo 9 күн бұрын
Pamene apolisi akusowa nsapato nawo ma pensioners sakulandira ndalama zawo ena mpaka zaka panopa katangale mbona wa chulukadi
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV❤
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v 9 күн бұрын
Matha
@RuthMkangala
@RuthMkangala 9 күн бұрын
Koma kumeneko
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@GiftNyirenda-q9d
@GiftNyirenda-q9d 7 күн бұрын
Vuto lanu lopanga compare anthu awiri osiya, zolinga zosiya, koma kulephela kusiyanitsa.
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 9 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
Happy 4th of July 😂
00:12
Pink Shirt Girl
Рет қаралды 62 МЛН
Sigma Kid Hair #funny #sigma #comedy
00:33
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 15 МЛН
I Can't Believe We Did This...
00:38
Stokes Twins
Рет қаралды 109 МЛН
마시멜로우로 체감되는 요즘 물가
00:20
진영민yeongmin
Рет қаралды 29 МЛН
THE THORNY PUZZLE: WHO WILL SAVE RUTO??
21:08
Herman Manyora
Рет қаралды 33 М.
KWAGWANJI - KUSANTHULA ZOMWE ZACHITIKA KU UTM 12 July 2024
1:16:26
Hot Current Nduna Yoona Zachitetezo Cha Mdziko Wamukalipira Brian Banda
1:03:23
CRUISE 5 WITH BYSON KAULA PART 2 - 20 JUNE 2021
59:55
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 48 М.
TAMVANI ZA IMFA YA CHILIMA IJA
10:10
FRANCIS MTAWAYA TV
Рет қаралды 190 М.
Happy 4th of July 😂
00:12
Pink Shirt Girl
Рет қаралды 62 МЛН