KAMLEPO KALUWA BOMA ZOMWE MUKUFUNA KUPANGA NDIKUDZIWA

  Рет қаралды 10,397

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

23 күн бұрын

Пікірлер: 49
@MosesTangwe
@MosesTangwe 22 күн бұрын
Uku mkuchikweza amputa olakwika, voice imeneyo ikumveka mwa simple koma ili fire😊
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i 22 күн бұрын
Even neba ku Zambia they know that we don't have president in Malawi
@TwalikiWisiki
@TwalikiWisiki 21 күн бұрын
Mr Kaluwa i appreciate you,,,you a true gentleman a hero,, if it takes you to go back to your past to resolve this chakwera issue so it be,,
@wittinessnkhokwe
@wittinessnkhokwe 22 күн бұрын
Inu a mcp nenani kuti tonse amalawi tichokemo tifune kolowela muone kuti mudzilanulira ndani?
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 22 күн бұрын
You have to take this Government to court for this damage.
@luuu22mwanjabala79
@luuu22mwanjabala79 22 күн бұрын
Wise man from the North side
@FionaKhoma
@FionaKhoma 21 күн бұрын
Bora ilili tikachotsa chakwera a police ambili akuyenera kuchotsedwa tchito
@HenryLaidon-pl9ly
@HenryLaidon-pl9ly 22 күн бұрын
Guys Kamlepo ndi One of True democrat ku Malawi kuno tsopano kodi kuzunza mukumuzuza munthu wobweretsa democracy koma kokoliko ndalama zamisonkho yamphawi zakomadi
@amoschataika7440
@amoschataika7440 22 күн бұрын
Well said, loud and clear
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 22 күн бұрын
Wise man mr kamulepo ❤❤❤❤❤
@brendamakokola7498
@brendamakokola7498 21 күн бұрын
Politics is dirty game
@JamayakoJamayako-rv2he
@JamayakoJamayako-rv2he 22 күн бұрын
Am agreed with you Pipo shud open their eyes Wise man
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b 21 күн бұрын
Amenewo ndie mawu amphamvu mbuzi za police zogwilisidwa ntchito ndi chikangawazo makape amenewo akuti agulidwa ndi mcp gvrt Makamaka mai yolamu nayeso chipawa chosamukhala mutu chija mbuzi ya munthu aziwona makape amenewo mu 2025 wonsewo akathela ku mawulapalibeso kuwakhululukila inshaAllah
@user-zy2nh4lj4h
@user-zy2nh4lj4h 21 күн бұрын
Zinazo muzipanga koma za artist fredokiss mukangoesera 😮 malawi tiyatsa mukangopha fredo achinyamata tifafaniza state house
@chipilirokalison1334
@chipilirokalison1334 21 күн бұрын
Sizitheka mulungu alipo kumwamba osamara
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr 21 күн бұрын
Chomwe wachiona wankulu atakhala pansi, mwana olo atakwera mumtengo sangachione. Welcome Big
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 22 күн бұрын
Ndikatundu ameneyu aboma musamutengele masewelo zomwewakambazo ndizoona ndithu
@JameChome
@JameChome 21 күн бұрын
Ask Bakii Muluzi anamtangwanitsa kooopya 😂😂😂😂😂
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 21 күн бұрын
Yooo zilichonchoso 😢
@Blessings-td4cr
@Blessings-td4cr 22 күн бұрын
Boma iliri azitsogoleri mitu sikuyenda bwino why still keeping cellphones of Born kalindo and kamlepo why why Malawi President and the Police why can you please change your decisions why.
@NescotNyamwela
@NescotNyamwela 22 күн бұрын
Ine president wanga ndi Dad Bingu wa mutharika kwa ine sanafe i can see kuti anapanga chani. Kma mbuz zinaz zimangozuza amalawi osalakwa anyway sindili ku malawi kma home is best mbuziyi izaziwa kazachopa pamwambapo
