Koma vuto amati abwino sankhalitsa zikumandinkhudza kwambili zomwe zikuchitika mu Malawi muno
@YOMUJAY9 күн бұрын
Dc we stand with you akuphawa tigwetse basi
@Location.Skyrim9 күн бұрын
Your a true son of the soil Bon Kalindo osaopa osatopa keep the fire burning chilungamo chiyende ngati madzi
@LindaSonipa9 күн бұрын
We love you the DC ng'alulani tikufuna kudziwa amene adakhudza thupi la VP wathu Chilima ,,, his soul continue rest in peace
@charlesbanda19659 күн бұрын
Mulungu apitilize kukutetezelan DC moyo wauta❤
@hamiltonmalata64908 күн бұрын
DC thanks for representing us
@frankkamwendo49508 күн бұрын
I like the ending..."iweyoo?" 😂😂😂
@letuschikalamba68868 күн бұрын
Tili nanu a Bon may God protect you
@Robertmkango9 күн бұрын
Bon kakalindo wa limpopo akumawanchura anthu live km inu simukuwa nchura amkhazuleren aziwikire ndikuba kwawo ndikumpha kwawo timakudalilan nose awili ❤
@temwarachaelkhonje37338 күн бұрын
Longlive Boooooooon Kaliiiiiiindooooooooo....brave man
@Odeta-j2c8 күн бұрын
Mumatilimbitsa mtima kobasi the dc🎉🎉🎉🎉
@PeterThomas-lw3io9 күн бұрын
Your talking true bro Mdima umadana kuwunika Awululeni aziwe okha
@DavidJackson-ox4xm9 күн бұрын
We love you The DC'S mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi chilungamo chiyende ngat madzi.
@stevovosalimu54439 күн бұрын
The DC of the world number one ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@preciousmkwangwanya9 күн бұрын
We really need to light the candles daily but my question is where we we get the money to buy the candles and lighters on daily basis? Do we really have the power to make the spirit of the dead rest by showing our love, allegiance and good works of the deceased?
@KingashinaRambo8 күн бұрын
The DC umàkwana iweyo mr president wa anthu osauka 😂😂😂 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 Osaopa osatopa
@JoseKagona-lb4ef8 күн бұрын
Thanks born karindo
@GiftHarawa9 күн бұрын
Listening from Capetown
@PreciousKARINGANIZA8 күн бұрын
Dc ndimakunyadirani❤❤❤
@HassanIzaya9 күн бұрын
Love dc kalindo ❤❤❤
@JohnBanda-ux9fy9 күн бұрын
Uremu wanu the DC ❤❤
@MercyMhango-lt4dm9 күн бұрын
.
@YankhoBanda-h7p8 күн бұрын
Big up Mr dc no fear no body😅😅
@joneswillymakaniko-dg8ub8 күн бұрын
Chilungamo sichiphedwa Bwana stand on your feet
@user-ci5ik8kx6s9 күн бұрын
We stand with you
@DN-mp8pp9 күн бұрын
DC we support you!!! We pray for you and God cover you with his blood
@user-ov8by9uw9g8 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngati madzi ❤❤❤❤❤❤
@ngozo079 күн бұрын
We stand with u our freedom Fighter ❤
@lytonmaseko45348 күн бұрын
❤ we love you man of vision
@CharityPhiri-rl7sz9 күн бұрын
Tili pambuyo panu DC
@user-qo6ru2nb9r8 күн бұрын
Following the DC
@godwinkhunga9 күн бұрын
Keep up mr we are proud of you
@RobertoTonde9 күн бұрын
Obvious Mr president let's fighting together
@Yungjoe7869 күн бұрын
The DC our own independent journalist
@LastonTiligu9 күн бұрын
We love you Bon k the DC more fire!!!
@RichNgwira9 күн бұрын
Mmmmm koma inuyo ambuye akudalitsen kwambiri mwaimiladi ife osauka zikomo
@ChikumbutsoTsalangu9 күн бұрын
Respect to you the Dc
@Robertmkango9 күн бұрын
Tilinawerimozi chilungamo tidalila kwayinu kms Ana ntema chilima timuziwe
@TechnicalSupport-lk9im9 күн бұрын
The DC plz we love pitilizani kutiyimilira monga president wanthu wa amphawi more fire the Dc
@JohnJohn-og8rt9 күн бұрын
Ulibwino big man bon kalindo
@DuntumaziyaDuntumaziya9 күн бұрын
keep it up my DC❤❤❤❤❤❤
@YasinMmadi9 күн бұрын
We the whole malawi support you the DC
@vitumbikokamanga58699 күн бұрын
I support you bon kalindo ❤❤❤❤❤
@MosesTangwe9 күн бұрын
Proud of you the DC ✨☀️
@RodneyBossom9 күн бұрын
The DC keep the fire burning...
@PatrickMailos9 күн бұрын
Timakukondani kwambiri the DC
@yassinn56349 күн бұрын
Lerotu Kalindotu akuyankhula zanzeru
@RichardMussa-qe6zi9 күн бұрын
We are going together with u
@McneverMauwa9 күн бұрын
Ulemu wanu bwana DC God bless you
@MusaAjusu9 күн бұрын
Palibenso, Bon kalindo ulemu wanu, Respect
@FrancisMbewe-xn2pl9 күн бұрын
DC the number one 💪🧢🔥
@user-di8hq3dl9o9 күн бұрын
Go ahead
@user-vh9uk1jy7w9 күн бұрын
More fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌
@AungunKadzinja-wv2uc9 күн бұрын
More fire Mr president
@ishkidalie59589 күн бұрын
Mpaka akumajambula Film
@KelvinMandawala9 күн бұрын
Timamvela zoona kuchoka Kwa inu bwana kalindo mmakwana long leav❤
@user-xq2mv7jl5m9 күн бұрын
Munthu wa personality yokwanira.
@ChimzimusPatrick9 күн бұрын
Dc we love you❤❤❤❤❤
@Edson-sj8vn9 күн бұрын
Long live Mr DC
@TimothyNkhutembaChirwa8 күн бұрын
Abwana chonde mupite ku immigration anthu akuvutika kwambiri
@ThandoKunene-j9u9 күн бұрын
Mumatiimilira mr DC pitilidzani kung'alura !.
@user-dt4po2kk7o9 күн бұрын
Madness kalindo school niyaying’ono kwambili I think anapangapo misala
@JimmyMzozoma9 күн бұрын
Mumakwana Mr DC
@MaryMary-dz2th6 күн бұрын
The DC akuti aja anaphedwa kuchikangawa😂😂
@ChiccoMazengera-hx1eu9 күн бұрын
Mbambande DC👏👏👏
@user-ci5ik8kx6s9 күн бұрын
We stand with you even though we are forced to be quiet
@RajMass-nr3uy9 күн бұрын
Iweo mulungu azikudalisa ndi moyo wawutali❤
@user-et5nz4vz2v9 күн бұрын
The DC mwana oopsa kwambiri 🔥🔥🔥🔥
@user-fi7ko7bl6f9 күн бұрын
We love you the DC
@REXCHARLESKAJAWO9 күн бұрын
The DC mwana owooopsa kwambili 🔥🔥🔥🔥🇲🇼
@JimmyMzozoma9 күн бұрын
MULUNGU AZIKUTETEZARANI MR DC
@user-ge6bm7yr4p8 күн бұрын
Km iwe umayimirira malawi😎
@ZainabFaki8 күн бұрын
Dc mumatilmilira
@user-ky8eq5ek1p9 күн бұрын
Zoonadi Big ulemuwanu
@DavidJames-uv1jr9 күн бұрын
Our own spoke person
@kondwanikamanga-ti2yi8 күн бұрын
BON KALINDO NDIWE MBULI CHISILU
@AmusedDimSum-hd5yp9 күн бұрын
❤❤❤❤ God bless you big
@EdwinMabviko9 күн бұрын
Koma K30,000,000 mukuyidziwa kapena misala!
@user-fi7ko7bl6f9 күн бұрын
Ulemu wanu Dr DC president waife osauka l salute you 😅😅
@YasinMusa-ym8lp9 күн бұрын
❤❤❤mtili nanu bwana 💪💪
@raphaelfanuel46089 күн бұрын
The DC mmatidziwitsa zomwe sitikanazidziwa real man
@richardchimatiro56078 күн бұрын
ena mwina tungotsatila, Kalindo is not accusing anyone while okumva tikumva ngati he is accusing someone
@SifatiMoses9 күн бұрын
Malawi akufunika anthu ngati awa.
@user-nr5ns2ke4o9 күн бұрын
aaaaaaaaaaaa ndimamusata kale koma ndikuona ngat misala iyi chomwe akukamba sakuchidziwa mbuz
@CharlesKachipanda-jz9jv9 күн бұрын
Big up Mr Dddddcccccc
@harrisbanda58919 күн бұрын
Ndemwati msing'angayo wapasidwa ma drip kunyumba ya m'busayo 😂😂😂😂
Kalindo Anthu amamutenga ngat ndiwosokonedza Km ineyo ndikut ayi ndikalindo yemweyu amayidzudzura dpp koma ali momwemo komano ifeyo ndi amene sitimupasa support yokwanira
@MaggieCement8 күн бұрын
Sure anthu mumasatopa ntambo ndi chakwera poononga katundu wa Amalawi lero yakwiya ndi mizimu