Limpopo iiiih! ma demo ajatu kwabwela anthu akunja kudzaletsa atapangidwa hayala Ntanyiwa waulura

  Рет қаралды 23,532

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

5 күн бұрын

Пікірлер: 98
@ShaolinThomas-ow8yn
@ShaolinThomas-ow8yn 4 күн бұрын
Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 3 күн бұрын
Akulu akulu mukulankhula koma sitikumva 😢
@user-mw3kj4qz7b
@user-mw3kj4qz7b 4 күн бұрын
We won't fear anything even as Zambian s were coming in Malawi guys to fight that evil man chakwela
@JuuuKomba
@JuuuKomba 3 күн бұрын
Koma iweyo pokhapa pot awagwila ndakuimikila manja mwamba athuo agwidwad
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 4 күн бұрын
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 3 күн бұрын
Koma chakwera wandikwana one day ndi kupedza people they call gringo
@mellipherjohn7158
@mellipherjohn7158 2 күн бұрын
umakwana mtanyiwa tikuziwa zambili amalawi ambuye azikupasani moyo wautali 🎉🎉🎉🎉
@mthawisakaunda
@mthawisakaunda 3 күн бұрын
Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa
@WatsonNtchito
@WatsonNtchito 2 күн бұрын
Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa
@Hassankazembe-d3o
@Hassankazembe-d3o 3 күн бұрын
May God bless you comrade Ntanyiwa
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 3 күн бұрын
Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi
@UsenLashid
@UsenLashid 3 күн бұрын
Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 3 күн бұрын
Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 3 күн бұрын
Umwa chani
@user-ht7vs3dp2u
@user-ht7vs3dp2u 4 күн бұрын
Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee
@CadTafa2
@CadTafa2 4 күн бұрын
Apolici a malawi a kuzishipisa
@JaneLikome
@JaneLikome 3 күн бұрын
Nice mr ntanyiwa
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 4 күн бұрын
Pano malawi ndi North Korea 😭😭😭
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 3 күн бұрын
Apapa ndatanganidwa kuwerenga nkunvesera😂😂
@AjibuTwalibu
@AjibuTwalibu 3 күн бұрын
Umakwana ya mtanyiwa tili nawenawe my brother
@CathrineRamseyJafaal
@CathrineRamseyJafaal 3 күн бұрын
Anthu nonse amene mukudana ndi nthanyiwa mitungati zoswera malambe inu zikukusangalasani mmene akuyendesela dzikoli gule wanuyi achoke alibe phindu
@DuntumaziyaDuntumaziya
@DuntumaziyaDuntumaziya 3 күн бұрын
following you sir
@blacksonpeshes5057
@blacksonpeshes5057 3 күн бұрын
kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja
@BitonFred
@BitonFred Күн бұрын
Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 3 күн бұрын
Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka
@PartsonMdeza
@PartsonMdeza 2 күн бұрын
nkhanga zaonaaa
@MikeMerecah
@MikeMerecah 3 күн бұрын
Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,
@NisharChibisa
@NisharChibisa 4 күн бұрын
Mumakwana
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 3 күн бұрын
Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe
@misoMoyo
@misoMoyo 3 күн бұрын
Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 3 күн бұрын
Comredy mtanyiwa tikufuna number yanu tizipephela Nanu mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 3 күн бұрын
Ndipo chakwera tidzachita kuotcha pamoto chifukwa chankhanza akuchitazi
@AugustineIshmael
@AugustineIshmael 2 күн бұрын
Zachamba basi dikilani 2025 vote yanu ndiye nuclear power osati zabibi zanuzi
@BrunoChakukuma
@BrunoChakukuma 2 күн бұрын
Ntanyiwa woyeeeee
@JamesIsaac-zi4kb
@JamesIsaac-zi4kb 3 күн бұрын
Chakwela ofuna adibwe kanyenya basi
@Bonisiwentamo
@Bonisiwentamo 4 күн бұрын
❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke
@user-vu4cz1mt4f
@user-vu4cz1mt4f 3 күн бұрын
Tisayembekezere kuti tingamve munthu wakuphayo kuti ndine ndapha mayz ? Munona kt wakupha kufufuza chifkwa chomwe wina wafera koma atapha ndiyeyo ? Mayankho ndiomwewa omwe tikumayankhulawa coz action ikuchitatu kuoneka yokha ndipo mwachindunji monga kumangidwa anthu then kulowesa zigawenga nde ngt akusakidwa anthuwa kuti aphedwe nde nkumat ena omwe adafa aja anafera zina ?
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 3 күн бұрын
Ukanakhala kut mwina ukutiwuza munthu wozamuvotera koma nawenso ukumpangila peter kampen choti uziwe peter nayenso atatitopesa kale sitikunfunanso
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili 3 күн бұрын
Mcp mukali kuyalukirayalukiratu
@IssahAluba
@IssahAluba 3 күн бұрын
Chonde AMalawi asatiphimbe maso BOMA ilili osalivera tiyeni pansewu week yamawa osaopa gayz 💪💪🛶🛶🏹🏹⚒️⛏️
@UsenLashid
@UsenLashid 3 күн бұрын
Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please
@dorisbutao4227
@dorisbutao4227 3 күн бұрын
Mmmh
@stanleychisasa4343
@stanleychisasa4343 3 күн бұрын
Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which Big man?
@YONA-v5o
@YONA-v5o 4 күн бұрын
Anthu amenewo ngat agwidwa aphedwe ndinthu cifukwa iwowo anabwela kuzapha
@maluli5691
@maluli5691 3 күн бұрын
Asilikali Aku malawi ndi asilikadzi.west Africa asilikali sakunyengelela kulanda boma
@MandalaChaona
@MandalaChaona 4 күн бұрын
M C P -- Malawi Congress Party M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️
@mipeacemakermw9501
@mipeacemakermw9501 Күн бұрын
Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣kzfaq.info/get/bejne/jbh0nrRp2MWXZJ8.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p
@jangiya03
@jangiya03 3 күн бұрын
Ambuye tithandizeni Malawi waipa
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 3 күн бұрын
mademo mpanga komweko ku lilongwe ayi mkanya
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 3 күн бұрын
Nde inu mukuganiza kut olo patabwera peteryo zinthu zingasinthe foundation ya Malawi kuvuta konseko ndi chipani Cha udf olo mutatani Malawi sazasintha
@shadreckphiri1799
@shadreckphiri1799 4 күн бұрын
If what comrade is saying is the truth,then Chakwera must be the worst president in Southern Africa.
@GetrudeBanda-sd1yf
@GetrudeBanda-sd1yf 4 күн бұрын
Zoonad amalawi azimai tizingoyang'anira nyasizi bvuto azimai timatengrka ndi kathu kochepa
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 4 күн бұрын
Hahaha AAA, Malawi poison party, Wanthu anawa votera dala, bolani ife tiri kutali zina ukamva zina Leku kamba anga mwala.
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 4 күн бұрын
Limpopo FM ndi 1
@SeephyMfaume
@SeephyMfaume 4 күн бұрын
MCP Pamtumbo pawo ndithu
@HappyMaolid
@HappyMaolid 4 күн бұрын
It's time to figh now,osagona
@BitonFred
@BitonFred Күн бұрын
😂😂😂😂
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 4 күн бұрын
😂😂😂😂😂 zabwino zonse wachita bwino wagwidwa tiakonzere konkuno
@walesbanda4959
@walesbanda4959 2 күн бұрын
😂😂😂
@AnaffSayamika-uh6vg
@AnaffSayamika-uh6vg 4 күн бұрын
Chakwela ndigalu kwabasi
@ThokohPrescotKalonga
@ThokohPrescotKalonga 4 күн бұрын
Malawian kuwopa too much that’s why amakonda kulepheresa mademo so don’t tell us ngati muziwona zoti sizingatheke zochita mademo! Aaa why amakonda kulepheresa mademo
@ConfusedAstronaut-qv6wq
@ConfusedAstronaut-qv6wq 4 күн бұрын
Koma chakwera anthawa wauyouyo mbwiyache.
@CHIWSABINYAMBOSE
@CHIWSABINYAMBOSE 4 күн бұрын
Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 4 күн бұрын
Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe
@PaulineKamwana
@PaulineKamwana 4 күн бұрын
<a href="#" class="seekto" data-time="510">8:30</a> musova mcp ,mulithawa dziko mukulifuna
@ConfusedAstronaut-qv6wq
@ConfusedAstronaut-qv6wq 4 күн бұрын
Asilikira akumalawi ndi wopusa.