@FionaKhoma
@FionaKhoma 21 күн бұрын
Mcp ikuyenera kuchoka basi ikuzuza athu osarakwa chakwera wakupha ayende basi
@temwarachaelkhonje3733
@temwarachaelkhonje3733 22 күн бұрын
Aputa olakwika tu....
@raytavares2256
@raytavares2256 21 күн бұрын
Collect your phone via the attorneys and high court on releasing it without prejudice and bias. We are praying for you. Ndine kuno ku Great Britain. Yes the late dad Green Ng'oma used to w for Southern Bottles even when they lived in Mzimba before moving to Zingwangwa Blantyre and after ZINGWANGWA THEY MOVED TO ALIMAUNDE AREA 25 LILONGWE. We must all pray for each other and the countries experiencing the political tarmoils.
@zelliachamboto5744
@zelliachamboto5744 20 күн бұрын
Kulibedi wamuyaya
@MzikaPhiri
@MzikaPhiri 21 күн бұрын
Amen Amen...
@IdahNyasulu
@IdahNyasulu 22 күн бұрын
Deal with them bwana kalua
@GeraldChisokeza-er5cf
@GeraldChisokeza-er5cf 22 күн бұрын
Oh no osat Fredo ayi.Komano kukhetsa Mwazi chifukwa Cha mpamdo Kaya Mulungu amaona amakantha
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b 21 күн бұрын
Apolice yakhani kuti umuyaya uja udakalipobe kapena ai?
@mbewemisoyaanenenji1908
@mbewemisoyaanenenji1908 21 күн бұрын
You fought ngwazi , who are these dogs to fear .
@MaxWell-d7o
@MaxWell-d7o 22 күн бұрын
Pambuyo panu bwana..iponden
@user-kp7le2pu7h
@user-kp7le2pu7h 22 күн бұрын
Wise man❤❤❤
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 21 күн бұрын
Pena pache MCP tu , mukuonjeza eti!!?? Is this what we wanted? Why why why??
@ShorayChimera
@ShorayChimera 21 күн бұрын
I feel ur pain father 💔
@victorauwana7258
@victorauwana7258 22 күн бұрын
Good 👍
@AgnessMzengo
@AgnessMzengo 21 күн бұрын
Iponden fadah,,,,,
@NaduMbewe-zz6iw
@NaduMbewe-zz6iw 22 күн бұрын
Zosaesanda
@babranzima8120
@babranzima8120 22 күн бұрын
Athu akupha abusa wokopha kodi eeeeee athu akumpoto mwasiye mutha ndinu achakwera ndi azanu wood
@EllinaBitto
@EllinaBitto 22 күн бұрын
😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 22 күн бұрын
Mwaonjeza English enafe sitimva nde izizo muzilankhulako chichewa chifukwa nzatonse amalawi kuti timve
@CharlesKachipanda-jz9jv
@CharlesKachipanda-jz9jv 22 күн бұрын
Awuzeni makapewa adziwe kuti inu madala madala
@MagaLassi-tg7lj
@MagaLassi-tg7lj 21 күн бұрын
🆓✊
@user-ss9bj5eh6b
@user-ss9bj5eh6b 22 күн бұрын
chonde bwelerani muzakale bwana tithane nawo anthu oipawa
@Standwell78
@Standwell78 22 күн бұрын
Chana?? Ayesele
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 22 күн бұрын
Akupa mcp
@MilacleSankhani
@MilacleSankhani 21 күн бұрын
Ask late kamazu about u
@HamzaMkwanda-bh8dc
@HamzaMkwanda-bh8dc 22 күн бұрын
Wise man
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 23 М.
Stay on your way 🛤️✨
00:34
A4
Рет қаралды 23 МЛН
Mama vs Son vs Daddy 😭🤣
00:13
DADDYSON SHOW
Рет қаралды 46 МЛН
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 55 М.
Vice President Chilima's visit to the SVTP (Chichewa Interview)
1:47
Shire Valley Transformation Programme
Рет қаралды 44 М.
NKHANGA ZAONA
21:49
TIDZIWE TV
Рет қаралды 65 М.
MAYI WINA WAGONANASO NDI DOCTOR WA PRESIDENT KU STATE HOUSE
17:36
Stay on your way 🛤️✨
00:34
A4
Рет қаралды 23 МЛН