Uyu nde Bon Kalindo kukhadzula lero pa 30 June 2024 timve zimenezi basi

  Рет қаралды 58,865

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

11 күн бұрын

Пікірлер: 278
@yamikanimagwetsa4319
@yamikanimagwetsa4319 9 күн бұрын
But then this guy bon kalindo is a true hero of Malawi.. Long live sir
@blessingmnomanda
@blessingmnomanda 9 күн бұрын
Dc we love you
@AnockyDavidd
@AnockyDavidd 9 күн бұрын
We love you DC
@HarrisNyirenda
@HarrisNyirenda 9 күн бұрын
Good point Bon kalido​@@AnockyDavidd
@thomasnyirenda1938
@thomasnyirenda1938 8 күн бұрын
I love you sir this true leader who shows the way and follow the way 💪💪💪💪
@user-hg2cw1om1p
@user-hg2cw1om1p 9 күн бұрын
Never to see person like kalindo ❤❤mulungu akudalise kalindo.. Bwedzi ena anasiya Kale Kale koma kalindo amatiyimira❤️❤️
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 9 күн бұрын
Tavaso kuti chakwera anaphaso m'busa nzake wa assembulesi ndi fiti yachikhalire😢😢kudziko
@hamiltonmalata6490
@hamiltonmalata6490 8 күн бұрын
Muthuyi ndi fiti
@user-rl5zq1qr4d
@user-rl5zq1qr4d 9 күн бұрын
Kalindo ndi munthu osawopa ndipo akati sindimaopa tigwirizane naye (1) Ali mziko mommuno (2) amanena mpanda mantha (3) samabisala akamasakidwa (4) amatha kusiya udindo umene wapasidwa (5) samahongedwa (6) amawayalusa anthu amene sayenera kuyalusidwa (7) alibe mzache amamunena aliyense amene walakwisa (8) umoyo wake nthawi zonse umakhala pa chiwopyezo
@MayimunaZuber
@MayimunaZuber 9 күн бұрын
Ndipo zoonadi😊
@MayimunaZuber
@MayimunaZuber 9 күн бұрын
Ndipo zoonadi😊
@user-vy2lm8jk2x
@user-vy2lm8jk2x 9 күн бұрын
Ndipo live l love like this guy😊
@ElishaMapepa
@ElishaMapepa 9 күн бұрын
Koma vuto amati abwino sankhalitsa zikumandinkhudza kwambili zomwe zikuchitika mu Malawi muno
@YOMUJAY
@YOMUJAY 9 күн бұрын
Dc we stand with you akuphawa tigwetse basi
@Location.Skyrim
@Location.Skyrim 9 күн бұрын
Your a true son of the soil Bon Kalindo osaopa osatopa keep the fire burning chilungamo chiyende ngati madzi
@LindaSonipa
@LindaSonipa 9 күн бұрын
We love you the DC ng'alulani tikufuna kudziwa amene adakhudza thupi la VP wathu Chilima ,,, his soul continue rest in peace
@charlesbanda1965
@charlesbanda1965 9 күн бұрын
Mulungu apitilize kukutetezelan DC moyo wauta❤
@hamiltonmalata6490
@hamiltonmalata6490 8 күн бұрын
DC thanks for representing us
@frankkamwendo4950
@frankkamwendo4950 8 күн бұрын
I like the ending..."iweyoo?" 😂😂😂
@letuschikalamba6886
@letuschikalamba6886 8 күн бұрын
Tili nanu a Bon may God protect you
@Robertmkango
@Robertmkango 9 күн бұрын
Bon kakalindo wa limpopo akumawanchura anthu live km inu simukuwa nchura amkhazuleren aziwikire ndikuba kwawo ndikumpha kwawo timakudalilan nose awili ❤
@temwarachaelkhonje3733
@temwarachaelkhonje3733 8 күн бұрын
Longlive Boooooooon Kaliiiiiiindooooooooo....brave man
@Odeta-j2c
@Odeta-j2c 8 күн бұрын
Mumatilimbitsa mtima kobasi the dc🎉🎉🎉🎉
@PeterThomas-lw3io
@PeterThomas-lw3io 9 күн бұрын
Your talking true bro Mdima umadana kuwunika Awululeni aziwe okha
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 9 күн бұрын
We love you The DC'S mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi chilungamo chiyende ngat madzi.
