zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu
@abdulhameed78085 күн бұрын
Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.
Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya , Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva
@FarhaazbashaMdoka3 күн бұрын
Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏
@FarhaazbashaMdoka3 күн бұрын
Koma ndalamazi guyz tisamale nazo
@udkconsultancy55675 күн бұрын
POWERFUL
@HalisonSolomon5 күн бұрын
SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI
Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope
@abbasdamsonamini48884 күн бұрын
Naam Ameen thumma Ameen
@user-ky8eq5ek1p5 күн бұрын
Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo
@RobertLuka-wy9cl5 күн бұрын
Ameen
@shadrackdrums35364 күн бұрын
Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.
@user-xd1cm7tm7t4 күн бұрын
Chemoto ndinu mwandila ma unforp
@HallimaMakwinja4 күн бұрын
Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama
@HallimaMakwinja4 күн бұрын
Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu
@harrisbanda58915 күн бұрын
Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir
@JumaMboneka4 күн бұрын
Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas