Shehe uyuso wagagada ulariki wake mopanda mantha kusiya anthu akungoombera mmanja

  Рет қаралды 39,034

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

7 күн бұрын

Пікірлер: 156
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b 5 күн бұрын
Tayesedwa ndi president wakhaza chakwera ndie timupempha Allah kuti atichosele chakwelayo ameen
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo 5 күн бұрын
Sheikhe ulaliki wanu siukugwilizana ndi ma aya omwe mumatulutsa pakamwa panu, uku ndikugulitsa mawu amulungu, ambuye akumvelen chison Ameen
@omardyman8083
@omardyman8083 4 күн бұрын
Analandila ndalama nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto zachamba
@rasulmaulidi2224
@rasulmaulidi2224 2 күн бұрын
zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu
@abdulhameed7808
@abdulhameed7808 5 күн бұрын
Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.
@NenehMasanje
@NenehMasanje 5 күн бұрын
Sheikh mwadya now ndrama
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
7:53 7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizanu Mayeselo aifa muyesa ife sitimaziwaaa, Nde imfazake zochita kumugwira munthu pakhosi mwadaladala , kumuombela mfuti mkamwa munthu ,kodi yinu mulankhulabwanj muli ndiwumunthuyinu ,aaa muzichotsela ulemu nokhatuyinu mwangotengana nonse odya ndalama zamagazibasi , Afitiwo alimwetuuuu ati zikuyenda malawi wake utiyo amene mungamunamize lelo , Azibusa muzichotsera ulemu nokha mwamva
@SulaimanaJames-b9v
@SulaimanaJames-b9v 2 күн бұрын
Maa Shaa Allah May Allah bless this message and make it beneficial
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Wadya nawo ndalama zamagazi iwee, usatinamize asilamufe pamodzi ndi amalawife, ifenso ndife asilamutu, mayesero ukunena apawa simayesero ochokeraxkwa ALLAH, awa ndimayesero ochokera kwa satana kudzela kwa chizukulu tudzi chake chotchedwa chakwela ndi boma less lake 😂😂😂😂😂
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 5 күн бұрын
Odya ndalama zamagazi ngati akumasowa zoyankhula zawo? Allah mukunenayo akuyendereni Sheik😢
@MillieMalakam
@MillieMalakam 5 күн бұрын
Ameen sheikh Allah ahead u. From Cape Town centre
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Chemoto alipomwepo anapha ALLAN WITIKA, anapha chilima kuchikangawa 😂😂😂😂
@SteveriaZimba-qs1id
@SteveriaZimba-qs1id 4 күн бұрын
Amen and amen uthenga wamphavu ambuye alemekezeke ndipo akhululukire zochimwa zathu
@MariamJaffali
@MariamJaffali 4 күн бұрын
Naam sheikh ma shaa Allah ulaliki wabwino ndithu ❤❤❤❤
@BrownMatonyola-xi3lb
@BrownMatonyola-xi3lb 2 күн бұрын
Mwadya zingati Aliyese wanyambita ndalama zoti azizilise za imfa yachilima ndikupepha Yehovah Mulungu wathu amuonetse kiyama akumane ndi mavuto
@FebbieMaulidi
@FebbieMaulidi 5 күн бұрын
God bless you sheik for unity message ❤
@SayidiIshmael
@SayidiIshmael 3 күн бұрын
❤Allah give you more life and imaan to defending this deen
@IshaaakKango
@IshaaakKango 2 күн бұрын
Maashallah sheikh
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 8 сағат бұрын
Aaaa sizomwezija Izi inu asheikh opanda manyazi , Panja peni peni wadya ndalama Za Chikangawa uyu, Sali pachilungamo uyu
@muhmmadsarwer9527
@muhmmadsarwer9527 3 күн бұрын
Ameen thuma ameen Allah tichotseleni President ameneyu..ndipo tipatseni mtsogoleri wabwino mdziko mwathu muno
@abwinoamatani4921
@abwinoamatani4921 5 күн бұрын
Mukufuna mutamike. M'nungu tam'nyekule ngulumbira une
@mosewallace9717
@mosewallace9717 2 күн бұрын
mweye che kuntamba 🔥🔥
@kekeaufi9834
@kekeaufi9834 5 күн бұрын
*WA ALYKUM SSALAAM WARAHAMATULLAHI WABARAKATUHU,,,,Inna lillah wa Inna ilayh rajoon*
@TWAIBAKBANIES
@TWAIBAKBANIES 4 күн бұрын
Ma vesi ali apa zili kutali tali . Aaaaaaa koma akulu akulu sheikh mudziima pachilungamo komanso ma ves osamawakhitetsa ai
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 4 күн бұрын
Kkkkkkkkkkk wabodza ndiwe ma inovolopu yakutseka pakamwa ya chakwela, zikhale ndi kunkuyu 😂😂😂 waukape ndani sakudziwa.