@stevovosalimu5443
@stevovosalimu5443 9 күн бұрын
The DC of the world number one ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@preciousmkwangwanya
@preciousmkwangwanya 9 күн бұрын
We really need to light the candles daily but my question is where we we get the money to buy the candles and lighters on daily basis? Do we really have the power to make the spirit of the dead rest by showing our love, allegiance and good works of the deceased?
@KingashinaRambo
@KingashinaRambo 8 күн бұрын
The DC umàkwana iweyo mr president wa anthu osauka 😂😂😂 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 Osaopa osatopa
@JoseKagona-lb4ef
@JoseKagona-lb4ef 8 күн бұрын
Thanks born karindo
@GiftHarawa
@GiftHarawa 9 күн бұрын
Listening from Capetown
@PreciousKARINGANIZA
@PreciousKARINGANIZA 8 күн бұрын
Dc ndimakunyadirani❤❤❤
@HassanIzaya
@HassanIzaya 9 күн бұрын
Love dc kalindo ❤❤❤
@JohnBanda-ux9fy
@JohnBanda-ux9fy 9 күн бұрын
Uremu wanu the DC ❤❤
@MercyMhango-lt4dm
@MercyMhango-lt4dm 9 күн бұрын
.
@YankhoBanda-h7p
@YankhoBanda-h7p 8 күн бұрын
Big up Mr dc no fear no body😅😅
@joneswillymakaniko-dg8ub
@joneswillymakaniko-dg8ub 8 күн бұрын
Chilungamo sichiphedwa Bwana stand on your feet
@user-ci5ik8kx6s
@user-ci5ik8kx6s 9 күн бұрын
We stand with you
@DN-mp8pp
@DN-mp8pp 9 күн бұрын
DC we support you!!! We pray for you and God cover you with his blood
@user-ov8by9uw9g
@user-ov8by9uw9g 8 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngati madzi ❤❤❤❤❤❤
@ngozo07
@ngozo07 9 күн бұрын
We stand with u our freedom Fighter ❤
@lytonmaseko4534
@lytonmaseko4534 8 күн бұрын
❤ we love you man of vision
@CharityPhiri-rl7sz
@CharityPhiri-rl7sz 9 күн бұрын
Tili pambuyo panu DC
@user-qo6ru2nb9r
@user-qo6ru2nb9r 8 күн бұрын
Following the DC
@godwinkhunga
@godwinkhunga 9 күн бұрын
Keep up mr we are proud of you
@RobertoTonde
@RobertoTonde 9 күн бұрын
Obvious Mr president let's fighting together
@Yungjoe786
@Yungjoe786 9 күн бұрын
The DC our own independent journalist
@LastonTiligu
@LastonTiligu 9 күн бұрын
We love you Bon k the DC more fire!!!
@RichNgwira
@RichNgwira 9 күн бұрын
Mmmmm koma inuyo ambuye akudalitsen kwambiri mwaimiladi ife osauka zikomo
@ChikumbutsoTsalangu
@ChikumbutsoTsalangu 9 күн бұрын
Respect to you the Dc
@Robertmkango
@Robertmkango 9 күн бұрын
Tilinawerimozi chilungamo tidalila kwayinu kms Ana ntema chilima timuziwe
@TechnicalSupport-lk9im
@TechnicalSupport-lk9im 9 күн бұрын
The DC plz we love pitilizani kutiyimilira monga president wanthu wa amphawi more fire the Dc
@JohnJohn-og8rt
@JohnJohn-og8rt 9 күн бұрын
Ulibwino big man bon kalindo
@DuntumaziyaDuntumaziya
@DuntumaziyaDuntumaziya 9 күн бұрын
keep it up my DC❤❤❤❤❤❤
@YasinMmadi
@YasinMmadi 9 күн бұрын
We the whole malawi support you the DC
@vitumbikokamanga5869
@vitumbikokamanga5869 9 күн бұрын
I support you bon kalindo ❤❤❤❤❤
@MosesTangwe
@MosesTangwe 9 күн бұрын
Proud of you the DC ✨☀️
@RodneyBossom
@RodneyBossom 9 күн бұрын
The DC keep the fire burning...
@PatrickMailos
@PatrickMailos 9 күн бұрын
Timakukondani kwambiri the DC
@yassinn5634
@yassinn5634 9 күн бұрын
Lerotu Kalindotu akuyankhula zanzeru
@RichardMussa-qe6zi
@RichardMussa-qe6zi 9 күн бұрын
We are going together with u
@McneverMauwa
@McneverMauwa 9 күн бұрын
Ulemu wanu bwana DC God bless you
@MusaAjusu
@MusaAjusu 9 күн бұрын
Palibenso, Bon kalindo ulemu wanu, Respect
@FrancisMbewe-xn2pl
@FrancisMbewe-xn2pl 9 күн бұрын
DC the number one 💪🧢🔥
@user-di8hq3dl9o
@user-di8hq3dl9o 9 күн бұрын
Go ahead
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w 9 күн бұрын
More fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌
@AungunKadzinja-wv2uc
@AungunKadzinja-wv2uc 9 күн бұрын
More fire Mr president
@ishkidalie5958
@ishkidalie5958 9 күн бұрын
Mpaka akumajambula Film
@KelvinMandawala
@KelvinMandawala 9 күн бұрын
Timamvela zoona kuchoka Kwa inu bwana kalindo mmakwana long leav❤
@user-xq2mv7jl5m
@user-xq2mv7jl5m 9 күн бұрын
Munthu wa personality yokwanira.
@ChimzimusPatrick
@ChimzimusPatrick 9 күн бұрын
Dc we love you❤❤❤❤❤
@Edson-sj8vn
@Edson-sj8vn 9 күн бұрын
Long live Mr DC
@TimothyNkhutembaChirwa
@TimothyNkhutembaChirwa 8 күн бұрын
Abwana chonde mupite ku immigration anthu akuvutika kwambiri
@ThandoKunene-j9u
@ThandoKunene-j9u 9 күн бұрын
Mumatiimilira mr DC pitilidzani kung'alura !.
@user-dt4po2kk7o
@user-dt4po2kk7o 9 күн бұрын
Madness kalindo school niyaying’ono kwambili I think anapangapo misala
@JimmyMzozoma
@JimmyMzozoma 9 күн бұрын
Mumakwana Mr DC
@MaryMary-dz2th
@MaryMary-dz2th 6 күн бұрын
The DC akuti aja anaphedwa kuchikangawa😂😂
@ChiccoMazengera-hx1eu
@ChiccoMazengera-hx1eu 9 күн бұрын
Mbambande DC👏👏👏
@user-ci5ik8kx6s
@user-ci5ik8kx6s 9 күн бұрын
We stand with you even though we are forced to be quiet
@RajMass-nr3uy
@RajMass-nr3uy 9 күн бұрын
Iweo mulungu azikudalisa ndi moyo wawutali❤
@user-et5nz4vz2v
@user-et5nz4vz2v 9 күн бұрын
The DC mwana oopsa kwambiri 🔥🔥🔥🔥
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 9 күн бұрын
We love you the DC
@REXCHARLESKAJAWO
@REXCHARLESKAJAWO 9 күн бұрын
The DC mwana owooopsa kwambili 🔥🔥🔥🔥🇲🇼
@JimmyMzozoma
@JimmyMzozoma 9 күн бұрын
MULUNGU AZIKUTETEZARANI MR DC
@user-ge6bm7yr4p
@user-ge6bm7yr4p 8 күн бұрын
Km iwe umayimirira malawi😎
@ZainabFaki
@ZainabFaki 8 күн бұрын
Dc mumatilmilira
@user-ky8eq5ek1p
@user-ky8eq5ek1p 9 күн бұрын
Zoonadi Big ulemuwanu
@DavidJames-uv1jr
@DavidJames-uv1jr 9 күн бұрын
Our own spoke person
@kondwanikamanga-ti2yi
@kondwanikamanga-ti2yi 8 күн бұрын
BON KALINDO NDIWE MBULI CHISILU
@AmusedDimSum-hd5yp
@AmusedDimSum-hd5yp 9 күн бұрын
❤❤❤❤ God bless you big
@EdwinMabviko
@EdwinMabviko 9 күн бұрын
Koma K30,000,000 mukuyidziwa kapena misala!
