Ndizinthu zokhumudwitsa kumene chifukwa tsiku la 10 july silinatchulidwe dzulo ai, tatopa nazo ife zimene likupanga boma limeneli.
@JohnAsendi3 күн бұрын
Akambanje ndigulu lanu pazakuti zanu musankha nokha pazomwe muzitukwane papa njoka sitimayang'ana zakuti Pali madzira ankhuku kapena Pali m'phika ine ndikukulupirira Pali chaka chomwe Ana sukulu sanalembe mayeso ndiye anamwalira nyamako mapana chibaanzi 🤣🤣🤣🤣🤣 timadabwa man demo amwezi wamawa kulenge PA 1 amwezi inu iyayi mwatisandusa muno opezera chakundya chanu😭😭😭😭😭😭😭
@PrinceBlessings-bv5bs4 күн бұрын
Eee eee ai zovutat
@JustinChiwale3 күн бұрын
Ndizoona cz kulibe ma demo amtendere ana alembe kaye mayeso plz
@user-gj4li2gc8o3 күн бұрын
Anthu akumwera inu koma muli ndi kwiyo koma boma lokha sitisintha munya inu mpaka 2030 woooooo
@user-jl6sq3ph1b3 күн бұрын
Iwe tachoka apa 2030 ndanio machende akowo ndi 2030 yakoyo ukuwona ngat ndi gule kod iweo ndi chakwela wakoyo kupanda kuvota mumwera kuno ku mpoto inuo chigawo chapakati simungawinebe mwamva muzikhala mukuziwa zimenezo ku mwela kuno ndi kumene kuli anthu ochuluka kwambir ndikumapita ku mpoto pakatipo Mesa mwangochuluka ma farm basi ndie mukuona kuti inuyo mungamuwinise chakwelayo inu agalu eti muuzaneso zimenezo ndi kuousa kwanuko
@AlexManuelMisomali-sv1vn3 күн бұрын
Mademo asachitike chifukwa nthawi yatha ndipo zingabweretse mavuto ena kwa boma lomwe likubweralo