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
Sheikh awa salibwino akugulitsa mawu aMulungu ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa mutsiku lomaliza
@AndersonTsoyo
@AndersonTsoyo 15 сағат бұрын
100% shehe uthenga omanganga dziko
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 2 күн бұрын
Ili ndiye gulu loyitana chakwela ku Eid atawapasa mbia makwacha mashehe adyera ichoooo!
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Usatiipisile Islam yathu iwe wamva , bwanji sukuwalesa makafiir omwe ulinawo pomwepowo kuti azikha okonda anzawo?
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
Mwapatsidwa ndalama
@Macsaidi
@Macsaidi 4 күн бұрын
Komabe sitinganame pa chilungamo. Saulos Chilima anaphedwa ndi ndege ya boma la mcp
@omardyman8083
@omardyman8083 4 күн бұрын
Ndine msilamunso koma sheikh uyu wapochelaapo nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto akatero anali ku state house
@MollenMponya
@MollenMponya Күн бұрын
Awa ndye mau ochokwera kwa Mulungu osati Za Anja amaziyesa Okha opambana
@PeterThomas-lw3io
@PeterThomas-lw3io 5 күн бұрын
Alhamudulillla sheih my Allah bless you all the time what's a sweet Message like 💋💗 this Marshall ( port Erizabeth SA missionvale
@johnarushamasese108
@johnarushamasese108 5 күн бұрын
Ana usawi chemwalimu apochele silingwa
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 4 күн бұрын
Soni jamanja
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 5 күн бұрын
God bless you Sheik all the time ❤❤❤❤❤
@juntoiman
@juntoiman 4 күн бұрын
Mmmmm sheikh zoona malo molankhula chilungamo pamaso pa anthu muli busy kubisa choona.Pamenepotu padali anzanu koma lero alikyt
@JeanKambala-gm1zr
@JeanKambala-gm1zr 5 күн бұрын
Nyasi zenizeni pamaso pamulungu chilungamo mukuchidziwa Shehe iwe. Wadya ndalama
@MafumuBanda
@MafumuBanda 5 күн бұрын
Sheikh ilim yanu ndiyochepa mupite mukaphunzirenso, ngati mukuzitenga zinthu za Allah maso mmwamba eeeeee chilango chaukali chkupezani pompo mulipo asakutameni awowo andalewo ndizotsala , ifenso tinaphunzira kwambiri kuposa iweyo xxx
@AbouzaidahSayeed
@AbouzaidahSayeed 5 күн бұрын
Kkkkkk sheikh wasanjatu uyu 😅
@NuradinaAbrahima-rt9ip
@NuradinaAbrahima-rt9ip 4 күн бұрын
No i was interested ndi ulaliki wanu Sheikh koma kumapetoko mwandionongela data yanga😭😭😭😭
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Ine ndine Msilamu, uyu ndi sheikh wa chishiya uyu kafiir weniweni uyu,
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo 5 күн бұрын
Sheikhe wamanyi uyu mbuz
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 4 күн бұрын
@@HusseinAdamLidezo zoona angamasinthanise chisilamu ndi ndalama?, bwanji sakulesa asatana anzakewa kuzunza ndikupha anthu mdziko muno ?
@trickermussa472
@trickermussa472 4 күн бұрын
Kukangotinyasisila deen yathu mbuzi ya shaikh
@marvelousmadzimure1811
@marvelousmadzimure1811 2 күн бұрын
Masha Allah ❤❤❤
@Sasha-g3z
@Sasha-g3z 4 күн бұрын
Bas allah awadalotse ndi ulaliki wawow
@yassinn5634
@yassinn5634 3 күн бұрын
Msilamu wolakira zau Mulungu osati enewa .Akuti ngati munthu wa mulungu walalika osanyoza president akuti ndiye sadziwa kulalikira. Shame
@ZionekaMember
@ZionekaMember 5 күн бұрын
Soka kwaiye akupindisa chilungamo popeza akuziyandikisa matako ake kumoto
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Zikhale ng'oma akuwombelanso mmanja pamfundoless zomwe wanena, kodi unamulesa kuti asamaphe ma ruandaniz and Burundians komanso amalawi?.
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 8 сағат бұрын
Inu nde muletsa zoipazooo suyu muyamikira mfiti ,wakuba, musatinyase
@Musa-cz1nm
@Musa-cz1nm 5 күн бұрын
Ma shaallah ma shaallah ma shaallah
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Izo mzoona zoti tiziphunzisana zabwino ndikulesana zoyipa, funso kwa iweyo shehe ndiloti; Kodi zoipa zomwe akuchita chakwelayo wamulesa? Kupha kumene akupha aboma anthu kumalawi kuno wawalesa aboma ako awusiluwo ?,
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo Күн бұрын
Thanks shelk potipatsa ulaliki wabwnowu
@KasundaAbbasi
@KasundaAbbasi 5 күн бұрын
Ngakhale mawu akewo akupepuka zoyakhula zakeso kumalemelera abusa aja
@abwinoamatani4921
@abwinoamatani4921 5 күн бұрын
Mzimu wa Chilima ukunyetseni nonse amene mukugawa ma yellow band ndi inu amene mukudya ma bans
@AminahMussah
@AminahMussah 5 күн бұрын
sheikh zamanyazitu iziii kufuna kuoneka wabwino pamanso pa pule mwadya zingat
@JUSTINChigamba
@JUSTINChigamba 3 күн бұрын
Ndipo inu zosayenda
@amoschataika7440
@amoschataika7440 4 күн бұрын
Chemoto akhale Kunkuyu😅😅😅😅
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya , Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva
@FarhaazbashaMdoka
@FarhaazbashaMdoka 3 күн бұрын
Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏
@FarhaazbashaMdoka
@FarhaazbashaMdoka 3 күн бұрын
Koma ndalamazi guyz tisamale nazo
@udkconsultancy5567
@udkconsultancy5567 5 күн бұрын
POWERFUL
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 5 күн бұрын
SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI
@Ishmael376
@Ishmael376 5 күн бұрын
Komati choti muziwe kulankhula boA pamaso pamulungu pomwe chilungamo mukuziwa muziwe kuti akakuwochani
@user-ti8ds7iq8z
@user-ti8ds7iq8z 5 күн бұрын
Chakwela akusapoter Israel shehe wa mabi
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 4 күн бұрын
Awaso nawo aaaaaa zaziiii mazidyani wosatipusitsa
@AugustineIshmael
@AugustineIshmael 4 күн бұрын
Naam ena akwiya chifukwa mwayakhula zosephana ndizomwe Iwo akufuna
@emilynthite6545
@emilynthite6545 5 күн бұрын
Apasidwa ndarama alaliki adyela
@AnnieKwisanja
@AnnieKwisanja 4 күн бұрын
Akutuma Kodi sheikh wachinyengo iwe nde akupasa zingati ?
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizaunu
@Hassankazembe-d3o
@Hassankazembe-d3o 5 күн бұрын
Sheikh apatu nanu mwanama kwambiri 😂😂😂😂😂😂
@medicoastkzn
@medicoastkzn 4 күн бұрын
Mashala
@ChristianMtambalika
@ChristianMtambalika 5 күн бұрын
Anthu muzinena chirungamo osamabisala mukaona omunenayo kuti alipopo mamizimu anthu akuvutika pqmene iweyo ukufunq kukomesera president umenewo moyo oyipa ngati uli sogoleri wapingo ndiwe waboza liuze chirungamo dziko
@UseniMailosi
@UseniMailosi 5 күн бұрын
Walykum ssalam wakahmatul llah wabaraktu
@KassimIssa-bn3od
@KassimIssa-bn3od 5 күн бұрын
Kmatu musamapange zindu kut akutamen shehe Allah wanji angasangalale ulaliki zimayi sisi kunja osamvala pango 😢😢😢 dini ulindo bas inarilah
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Moses kumkuyu akukuwombela mmanja pamfundoless zakozo, kodi unamulesa kuti asamaphe anthu ngati mmene anaphela ALLAN WITIKA uja?