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 9 күн бұрын
Ulemu wanu Dr DC president waife osauka l salute you 😅😅
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 9 күн бұрын
❤❤❤mtili nanu bwana 💪💪
@raphaelfanuel4608
@raphaelfanuel4608 9 күн бұрын
The DC mmatidziwitsa zomwe sitikanazidziwa real man
@richardchimatiro5607
@richardchimatiro5607 8 күн бұрын
ena mwina tungotsatila, Kalindo is not accusing anyone while okumva tikumva ngati he is accusing someone
@SifatiMoses
@SifatiMoses 9 күн бұрын
Malawi akufunika anthu ngati awa.
@user-nr5ns2ke4o
@user-nr5ns2ke4o 9 күн бұрын
aaaaaaaaaaaa ndimamusata kale koma ndikuona ngat misala iyi chomwe akukamba sakuchidziwa mbuz
@CharlesKachipanda-jz9jv
@CharlesKachipanda-jz9jv 9 күн бұрын
Big up Mr Dddddcccccc
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 9 күн бұрын
Ndemwati msing'angayo wapasidwa ma drip kunyumba ya m'busayo 😂😂😂😂
@Chrissyluwe
@Chrissyluwe 9 күн бұрын
Love you DC🎉
@CelsogeraldoGeraldoe
@CelsogeraldoGeraldoe 9 күн бұрын
Zoona Inu mumanena zoona
@DanNzima
@DanNzima 9 күн бұрын
The DC. !!!🔥🔥🔥🔥
@user-yk5xv4dt7v
@user-yk5xv4dt7v 8 күн бұрын
Anaphadi mbusa nzake ndizona ndipo chakwera ndiwasani
@user-vy2lm8jk2x
@user-vy2lm8jk2x 9 күн бұрын
Ndipo uyuyu ndi mwala mwala💪
@lydiakaisi16
@lydiakaisi16 9 күн бұрын
Ndipo straight 😊
@user-gv2uu3cs3g
@user-gv2uu3cs3g 9 күн бұрын
😂😂😂 Koma a president more fire
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 9 күн бұрын
Powerful kalindo ❤❤❤
@stevenrajab538
@stevenrajab538 9 күн бұрын
Kalindo Anthu amamutenga ngat ndiwosokonedza Km ineyo ndikut ayi ndikalindo yemweyu amayidzudzura dpp koma ali momwemo komano ifeyo ndi amene sitimupasa support yokwanira
@MaggieCement
@MaggieCement 8 күн бұрын
Sure anthu mumasatopa ntambo ndi chakwera poononga katundu wa Amalawi lero yakwiya ndi mizimu
@drbanda6105
@drbanda6105 9 күн бұрын
DC. ❤❤❤
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 90 М.
Akufuna kupha mafumu a ku Ntcheu; Umboni wa mfuti 400 tili nawo
8:45
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 26 М.
OMG🤪 #tiktok #shorts #potapova_blog
00:50
Potapova_blog
Рет қаралды 18 МЛН
Жайдарман | Туған күн 2024 | Алматы
2:22:55
Jaidarman OFFICIAL / JCI
Рет қаралды 1,7 МЛН
KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌
17:19
| UKUMBI | Mikakati ya Rais Ruto baada ya maandamano ya Gen Z [Part 3]
30:44
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Sam Malvitha
Рет қаралды 155 М.
LUCIUS BANDA EXCLUSIVEINTERVIEW - 20 MAY 2021
56:54
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 127 М.
Nancy vs Che Nkope - Zikhale Ngoma Kapena Drums?
10:46
CHE NKOPE
Рет қаралды 26 М.
Ine Sindingasiye U Akitivizimu - Bon Kalindo
11:12
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 15 М.
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 235 М.