@user-xi2vo4gc4u
@user-xi2vo4gc4u 4 күн бұрын
Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 3 күн бұрын
Chakwela ndikanankhala kuti ndimatha ufiti ndinakamchosa ineyo manyi akee anthu
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 3 күн бұрын
Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊
@EllinaBitto
@EllinaBitto 4 күн бұрын
😢😢😢😢😢😢😢😢
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 3 күн бұрын
zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 3 күн бұрын
Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera
@CharlesMateya
@CharlesMateya 3 күн бұрын
Following
@user-td6qe4gr6w
@user-td6qe4gr6w 3 күн бұрын
Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 3 күн бұрын
Ndipo kwambili eni dziko kumangosaukirabe
@FrankMulela-qt1wi
@FrankMulela-qt1wi 4 күн бұрын
Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko 4 күн бұрын
Atanyiwa pathako pako
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko 4 күн бұрын
Yess
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko 4 күн бұрын
Zowonadi mchutsuludi chimenechi
@user-yc3ik9dq3x
@user-yc3ik9dq3x 3 күн бұрын
Inu amenewo mungodziyankha nokha muli phee kugwiritsidwa ntchito ndi agaluwo 🥺mxieuw
@FatimanickisJaffer
@FatimanickisJaffer 4 күн бұрын
Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel 4 күн бұрын
Ndikut mambodza akowa Pali ine no comment ndizopusa zakozo tithana phwanga galimoto uma user ija nditha kukutumizira komaso pachikwangwani umakonda kucheza paj okay
@victorauwana7258
@victorauwana7258 4 күн бұрын
Mwapemphedwa kutu mupange comment?
@NizigiyimanaChantal-c2p
@NizigiyimanaChantal-c2p 4 күн бұрын
😢
@SoundmasterElectrical
@SoundmasterElectrical 4 күн бұрын
Mbudzi iwe uthana ndindani usawone ngat ndife ogona wamva panyo pako
@MaryNyirenda-nq3mh
@MaryNyirenda-nq3mh 4 күн бұрын
Chigawenga iwe chimunthu chopanda phindu chitsilu ulibe manyazi mulungu akukanthan
@LukaThawe
@LukaThawe 4 күн бұрын
Anthu achoka Kuti iwe nawendimbuzi kwambiri ukukofuna kusokoneza amalawi ,chifukwa amalawi ndiopepera kale ndiye azikuvera nyasi zako sata yako
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 4 күн бұрын
Chakwera atha ngati Idi amin sizimuthera bwino ndithu.
@user-tm3zh5zk4t
@user-tm3zh5zk4t 4 күн бұрын
Paja ninakuwuza kale kuti upite kumalawi mabodza akowo mtanyiwa yiweyo niamene ukumasokoneza anthu infe timapeleka ulemu kwa boni kalindo osati mbuziyiweyo ayi
@AchinaKellz
@AchinaKellz 3 күн бұрын
Achakwera vomelezani😂
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko 4 күн бұрын
Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko 4 күн бұрын
Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi
@FrancisDay-br7xb
@FrancisDay-br7xb 4 күн бұрын
Pain MCP
@user-yc3ik9dq3x
@user-yc3ik9dq3x 3 күн бұрын
Dzidyani za magazizo. Mulungu akulangani nkhuku inu
@AminahMussah
@AminahMussah 3 күн бұрын
ukatelo watumidwa nda nzako akuphawo
@CHIWSABINYAMBOSE
@CHIWSABINYAMBOSE 4 күн бұрын
Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 12 М.
Получилось у Вики?😂 #хабибка
00:14
ХАБИБ
Рет қаралды 7 МЛН
Always be more smart #shorts
00:32
Jin and Hattie
Рет қаралды 47 МЛН
Smart Sigma Kid #funny #sigma #comedy
00:25
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 16 МЛН
BON KALINDO KU MANGOCHI WAYAKA MOTO |
2:26
DZIWE TV
Рет қаралды 6 М.
Times Exclusive featuring Bishop Gilford Matonga - 29 June 2024
1:07:17
Times 360 Malawi
Рет қаралды 12 М.
KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌
17:19
'If we continue like this, we can kiss power goodbye' -Fikile Mbalula
59:55
Imvani komwe kuli Mzimu wa Chilima akufotokoza Sam Lwara
17:40
Malawi Trends TV
Рет қаралды 23 М.
Nkhani ya ku Bisesero ikumukhudza bwanji Zikhale Ng'oma
11:25
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 41 М.
ulaliki kwa mfumu chalenga
11:08
Zion City Malawi Church Channel 1
Рет қаралды 53 М.
ABDULL..CHIPANI CHOLAMURA UK CHAULUTSA ZISANKHO
12:53
Club Junta
Рет қаралды 5 М.