@user-zf7xk8fk5s
@user-zf7xk8fk5s 5 күн бұрын
Km Inu sheikh ndinu opanda nzeru apurezident akunyoza chisilam kms amakokomezera nkhondo ku Palestine kut adziwapha asilam zoon Inu kumaim pagulu kwacemera
@user-zf7xk8fk5s
@user-zf7xk8fk5s 5 күн бұрын
Ndipo panop asilam akumalaw akuchititsa manyaz chisilam chifukwa chokonda ndalam mmmm zomvetsa chison
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 5 күн бұрын
Ndipo sheih uyu watinamizapo wadya nao ndalama za pule malawi sadzathekayi
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
Alibenzeru uyu
@user-fm7yg5yc2c
@user-fm7yg5yc2c 5 күн бұрын
Walaikum salaam warahmatullah wabarakatuh... Innalillah wainna illaih rajiun
@AliSinoya
@AliSinoya 4 күн бұрын
Sheikh uyu manyakwa
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 4 күн бұрын
Shehee wadya chamba chanji chakwera Mutu Ngati gwafa😂
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg 3 күн бұрын
Mashallah
@user-qs7xw4ph7z
@user-qs7xw4ph7z 4 күн бұрын
Amen
@MussaAndreQuenessi
@MussaAndreQuenessi 4 күн бұрын
Chakwera anapha chilima😊
@SolomonShaibuh
@SolomonShaibuh 5 күн бұрын
Live from Gaza city
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 күн бұрын
Palibe amene angakutameni yinu bodza zidyani ndalamazo msilamu weni weni akuonani Kuti mwanama akulu ndinu adyela
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 4 күн бұрын
Achina chimoto ndi a MCP ndiwe shehe😂
@moosakananji1879
@moosakananji1879 4 күн бұрын
Sheikh awa Malo ngt awa kumafunika Sheikh ayyub azipita kumeneku not awa
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 5 күн бұрын
Ndiye ulaliki otaninso uwu, mukulalikila ngati simukumva kuwawa bwanji, odya banzi sasowa.
@user-jb5yb9wq3y
@user-jb5yb9wq3y 5 күн бұрын
Ndalama Za mcp zikuyakhula
@bisweckchimphamba8497
@bisweckchimphamba8497 4 күн бұрын
Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope
@abbasdamsonamini4888
@abbasdamsonamini4888 4 күн бұрын
Naam Ameen thumma Ameen
@user-ky8eq5ek1p
@user-ky8eq5ek1p 5 күн бұрын
Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 5 күн бұрын
Ameen
@shadrackdrums3536
@shadrackdrums3536 4 күн бұрын
Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.
@user-xd1cm7tm7t
@user-xd1cm7tm7t 4 күн бұрын
Chemoto ndinu mwandila ma unforp
@HallimaMakwinja
@HallimaMakwinja 4 күн бұрын
Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama
@HallimaMakwinja
@HallimaMakwinja 4 күн бұрын
Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 5 күн бұрын
Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir
@JumaMboneka
@JumaMboneka 4 күн бұрын
Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas
@MussaAndreQuenessi
@MussaAndreQuenessi 4 күн бұрын
Awapasa ndalama 😮 awa
@NchocitoTuaibo
@NchocitoTuaibo 5 күн бұрын
Naam sheh
@JamesRoben-dy7bx
@JamesRoben-dy7bx 5 күн бұрын
Uyu anadya kale ndalama uyu komaso ndi wa mcp uyu
@abdulllahanubieimran06comanubi
@abdulllahanubieimran06comanubi 5 күн бұрын
Jazackah alla
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 2 күн бұрын
Shehe my foot 😅😅😅
@EmanuelPaul-io2hk
@EmanuelPaul-io2hk 3 күн бұрын
Shehe akufuna chuma chamagazichi eti?
KAMLEPO KALUA KUYANKHULA MOSANYENGELERA
29:23
HOT 265
Рет қаралды 29 М.
He sees meat everywhere 😄🥩
00:11
AngLova
Рет қаралды 11 МЛН
路飞被小孩吓到了#海贼王#路飞
00:41
路飞与唐舞桐
Рет қаралды 66 МЛН
Дибала против вратаря Легенды
00:33
Mr. Oleynik
Рет қаралды 5 МЛН
Мы никогда не были так напуганы!
00:15
Аришнев
Рет қаралды 6 МЛН
KAMLEPO KALUWA BOMA ZOMWE MUKUFUNA KUPANGA NDIKUDZIWA
28:58
Malawi Trends TV
Рет қаралды 7 М.
Zamanyazi mukafukufuku  wanimfa ya saulosi chilima
5:45
Nthambi Malawi
Рет қаралды 15 М.
kumalawi kuno ndani wandale angamake??
1:01:32
Malawian Cameras
Рет қаралды 63 М.
BON KALINDO 11 JULY 2024 KUNG’ALURA PA THURSDAY
17:16
Malawi Trends TV
Рет қаралды 26 М.
Wakatolika uyuyu Amutapa posachedwapa😂😂🤣😂😂
14:40
Malawian Cameras
Рет қаралды 64 М.
KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌
17:19
Palibe Chamuyaya Pa Dziko La Pansi - Hon Kamlepo Kalua
30:19
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 3,9 М.
He sees meat everywhere 😄🥩
00:11
AngLova
Рет қаралды 11 МЛН