Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa
@WatsonNtchito2 күн бұрын
Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa
@Hassankazembe-d3o3 күн бұрын
May God bless you comrade Ntanyiwa
@user-oc9vl9xz8e3 күн бұрын
Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi
@UsenLashid3 күн бұрын
Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela
@FrynessMoyo-to2du3 күн бұрын
Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂
@priscillamangata40233 күн бұрын
Umwa chani
@user-ht7vs3dp2u4 күн бұрын
Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee
kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja
@BitonFredКүн бұрын
Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika
@HalisonSolomon3 күн бұрын
Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka
@PartsonMdeza2 күн бұрын
nkhanga zaonaaa
@MikeMerecah3 күн бұрын
Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,
@NisharChibisa4 күн бұрын
Mumakwana
@EllenPhiri-xt8pt3 күн бұрын
Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe
@misoMoyo3 күн бұрын
Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa
Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please
@dorisbutao42273 күн бұрын
Mmmh
@stanleychisasa43433 күн бұрын
Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which Big man?
Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊
@EllinaBitto4 күн бұрын
😢😢😢😢😢😢😢😢
@chadreckchibwithala14933 күн бұрын
zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa
@HalisonSolomon3 күн бұрын
Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera
@CharlesMateya3 күн бұрын
Following
@user-td6qe4gr6w3 күн бұрын
Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa